< Luo Chronicle 13 >

1 In yac se aksingoul oalkosr lal Tokosra Jeroboam lun Israel, Abijah el tokosrala lun Judah.
Mʼchaka cha 18 cha ulamuliro wa Yeroboamu, Abiya analowa ufumu wa Yuda,
2 El leum in Jerusalem ke yac tolu. Nina kial pa Micaiah, acn natul Uriel, sie mwet in siti Gibeah. Mweun se srola inmasrlol Abijah ac Jeroboam.
ndipo analamulira mu Yerusalemu kwa zaka zitatu. Dzina la amayi ake linali Maaka mwana wa Urieli wa ku Gibeya. Koma panali nkhondo pakati pa Abiya ndi Yeroboamu.
3 Abijah el srukak mwet mweun angfoko tausin, ac Jeroboam el lainul ke mwet mweun oalfoko tausin.
Abiya anapita ku nkhondo ndi asilikali odziwa bwino nkhondo 400,000, ndipo Yeroboamu anandandalitsa ankhondo, asilikali 800,000 odziwa bwino nkhondo, osankhidwa ndi amphamvu, woti amenyane naye.
4 Un mwet mweun inge osun infulan eol in acn Ephraim. Tokosra Abijah el utyak Fineol Zemaraim ac pangla nu yorol Jeroboam ac mwet Israel, ac fahk, “Porongo ma nga ac fahk uh!
Abiya anayima pa phiri la Zemaraimu, mʼdziko lamapiri la Efereimu, ndipo anati, “Yeroboamu ndi Aisraeli onse, tandimverani!
5 Ya kowos nikin lah LEUM GOD lun Israel El tuh orala wulela se nu sel David su tia ku in musalla, mu el ac tulik natul ac fah tokosra fin Israel nwe tok?
Kodi inu simukudziwa kuti Yehova, Mulungu wa Israeli, wapereka ufumu wa Israeli kwa Davide ndi zidzukulu zake mpaka muyaya ndiponso pangano la mchere?
6 Jeroboam, wen natul Nebat, el tuh orek lokoalok lainul Solomon, tokosra lal.
Komabe Yeroboamu mwana wa Nebati, mtumiki wa Solomoni mwana wa Davide, anawukira mbuye wake.
7 Toko, el orani sie un mwet lusrongten, ac elos pahtok lungse lalos nu facl Rehoboam, wen natul Solomon, su srakna fusr ac mwalna ke inkanek in lainulos.
Ndipo anthu ena achabechabe anasonkhana kwa iye ndipo anatsutsana ndi Rehobowamu mwana wa Solomoni pamene anali wamngʼono ndi wosalimba mtima ndi wopanda mphamvu kuti athe kulimbana nawo.
8 Ac inge kowos ako in mweun lain tokosrai se su LEUM GOD El sang nu sin fita lal David. Oasr un mwet mweun lulap lowos, ac oasr pac yuruwos cow mukul fusr orekla ke gold, ma Jeroboam el orala tuh in god lowos.
“Ndipo tsopano inu mwakonzekera kutsutsana ndi ufumu wa Yehova, umene uli mʼmanja mwa zidzukulu za Davide. Inu ndithu mulipo ankhondo ambirimbiri ndipo muli ndi ana angʼombe agolide amene Yeroboamu anapanga kuti akhale milungu yanu.
9 Kowos lusla mwet tol lun LEUM GOD, su ma in fwil natul Aaron, ac kowos lusla pac mwet Levi. Na kowos srisrngiya mwet in aolulos, oana ouiya su orek in mutunfacl saya. Kutena mwet su use soko cow mukul, ku sheep itkosr, el ku in sifacna oru tuh elan sie mwet tol lun ma su kowos pangon god lowos ingan.
Koma kodi inu simunathamangitse ansembe a Yehova, ana a Aaroni ndiponso Alevi ndi kudzisankhira ansembe anuanu monga anthu ena amachitira? Aliyense amene amabwera kuti adzipatule atatenga mwana wangʼombe wamwamuna ndi nkhosa zazimuna zisanu ndi ziwiri amakhala wansembe wa zinthu zimene sizili milungu.
10 “A funu kut, kut srakna kulansupu LEUM GOD lasr, ac kut tiana fahsr lukel. Mwet tol su ma in fita lal Aaron, elos srakna oru ma kunalos, ac mwet Levi kasrelos.
“Koma kunena za ife, Yehova ndiye Mulungu wathu, ndipo sitinamusiye. Ansembe amene amatumikira Yehova ndi ana a Aaroni ndipo amathandizidwa ndi Alevi.
11 Lotutang nukewa ac eku nukewa elos esukak mwe keng nu sel, ac oru mwe kisa ke kosro ma fonna isisyak. Elos sang mwe kisa bread nu fin sie tepu aknasnasyeyukla fal nu ke oakwuk lun alu. Ac eku nukewa elos akosak lam uh fin sukan lam gold. Kut oru na ma LEUM GOD El sapkin, a kowos sisella.
Mmawa uliwonse ndi madzulo aliwonse amapereka nsembe zopsereza ndi kufukiza lubani kwa Yehova. Iwo amayika buledi pa tebulo loyeretsedwa monga mwa mwambo ndipo amayatsa nyale pa zoyikapo nyale zagolide madzulo aliwonse. Ife timachita zofuna za Yehova Mulungu wathu. Koma inu mwamusiya.
12 God sifacna El mwet kol lasr, ac mwet tol lal elos wi kut inge. Elos sruokya mwe ukuk ac akola in ukya in pangon kut nu ke mweun lain kowos. Mwet Israel, nimet kowos mweun lain LEUM GOD lun papa tomowos! Kowos ac tia ku in kutangla!”
Mulungu ali nafe pakuti ndiye mtsogoleri wathu. Ansembe ake atanyamula malipenga, adzayimba mfuwu wankhondo kulimbana nanu. Inu Aisraeli musalimbane ndi Yehova, Mulungu wa makolo anu, pakuti simungathe kupambana.”
13 In pacl sac pacna, Jeroboam el tuh supwala kutu sin mwet mweun lal ah in kasrik ut tukun mwet Judah, na mwet lula elos tu meet ac ngetang nu selos.
Tsono Yeroboamu anali atatumiza asilikali kumbuyo mowazungulira, kotero kuti iye ali kutsogolo kwa anthu a ku Yuda, anthu owabisalira anali kumbuyo kwawo.
14 Mwet Judah elos tapulla ac liye tuh na rauniyukla elos, na elos pang nu sin LEUM GOD Elan kasrelos, ac mwet tol elos ukya mwe ukuk.
Asilikali a Yuda anatembenuka ndipo anaona kuti nkhondo imachitikira kutsogolo ndi kumbuyo. Ndipo iwo anafuwulira Yehova. Ansembe anayimba malipenga awo
15 Na mwet Judah elos sala ke pusra lulap, ac Abijah el kol mwet inge ke mweun lalos. God El kutangulla Jeroboam ac mwet mweun lun Israel.
ndipo asilikali a Yuda anafuwula mawu ankhondo. Atafuwula mawu ankhondowo, Mulungu anagonjetsa Yeroboamu pamodzi ndi Aisraeli onse pamaso pa Abiya ndi Yuda.
16 Mwet Israel elos kaing liki mwet Judah, ac God El oru tuh mwet mweun lun Judah in arulana ku lukelos.
Aisraeli anathawa Ayuda. Ndipo Mulungu anawapereka mʼmanja mwawo.
17 Abijah ac mwet mweun lal orala kutangla na yohk fin mwet Israel. Mwet lumfoko tausin sin mwet ma pisrla ke mweun lun mwet Israel pa anwuki ke mweun sac.
Abiya pamodzi ndi anthu ake anapha anthu ambiri, kotero kuti Aisraeli 500,000 odziwa bwino nkhondo anaphedwa.
18 Ouinge mwet Judah elos kutangla mwet Israel, mweyen elos filiya finsrak lalos in LEUM GOD lun papa tumalos.
Ankhondo a Israeli anagonjetsedwa pa nthawi imeneyi, ndipo ankhondo a Yuda anapambana chifukwa anadalira Yehova, Mulungu wa makolo awo.
19 Abijah el ukwe mwet mweun lal Jeroboam ac sruokya siti lal inge: Bethel, Jeshanah, ac Ephron, oayapa inkul ma oan apkuran nu ke kais sie siti inge.
Abiya anathamangitsa Yeroboamu ndipo anamulanda mizinda ya Beteli, Yesana, ndi Efroni pamodzi ndi midzi yawo yozungulira.
20 Ke lusen pacl Abijah el leum, Jeroboam el tiana sifil ku. Saflaiyel LEUM GOD El unilya, ac el misa.
Yeroboamu sanapezenso mphamvu nthawi ya Abiya. Ndipo Yehova anamukantha nafa.
21 Ouinge Abijah el yokyokelik ke ku lal. Oasr mutan singoul akosr kial, ac el papa tumun wen longoul luo ac acn singoul onkosr.
Koma Abiya mphamvu zake zinakula. Iye anakwatira akazi 14 ndipo anali ndi ana aamuna 22 ndi ana aakazi 16.
22 Ma nukewa saya ke sramsram matu kacl Abijah, ma el fahk ac ma el oru, simla ke [Sramsram Matu lal Iddo Mwet Palu.]
Zina ndi zina zokhudza Abiya, zimene anachita ndi zimene anayankhula, zinalembedwa mʼbuku la mbiri ya mneneri Ido.

< Luo Chronicle 13 >