< Sie Samuel 3 >
1 In pacl se ke tulik Samuel el kulansupu LEUM GOD ye koko lal Eli, tia pus pacl LEUM GOD El sramsram nu sin mwet, ku sikyang nu sin mwet in aruruma.
Samueli ankatumikira Yehova moyangʼaniridwa ndi Eli. Masiku amenewo mawu a Yehova sankamveka pafupipafupi. Kuona zinthu mʼmasomphenya sikunkachitikanso kawirikawiri.
2 Sie fong ah Eli, su apkuran elan kunla mutal, el motul infukil sel sifacna.
Tsiku lina Eli, amene maso anali ofowoka ndi kuti sankatha kuona bwino, anagona pa malo ake.
3 Ac Samuel el motul in acn mutal, acn ma Tuptup in Wuleang lun LEUM GOD oan we. Meet liki lenelik, ke lam uh srakna firir,
Nthawiyi nʼkuti nyale ya Mulungu isanazimitsidwe. Samueli anali gone mu Nyumba ya Yehova, kumene kunali Bokosi la Chipangano cha Mulungu.
4 LEUM GOD El pangnol Samuel. Ac Samuel el topuk, “Nga inge!”
Yehova anayitana Samueli. Iye anayankha kuti, “Wawa.”
5 ac el kasrusr nu yorol Eli ac fahk, “Nga inge, tuh kom pangonyu.” A Eli el fahk, “Nga tia pangon kom. Folokla motulla.” Na Samuel el folokla ac motulla.
Ndipo iyeyo anathamangira kwa Eli ndipo anati, “Ndabwera ndamva kuyitana.” Koma Eli anati, “Ine sindinakuyitane, bwerera kagone.” Ndipo iye anapita kukagona.
6 Ac LEUM GOD El sifil pang, “Samuel!” Samuel el sifil tukakek ac som nu yorol Eli ac fahk, “Nga inge, tuh kom pangonyu.” A Eli el fahk, “Nga tia pangon kom. Folokla motulla.”
Yehova anayitananso, “Samueli!” Ndipo Samueli anadzuka ndi kupita kwa Eli nati, “Ndabwera popeza ndamva mukundiyitana.” Eli nati, “Mwana wanga, ine sindinakuyitane, bwerera kagone.”
7 Samuel el tiana akilen lah LEUM GOD pa pangnol, mweyen soenna oasr pacl LEUM GOD El kaskas nu sel.
Nthawiyi nʼkuti Samueli asanadziwe Yehova ndipo Mawu a Yehova nʼkuti asanawululidwe kwa iye.
8 LEUM GOD El sifilpa pangnol Samuel ke pacl se aktolu. Na Samuel el tukakek ac som nu yorol Eli ac fahk, “Nga inge, tuh kom pangonyu.” Na Eli el akilenak lah LEUM GOD pa pangnol uh.
Yehova anayitananso Samueli kachitatu ndipo Samueli anadzuka ndikupita kwa Eli ndipo anati, “Ndabwera popeza mwandiyitana ndithu.” Apo Eli anazindikira kuti Yehova ndiye ankayitana mnyamatayo.
9 Na Eli el fahk nu sel Samuel, “Folokla motulla, ac El fin sifil pangon kom, na kom fahk, ‘LEUM GOD, kaskas, tuh mwet kulansap lom el porongo.’” Na Samuel el folokla ac motulla.
Tsono Eli anamuwuza Samueli kuti, “Pita ukagone ndipo akakuyitananso ukanene kuti, ‘Yankhulani Yehova, pakuti mtumiki wanu ndikumvetsera.’” Choncho Samueli anapita ndi kukagona pamalo pake.
10 Ac LEUM GOD El tuku tuyang, ac pangnol oana ke El oru meet ah, “Samuel! Samuel!” Na Samuel el topuk ac fahk, “Kaskas, tuh mwet kulansap lom el porongo.”
Yehova anabwera ndi kuyima pomwepo, ndi kuyitana monga nthawi zina zija, “Samueli! Samueli!” Ndipo Samueli anayankha, “Yankhulani, pakuti mtumiki wanu akumvetsera.”
11 Ac LEUM GOD El fahk nu sel, “Sie pacl nga ac fah oru sie ma na upa in Israel, ac elos nukewa su lohng ac fah arulana lut ac oela kac.
Ndipo Yehova anati kwa Samueli, “Taona, patsala pangʼono kuti ndichite chinthu china mu Israeli chimene chidzadabwitsa aliyense amene adzamve.
12 In len sac nga ac fah oru ma nukewa ma nga fahk mu nga ac oru lain sou lal Eli, mutawauk nwe ke safla.
Tsiku limenelo ndidzachitadi zonse zimene ndinayankhula zokhudza banja la Eli kuyambira poyamba mpaka pomaliza.
13 Nga fahk nu sel tari lah nga ac fah kai sou lal ma pahtpat, ke sripen wen natul kaskas koluk lainyu. Eli el etu ma eltal oru a el tia kutongoltal.
Pakuti ndinamudziwitsa kuti Ine ndikhoza kulanga banja lake kwamuyaya chifukwa cha zoyipa zimene ana ake ankadziyipitsa nazo. Iye ankadziwa zimenezi koma osawaletsa.
14 Ouinge nga fahkak kalem nu sin sou lal Eli lah ac fah wangin mwe kisa ku mwe sang fah ku in molelosla liki ma koluk lalos inge.”
Nʼchifukwa chake ndinalumbira kuti, ‘Zoyipa zimene banja la Eli linandichita sizidzafafanizidwa mpaka muyaya ngakhale adzapereke nsembe kapena zopereka zina.’”
15 Ac Samuel el oanna nwe ke lenelik, na el tukakek ac ikasla srungul in lohm sin LEUM GOD. El sangeng in fahkak aruruma sac nu sel Eli.
Samueli anagona mpaka mmawa. Atadzuka anatsekula zitseko za Nyumba ya Yehova. Iye anachita mantha kumuwuza Eli za masomphenya ake.
16 Ac Eli el pangnol Samuel ac fahk, “Samuel, wen nutik!” Na Samuel el topuk, “Nga inge.”
Koma Eli anamuyitana nati, “Samueli mwana wanga.” Samueli anayankha kuti, “Wawa.”
17 Eli el siyuk sel, “Mea LEUM GOD El fahk nu sum? Nikmet okanla kutena ma. God El ac arulana kai kom, kom fin tia fahk ma nukewa nu sik.”
Tsono Eli anafunsa kuti, “Yehova wakuwuza chiyani? Usandibisire. Mulungu akulange ndithu ngati undibisira chilichonse cha zimene wakuwuza.”
18 Na Samuel el fahkak ma nukewa nu sel Eli. El tia okanla kutena ma. Eli el fahk, “El pa LEUM GOD. Lela Elan oru fal nu ke lungse lal.”
Choncho Samueli anamuwuza zonse, sanamubisire kalikonse. Ndipo Eli anati, “Iye ndi Yehova, mulekeni achite chimene chamukomera.”
19 Ke Samuel el kapkapak, LEUM GOD El welul ac oru tuh ma nukewa Samuel el fahk in pwaye.
Yehova anali ndi Samueli pamene amakula, ndipo zonse zimene ankayankhula zinkachitikadi.
20 Ouinge mwet Israel nukewa, mutawauk na e Dan me fahsru nwe Beersheba, elos etu tuh Samuel el mwet palu suwoswos lun God.
Ndipo Aisraeli onse kuyambira ku dera la Dani mpaka ku Beeriseba anazindikira kuti Yehova analozadi chala pa Samueli kuti akhale mneneri wake.
21 Pacl pus LEUM GOD El sikyak in acn Shiloh, acn se ma El tuh sramsram nu sel Samuel we. Pacl nukewa Samuel el ac sramsram uh, mwet Israel nukewa porongo.
Yehova anapitiriza kuoneka ku Silo, ndipo kumeneko anadziwulula yekha kwa Samueli mwa mawu ake.