< 여호수아 12 >

1 이스라엘 자손이 요단 저편 해 돋는 편 곧 아르논 골짜기에서 헤르몬산까지의 동방 온 아라바를 점령하고 그 땅에서 쳐 죽인 왕들은 이러하니라
Aisraeli anagonjetsa dziko lonse la kummawa kwa Yorodani, kuyambira ku chigwa cha Arinoni mpaka ku phiri la Herimoni pamodzi ndi dera lonse la kummawa kwa Araba. Iwo anatenga dzikoli kukhala lawo, ndipo mafumu a dzikoli anali awa:
2 헤스본에 거하던 아모리 사람의 왕 시혼이라 그 다스리던 땅은 아르논 골짜기 가에 있는 아로엘에서부터 골짜기 가운데 성읍과 길르앗 절반 곧 암몬 자손의 지경 얍복강까지며
Sihoni mfumu ya Aamori, amene ankakhala mu Hesiboni. Iye analamulira kuyambira ku Aroeri mzinda umene uli mʼmphepete mwa mtsinje wa Arinoni, mpaka ku mtsinje wa Yaboki, umene uli mʼmalire mwa Aamori, kuphatikizanso theka la dziko la Giliyadi.
3 또 동방 아라바 긴네롯 바다까지며 또 동방 아라바의 바다 곧 염해의 벧여시못으로 통한 길까지와 남편으로 비스가 산록까지며
Iye ankalamuliranso dera la chigwa cha Yorodani kuyambira ku Nyanja ya Kinereti, kummawa ndi kumatsika mpaka ku Beti-Yesimoti, mzinda umene unali kummawa kwa Nyanja ya Mchere ndi kutsikabe kummwera mpaka pa tsinde pa phiri la Pisiga.
4 또 르바의 남은 족속으로서 아스다롯과 에브레이에 거하던 바산 왕 옥이라
Ogi mfumu ya mzinda wa Basani, amene anali mmodzi mwa otsala mwa Arefaimu. Iye ankakhala ku Asiteroti ndi Ederi.
5 그 치리하던 땅은 헤르몬산과 살르가와 온 바산과 및 그술 사람과 마아가 사람의 지경까지의 길르앗 절반이니 헤스본 왕 시혼의 지경에 접한 것이라
Dera la ufumu wake linafika ku phiri la Herimoni, ku Saleka ndi dziko lonse la Basani mpaka ku malire ndi anthu a ku Gesuri Makati. Ufumu wake unaphatikizanso theka la Giliyadi mpaka ku malire a mfumu Sihoni ya ku Hesiboni.
6 여호와의 종 모세와 이스라엘 자손이 그들을 치고 여호와의 종 모세가 그 땅을 르우벤 사람과, 갓 사람과, 므낫세 반 지파에게 기업으로 주었더라
Mose mtumiki wa Yehova ndi Aisraeli anawagonjetsa ndipo anapereka dziko lawo kwa anthu a fuko la Rubeni, fuko la Gadi ndi theka la fuko la Manase kuti chikhale cholowa chawo.
7 여호수아와 이스라엘 자손이 요단 이편 곧 서편 레바논 골짜기의 바알갓에서부터 세일로 올라가는 곳 할락산까지에서 쳐서 멸한 왕들은 이러하니 그 땅을 여호수아가 이스라엘의 구별을 따라 그 지파에게 기업으로 주었으니
Yoswa ndi Aisraeli onse anagonjetsa mafumu onse okhala kumadzulo kwa mtsinje wa Yorodani kuyambira ku Baala-Gadi, ku chigwa cha Lebanoni mpaka ku phiri la Halaki, kumapita cha ku Seiri. Yoswa anagawira dzikolo mafuko a Israeli kuti likhale cholowa chawo.
8 곧 산지와, 평지와, 아라바와, 경사지와, 광야와, 남방 곧 헷 사람과, 아모리 사람과, 가나안 사람과, 브리스 사람과, 히위 사람과, 여부스사람의 땅이라)
Dziko limeneli linali dera la ku mapiri, chigwa cha kumadzulo, chigwa cha Yorodani, ku matsitso a kummawa, ndi dziko la chipululu la kummwera. Amene ankakhala mʼdzikoli anali Ahiti, Aamori, Akanaani, Aperezi, Ahivi ndi Ayebusi. Mafumu ake anali awa:
9 하나는 여리고 왕이요, 하나는 벧엘 곁의 아이 왕이요
mfumu ya Yeriko imodzi mfumu ya Ai (kufupi ndi Beteli imodzi
10 하나는 예루살렘 왕이요, 하나는 헤브론 왕이요, 하나는 야르뭇 왕이요
mfumu ya Yerusalemu imodzi mfumu ya Hebroni imodzi
11 하나는 라기스 왕이요
mfumu ya Yarimuti imodzi mfumu ya Lakisi imodzi
12 하나는 에글론 왕이요, 하나는 게셀 왕이요
mfumu ya Egiloni imodzi mfumu ya Gezeri imodzi
13 하나는 드빌 왕이요, 하나는 게델 왕이요
mfumu ya Debri imodzi mfumu ya Gederi imodzi
14 하나는 호르마 왕이요, 하나는 아랏 왕이요
mfumu ya Horima imodzi mfumu ya Aradi imodzi
15 하나는 립나 왕이요, 하나는 아둘람 왕이요
mfumu ya Libina imodzi mfumu ya Adulamu imodzi
16 하나는 막게다 왕이요, 하나는 벧엘 왕이요
mfumu ya Makeda imodzi mfumu ya Beteli imodzi
17 하나는 답부아 왕이요, 하나는 헤벨 왕이요
mfumu ya Tapuwa imodzi mfumu ya Heferi imodzi
18 하나는 아벡 왕이요, 하나는 랏사론 왕이요
mfumu ya Afeki imodzi mfumu ya Lasaroni imodzi
19 하나는 마돈 왕이요, 하나는 하솔 왕이요
mfumu ya Madoni imodzi mfumu ya Hazori imodzi
20 하나는 시므론 므론 왕이요, 하나는 악삽 왕이요
mfumu ya Simuroni Meroni imodzi mfumu ya Akisafu imodzi
21 하나는 다아낙 왕이요, 하나는 므깃도 왕이요
mfumu ya Taanaki imodzi mfumu ya Megido imodzi
22 하나는 게데스 왕이요, 하나는 갈멜의 욕느암 왕이요
mfumu ya Kadesi imodzi mfumu ya Yokineamu ku Karimeli imodzi
23 하나는 돌의 높은 곳의 돌 왕이요, 하나는 길갈의 고임 왕이요
mfumu ya Dori ku Nafoti Dori imodzi mfumu ya Goyini ku Giligala imodzi
24 하나는 디르사 왕이라 도합 삼십 일 왕이었더라
mfumu ya Tiriza imodzi mafumu onse pamodzi analipo 31.

< 여호수아 12 >