< 창세기 10 >

1 노아의 아들 셈과, 함과, 야벳의 후예는 이러하니라 홍수 후에 그들이 아들들을 낳았으니
Nayi mbiri ya ana a Nowa, Semu, Hamu ndi Yafeti. Ana atatuwa anabereka ana awo chitatha chigumula.
2 야벳의 아들은 고멜과, 마곡과, 마대와, 야완과, 두발과, 메섹과, 디라스요
Ana aamuna a Yafeti anali: Gomeri, Magogi, Madai, Yavani, Tubala, Mesaki ndi Tirasi.
3 고멜의 아들은 아스그나스와, 리밧과, 도갈마요
Ana aamuna a Gomeri anali: Asikenazi, Rifati ndi Togarima.
4 야완의 아들은 엘리사와, 달시스와, 깃딤과, 도다님이라
Ana aamuna a Yavani anali: Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Rodanimu.
5 이들로부터 여러 나라 백성으로 나뉘어서 각기 방언과 종족과 나라대로 바닷가의 땅에 머물렀더라
(Amenewa ndiwo makolo a anthu okhala mʼmphepete mwa nyanja. Awa ndi ana a Yafeti monga mwa mafuko a mu mitundu yawo, uliwonse ndi chiyankhulo chake).
6 함의 아들은 구스와, 미스라임과, 붓과, 가나안이요
Ana aamuna a Hamu anali: Kusi, Miziraimu, Puti ndi Kanaani.
7 구스의 아들은 스바와, 하윌라와, 삽다와, 라아마와, 삽드가요, 라아마의 아들은 스바와, 드단이며
Ana aamuna a Kusi anali: Seba, Havila, Sabita, Raama ndi Sabiteka. Ana aamuna a Raama anali: Seba ndi Dedani.
8 구스가 또 니므롯을 낳았으니 그는 세상에 처음 영걸이라
Kusi anabereka Nimurodi amene anali wankhondo wamphamvu kwambiri pa dziko lapansi.
9 그가 여호와 앞에서 특이한 사냥군이 되었으므로 속담에 이르기를 아무는 여호와 앞에 니므롯 같은 특이한 사냥군이로다 하더라
Iye anali mlenje wamphamvu kwambiri pamaso pa Yehova; nʼchifukwa chake anthu ali ndi chisudzo, chakuti, “Ndiwe mlenje wamphamvu kwambiri pamaso pa Yehova monga Nimurodi.”
10 그의 나라는 시날땅의 바벨과, 에렉과, 악갓과, 갈레에서 시작되었으며
Malo oyambirira a ufumu wake anali Babeli, Ereki, Akadi ndi Kaline. Malo onsewa anali mʼdziko la Sinara.
11 그가 그 땅에서 앗수르로 나아가 니느웨와, 르호보딜과, 갈라와
Atachoka mʼdziko limeneli anapita ku Asiriya kumene anakamanga Ninive, Rehoboti-Iri, Kala,
12 및 니느웨와 갈라 사이의 레센(이는 큰 성이라)을 건축하였으며
ndi Reseni, mzinda waukulu umene uli pakati pa Ninive ndi Kala.
13 미스라임은 루딤과, 아나밈과, 르하빔과, 납두힘과
Igupto ndiye kholo la Aludi, Aanami, Alehabu, Anafutu,
14 바드루심과, 가슬루힘과, 갑도림을 낳았더라 (블레셋이 가슬루힘에게서 나왔더라)
Apaturusi, Akasilu ndi Akafitori (kumene kunachokera Afilisti).
15 가나안은 장자 시돈과, 헷을 낳고
Kanaani anabereka mwana wake wachisamba, Sidoni, ndipo anaberekanso Ahiti;
16 또 여부스 족속과, 아모리 족속과, 기르가스 족속과
Ayebusi, Aamori, Agirigasi;
17 히위 족속과, 알가 족속과, 신 족속과
Ahivi, Aariki, Asini,
18 아르왓 족속과, 스말 족속과, 하맛 족속의 조상을 낳았더니 이 후로 가나안 자손의 족속이 흩어져 처하였더라
Aaravadi, Azemari ndi Ahamati. Pambuyo pake, mafuko a Akanaani anafalikira ponseponse,
19 가나안의 지경은 시돈에서부터 그랄을 지나 가사까지와, 소돔과, 고모라와, 아드마와, 스보임을 지나 라사까지였더라
mpaka ku malire a Kanaani. Malirewo anachokera ku Sidoni kulowa cha ku Gerari mpaka ku Gaza, ndi kulowa ku Sodomu, Gomora, Adima ndi Zeboimu mpaka ku Lasa.
20 이들은 함의 자손이라 각기 족속과 방언과 지방과 나라대로이었더라
Amenewa ndiwo ana aamuna a Hamu monga mwa mafuko ndi ziyankhulo zawo, mʼmadera omwe amakhala ndi mitundu yawo.
21 셈은 에벨 온 자손의 조상이요 야벳의 형이라 그에게도 자녀가 출생하였으니
Semu amene anali mkulu wake wa Yafeti nayenso anabereka nakhala kholo la Eberi.
22 셈의 아들은 엘람과, 앗수르와, 아르박삿과, 룻과, 아람이요
Ana aamuna a Semu anali: Elamu, Asuri, Aripakisadi, Ludi ndi Aramu.
23 아람의 아들은 우스와, 훌과, 게델과, 마스며
Ana aamuna a Aramu anali: Uzi, Huri, Geteri ndi Mesaki.
24 아르박삿은 셀라를 낳고, 셀라는 에벨을 낳았으며
Aripakisadi anabereka Sela, ndipo Selayo anabereka Eberi.
25 에벨은 두 아들을 낳고, 하나의 이름을 벨렉이라 하였으니 그 때에 세상이 나뉘었음이요 벨렉의 아우의 이름은 욕단이며
A Eberi anabereka ana aamuna awiri: Wina anamutcha Pelegi chifukwa pa nthawiyo anthu a pa dziko lapansi anagawikana. Dzina la mʼbale wake linali Yokitani.
26 욕단은 알모닷과, 셀렙과, 하살마웹과, 예라와
Yokitani anabereka Alimodadi, Selefi, Hazari-Maveti, Yera,
27 하도람과, 우살과, 디글라와
Hadoramu, Uzali, Dikila,
28 오발과, 아비마엘과, 스바와
Obali, Abimaeli, Seba,
29 오빌과, 하윌라와, 요밥을 낳았으니 이들은 다 욕단의 아들이며
Ofiri, Havila ndi Yobabu. Onsewa anali ana aamuna a Yokitani.
30 그들의 거하는 곳은 메사에서부터 스발로 가는 길의 동편 산이었더라
Chigawo chimene ankakhala chinayambira ku Mesa mpaka ku Seferi, ku dera la mapiri chakummawa.
31 이들은 셈의 자손이라 그 족속과 방언과 지방과 나라대로였더라
Amenewa ndiwo ana a Semu monga mwa mafuko ndi ziyankhulo zawo, mʼmadera omwe ankakhala ndi mitundu yawo.
32 이들은 노아 자손의 족속들이요 그 세계와 나라대로라 홍수 후에 이들에게서 땅의 열국 백성이 나뉘었더라
Amenewa ndiwo mafuko a ana aamuna a Nowa monga mwa mibado ya mitundu yawo. Mitundu yonse ya anthu inatuluka mwa iwowa ndi kufalikira pa dziko lonse lapansi chitatha chigumula chija.

< 창세기 10 >