< 4 Mose 15 >

1 Ra Anumzamo'a amanage huno Mosesena asmi'ne,
Yehova anawuza Mose kuti,
2 Israeli vahera zamasmige'za taminaku'ma nehua mopafima umanisu'za avaririsaza kasegea ama'ne.
“Yankhula ndi Aisraeli ndipo uwawuze kuti, ‘Mukakalowa mʼdziko limene ndikukupatsanilo,
3 Hagi tamagratami tamavesite kresramna vu ofa hugahazo, huvempa hunesare hu ofo, ranra knare'ma hu ofa hanazana, tamagra'a afu kevufinti bulimakaone, sipisipine, memene aheta kresramna tevefima nevazage'nama mna'ama nentahina Ra Anumzamo'na musema nehua ofa hugahaze.
ndipo mukamadzapereka kwa Yehova, nsembe yotentha pa moto ya ngʼombe kapena nkhosa monga fungo lokoma kwa Yehova, kaya ndi nsembe yopsereza kapena nsembe zina, nsembe yapadera chifukwa cha lumbiro kapena nsembe yoperekedwa mwaufulu kapenanso yoperekedwa pa chikondwerero,
4 Hagi mago'mo'ma sipisipio memema ofama erinoma Ra Anumzamo'narema esuno'a mago kilo hu'nesia witia 1lita olivi masavene eri havia huno herunesia witi ofama hu'zana erino egahie.
munthu amene akubweretsa zopereka zake, azikapereka kwa Yehova chopereka chachakudya cholemera kilogalamu imodzi ya ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta wokwana lita imodzi.
5 Hagi kresramna vu ofama hanazana, mago sipisipine 1lita wainine kresramna vugahaze.
Pamodzi ndi mwana wankhosa aliyense wa nsembe yopsereza kapena nsembe ina, muzikakonzanso lita imodzi la vinyo ngati chopereka cha chakumwa.’”
6 Hagi ve sipisipima kresramna vunaku'ma hanuta, 2kilo hu'nesia witine 1litagi hafu'a lita olive masavene herugahaze.
“Pamodzi ndi nkhosa yayimuna, muzikakonzanso chopereka cha chakudya cholemera makilogalamu awiri a ufa wosalala, wosakaniza ndi mafuta okwanira lita imodzi ndi theka,
7 Hagi waini ofama hanuta, 1litagi hafu'a lita waininu sipisipinena ofa hanage'na mna'a nentahina musena hugahue.
ndi vinyo wokwanira lita imodzi ndi theka ngati chopereka cha chakumwa. Muzikapereka monga nsembe yopereka fungo lokoma kwa Yehova.
8 Hagi agaho bulimakaoma aheta kre fanenema hu ofama hunakuma hanuto, huvempama hunesarema ofama hunaku'ma hanuto, rimpa fru ofama hunaku'ma hanuta,
“‘Pamene mukukonza mwana wangʼombe wamwamuna kuti akhale nsembe yopsereza kapena nsembe ina iliyonse: ya lumbiro lapadera kapena nsembe yachiyanjano kwa Yehova,
9 witia 3'a kilo hu'nesia herafinteta, 2'a lita hu'nesia olivi masavene herugahaze.
pamodzi ndi mwana wangʼombe wamwamunayo muzibweretsa nsembe yachakudya yolemera makilogalamu atatu a ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta okwana malita awiri.
10 Hagi 2 lita waini enerita mago ve bulimakaone erita eho. Nagra Ra Anumzamo'na e'ina hu ofamofo mna'a nentahina musena hugahue.
Komanso muzibweretsa vinyo wokwanira malita awiri monga chopereka chachakumwa. Imeneyi idzakhala chopereka chotentha pa moto kuti likhale fungo lokoma kwa Yehova.
11 E'ina huta witima, olivi masavema, waini ofanena mago'mago ve bulimakaone, ve sipisipine, sipisipi anenta'ene meme anenta'ene ofa Nagritega hugahaze.
Ngʼombe yayimuna iliyonse kapena nkhosa yayimuna iliyonse, mwana wankhosa aliyense kapena mbuzi yayingʼono, zizikonzedwa motere.
12 Hagi e'inahukna huta maka ofa hugahaze.
Ngakhale zingachuluke chotani, chitani izi kwa iliyonse ya nyamazo.
13 Maka Israeli vahepima kasezmantesaza vahe'mo'za kresramna vanage'na mana'ama nentahina musema hanua ofama hanuza anahukna hugahaze.
“‘Mbadwa iliyonse ya mu Israeli izichita zimenezi pamene ibweretsa nsembe yotentha pa moto kuti ikhale fungo lokoma kwa Yehova.
14 Hagi tamagranema emani'naza vahe' mo'za kremna vanagena mna'ama nentahina musema hanua ofama hanuza, ana zanke' hu'za ama kasegea avaririho.
Ku mibado yanu yonse ya mʼtsogolo, pamene mlendo kapena wina aliyense wokhala pakati panu apereka chopereka chotentha pa moto kuti chikhale fungo lokoma kwa Yehova, azichita mofanana ndi momwe inu mumachitira.
15 Hagi magoke tra ke me'nena rurega vahe'ene Israeli vahe'motanena avaririgahaze. Ama'i ana tra kemo'a mevava huno vugahie. Na'ankure Nagra Ra Anumzamo'na Israeli vahe'ma tamagoana magoke avamenteke vahe mani'naze.
Gulu lonse likhale ndi malamulo ofanana a inu kapena mlendo wokhala pakati panu. Limeneli ndi lamulo lamuyaya kwa mibado imene ikubwera. Inuyo ndi mlendo mudzakhala wofanana pamaso pa Yehova.
16 Hagi ama magoke tra ke me'nena rurega vahe'ma tamagranema emani'nenaza vahe'mo'za avaririgahaze.
Mudzakhale ndi malamulo ndi miyambo yofanana, inuyo ndi mlendo wokhala pakati panu.’”
17 Ra Anumzamo'a anage huno Mosesena asami'ne,
Yehova anawuza Mose kuti,
18 ama nanekea Israeli vahera zamasamio, nagrama taminaku'ma nehua mopafima uhanatita,
“Yankhula ndi Aisraeli ndipo unene kuti, ‘Mukakalowa mʼdziko limene ndikukutengeraniko
19 mopafima hozama ome antesageno ne'zamo'ma nenama hina, ese ne'zana refko huta ofa eme namiho.
ndipo mukakadya chakudya cha mʼdzikolo, mukapereke gawo lina kwa Yehova monga chopereka.
20 Hagi witi hozama antesageno ese'ma nenama hania witia erita witima refuzafunepaza kumapi ome refuzafupeteta, kekia kreta eme namiho.
Pa buledi wanu woyamba, mukapereke mmodzi monga nsembe, ngati chopereka chochokera ku malo wopunthira tirigu.
21 Hagi henkama fore hu anante anantema hu'za vanaza vahe'mo'za, ama ana tra ke avariri'za bretia kre'za ofa hugahaze.
Pa mibado yanu yonse muzidzapereka chopereka ichi kwa Yehova kuchokera ku zakudya zanu zoyamba za mʼnthaka.
22 Hagi Ra Anumzamo'nama Mosesema asami'noa tra kema mago vahe'mo'ma mago'azama hanirega hantga huno runetragenigeno,
“‘Ndipo ngati muchimwa mosadziwa posasunga ena mwa malamulo awa amene Yehova wapereka kwa Mose,
23 henkama fore hu anante anantema hanaza vahe'mo'za Ra Anumzamo'na Mosesesema asami'noa tra kema mago'a zama haniregama hantga huno runetragenigeno,
lina lililonse mwa malamulo a Yehova amene wapereka kwa inu kudzera mwa Mose, kuyambira tsiku limene Yehova anawapereka mpaka mibado ya mʼtsogolo,
24 ana mikamotama mago'azama hanaregama hantga huta tra ke'nima ruhantagisuta, mago ve bulimakao afu kre fanene hu ofa nehinkena mna'a nentahina musena haneno. Hagi ana ofama hanazana witine, wainine nehuta mago ve memena aheta kumima apasente ofa kresramna vugahaze.
ndipo ngati zimenezi zachitika osati mwadala ndipo gulu lonse silinadziwe, zikatero gulu lonselo lipereke mwana wangʼombe wamwamuna monga nsembe yopsereza kuti likhale fungo lokoma kwa Yehova pamodzinso ndi chopereka chachakudya ndi chopereka cha chakumwa ndi mbuzi yayimuna ngati nsembe yopepesera machimo potsata zimene zinalamulidwa.
25 Hagi pristi vahe'mo ama ana ofa nehanige'na, Israeli vahe'mokizmi kumizmia apasenezmantena kumizmia atrezmantegahue. Na'ankure zamagra kumi hugahune hu'za ontahi'neza hu'naza kumite Ra Anumzamonare'ma eme hanaza ofa hugahaze.
Wansembe apereke nsembe yopepesera machimo a gulu lonse la Aisraeli, ndipo adzakhululukidwa, pakuti linali tchimo lochita mosadziwa. Ndipo chifukwa cha tchimo lawolo, abweretse kwa Yehova nsembe yotentha pa moto ndi nsembe yopepesera machimo.
26 Ana hanagena mika Israeli vahe'ene ruregati tamagranema enemaniza vahe'mofo kumi'zmima apasezamantenu'a ofa hugahaze.
Gulu lonse la Aisraeli ndi alendo okhala pakati pawo adzakhululukidwa chifukwa anthu onsewo anachimwa mosadziwa.
27 Hagi mago'moma kumi hugahuema huno ontahineno mago'azama hanirega hantaga huno'ma hania kumitera, magoke ve meme anenta aheta kresramna vanageno,
“‘Koma ngati munthu mmodzi achimwa mosadziwa, ayenera kubweretsa mbuzi yayikazi ya chaka chimodzi kuti ikhale nsembe yopepesera machimo.
28 pristi ne'mo'a kumi'ma hu'nesia nemofonteku huno krenkena, kumi'a apasentegahue.
Wansembe apereke nsembe yopepesera machimowo pamaso pa Yehova chifukwa cha munthu yemwe anachimwa mosadziwayo. Nsembe yopepesera tchimo lakelo ikaperekedwa, munthuyo adzakhululukidwa.
29 Hagi ama'i tra kea maka Israeli vahe'motane rurega vahe'ma tamagranema enemaniza vahemo'zanena avaririgahaze.
Lamulo lomweli ligwiritsidwe ntchito kwa aliyense wochimwa mosadziwa, kaya ndi mbadwa ya mu Israeli kapena mlendo.
30 Hagi Israeli vahe'mo'o, rurega vahe'ma tamagranema emani'nenaza vahe'mo'za kumi'ma hanamo'za, Anumzamofo huhaviza hunteankna hugahazanki'za, Israeli vahepintira zamahe'natregahaze.
“‘Koma aliyense amene achimwa mwadala, kaya ndi mbadwa kapena mlendo, nachitira chipongwe Yehova, ameneyo achotsedwe ndithu pakati pa anthu ake.
31 Na'ankure anamo'a amefi hunamino agra'a avesite tra keni'a rufutagi'ne. Ana hu'negu Sabati tra ke rufutaginea kumimo'a agrite megahianki, anamofona ahe frigahaze.
Popeza wanyoza mawu a Yehova ndi kuphwanya malamulo ake. Munthu ameneyo achotsedwe ndithu, kuchimwa kwake kudzakhala pa iyeyo.’”
32 Israeli vahe'mo'za mago Sabati knarera ka'ma hagege kokampi mani'nazageno mago ne'mo'a teve'za nehige'za ke'naze.
Aisraeli ali mʼchipululu, munthu wina anapezeka akutola nkhuni tsiku la Sabata.
33 Ana nera azeri'za Mosesene Aronikiznire'ene mika Israeli vahete vu'naze.
Amene anamupeza akutola nkhunizo anabwera naye kwa Mose ndi Aaroni ndi kwa gulu lonse
34 Hagi ana ne'mofona nankna hazenke amigahaze ontahinazanki'za ana nera atrageno ovu'neanki kina huntazageno man'ine.
ndipo anamutsekera mʼndende chifukwa sankadziwa choti achite naye.
35 Hagi Ra Anumzamo'a amanage huno Mosesena asmi'ne, mika veara zamasmige'za kuma'mofona fegi'a avre'za vu'za have knonu ome ahe friho.
Pamenepo Yehova anawuza Mose kuti, “Munthu ameneyu ayenera kuphedwa. Gulu lonse liyenera kumugenda ndi miyala kunja kwa msasa.”
36 Ra Anumzamo'ma Mosesema asmia kante ante'za, ana nera avare'za seli no kumofona fegia vu'za haveknonu ome ahe fri'naze. Nofima kukenarema renentaza kasege.
Choncho gululo linamutengera kunja kwa msasa ndi kumupha pomugenda ndi miyala, monga momwe Yehova analamulira Mose.
37 Ra Anumzamo'a Mosesena amanage huno' asmi'ne,
Yehova anawuza Mose kuti,
38 Israeli vahera zamasmige'za kenazmimofo agentega nofira rente'za eviho. Hagi kukenamofo agentega haninke nofi rente'za evugahazanki anazana mika knafima henkama fore hu anante anante'ma hu'za vanaza vahe'mo'za kukenazmimofo atuparega rente'za evugahaze.
“Yankhula ndi Aisraeli ndipo uwawuze kuti, ‘Pa mibado yanu yonse muzisokerera mphonje pa ngodya za zovala zanu ndipo pa ngodya ya mphonje iliyonse azisokererapo chingwe chobiriwira.
39 Hagi ana nofi'ma negesuta Ra Anumzamo'nama tami'noa mika kasegegu tamagesa antahita nevaririta, tamagra'a tamavesizana avaririta havi tamavutamavara osugahaze.
Mudzakhala ndi mphonje zimenezi kuti mukaziona muzikakumbukira malamulo onse a Yehova ndi kuwamvera kuti musamatsatenso zilakolako za mʼmitima mwanu ndi za maso anu.
40 Hagi ana nofi'ma negesageno huramagesa nehina kasege'ni'ane naneke'ni'anena avaririta mani ruotge huta manigahaze.
Motero mudzakumbukira kumvera malamulo anga ndipo mudzakhala opatulikira a Mulungu wanu.
41 Nagra Ra Anumzamo'nama Isipiti'ma tamavre'na e'noana, tamagri Anumza maniku tamavre'na e'noa Anumza mani'noe.
Ine ndine Yehova Mulungu wanu, amene ndinakutulutsani mʼdziko la Igupto kuti ndikhale Mulungu wanu. Ine ndine Yehova Mulungu wanu.’”

< 4 Mose 15 >