< 詩篇 23 >

1 ヱホバは我が牧者なり われ乏しきことあらじ
Salimo la Davide. Yehova ndiye mʼbusa wanga, sindidzasowa kanthu.
2 ヱホバは我をみどりの野にふさせ いこひの水濱にともなひたまふ
Amandigoneka pa msipu wobiriwira, amanditsogolera ku madzi akumwa abwino,
3 ヱホバはわが霊魂をいかし名のゆゑをもて我をただしき路にみちびき給ふ
amatsitsimutsa moyo wanga. Amanditsogolera mʼnjira zachilungamo chifukwa cha dzina lake.
4 たとひわれ死のかげの谷をあゆむとも禍害をおそれじ なんぢ我とともに在せばなり なんぢの笞なんぢの杖われを慰む
Ngakhale ndiyende mʼchigwa cha mdima wakuda bii, sindidzaopa choyipa, pakuti Inu muli ndi ine; chibonga chanu ndi ndodo yanu zimanditonthoza.
5 なんぢわが仇のまへに我がために筵をまうけ わが首にあぶらをそそぎたまふ わが酒杯はあふるるなり
Mumandikonzera chakudya adani anga akuona. Mumadzoza mutu wanga ndi mafuta; chikho changa chimasefukira.
6 わが世にあらん限りはかならず恩惠と憐憫とわれにそひきたらん 我はとこしへにヱホバの宮にすまん
Zoonadi, zokoma ndi chikondi chosasinthika zidzanditsata masiku onse a moyo wanga, ndipo ndidzakhala mʼNyumba ya Yehova kwamuyaya.

< 詩篇 23 >