< 箴言 知恵の泉 9 >
Nzeru inamanga nyumba yake; inayimika nsanamira zake zisanu ndi ziwiri.
Inapha ziweto zake ndipo yasakaniza vinyo wake; inasakaniza vinyo wake ndi kuyala tebulo lake.
Nzeruyo inatuma adzakazi ake, kuti akakhale pamwamba penipeni pa mzinda ndi kukalengeza kuti,
“Aliyense amene ali munthu wamba, abwere kuno!” Kwa onse opanda nzeru inkanena kuti,
5 汝等きたりて我が糧を食ひ わがまぜあはせたる酒をのみ
“Bwerani, dzadyeni chakudya changa ndipo dzamweni vinyo amene ndakonza.
Lekani zopusa zanu kuti mukhale ndi moyo; yendani njira ya nzeru yomvetsa zinthu.”
7 嘲笑者をいましむる者は恥を己にえ 惡人を責むる者は疵を己にえん
Aliyense amene amayesa kukonza munthu wonyoza amadziputira minyozo; aliyense amene amadzudzula munthu woyipa amadetsa mbiri yake.
8 嘲笑者を責むることなかれ 恐くは彼なんぢを惡まん 智慧ある者をせめよ 彼なんぢを愛せん
Usadzudzule munthu wonyoza kuti angadzadane nawe; dzudzula munthu wanzeru ndipo adzakukonda.
9 智慧ある者に授けよ 彼はますます智慧をえん 義者を敎へよ 彼は知識に進まん
Ukalangiza munthu wanzeru ndiye adzapitirira kukhala wanzeru; ukaphunzitsa munthu wolungama ndiye adzawonjezera kuphunzira kwake.
10 ヱホバを畏るることは智慧の根本なり 聖者を知るは聰明なり
Kuopa Yehova ndiye chiyambi cha nzeru; kudziwa Woyerayo ndiko kukhala womvetsa bwino zinthu.
11 我により汝の日は多くせられ 汝のいのちの年は増べし
Chifukwa cha ine nzeru, masiku ako adzachuluka, ndipo zaka za moyo wako zidzawonjezeredwa.
12 汝もし智慧あらば自己のために智慧あるなり 汝もし嘲らば汝ひとり之を負ん
Ngati ndiwe wanzeru, nzeru yakoyo idzakupindulitsa; ngati ndiwe wonyoza ena, udzavutika wekha.
13 愚なる婦は嘩しく且つたなくして何事をも知らず
Uchitsiru ndi mkazi waphokoso, wopulikira ndiponso wosadziwa zinthu.
14 その家の門に坐し邑のたかき處にある座にすわり
Iye amakhala pa mpando, pa khomo la nyumba yake, pamalo aatali a mu mzinda,
kuti aziyitana anthu ongodutsa, amene akunka nayenda njira zawo.
16 拙者よここに來れと また智慧なき人にむかひては之にいふ
Amati, “Onse amene ndi anthu wamba abwere kuno,” ndipo kwa wopanda nzeru amati,
“Madzi akuba ndiye amatsekemera; chakudya chodya mobisa ndi chokoma!”
18 彼處にある者は死し者その客は陰府のふかき處にあることを是等の人は知らざるなり (Sheol )
Koma amunawo sadziwa kuti akufa ali kale komweko, ndi kuti alendo ake alowa kale mʼmanda akuya. (Sheol )