< 哀歌 3 >
Ine ndine munthu amene ndaona masautso ndi ndodo ya ukali wake.
2 かれは我をひきて黑暗をあゆませ光明にゆかしめたまはず
Wandipititsa kutali ndipo wandiyendetsa mu mdima osati mʼkuwala;
3 まことに屢々その手をむけて終日われを攻なやまし
zoonadi anandikantha ndi dzanja lake mobwerezabwereza tsiku lonse.
Wakalambitsa khungu langa ndi mnofu wanga, ndipo waphwanya mafupa anga.
5 われにむかひて患苦と艱難を築きこれをもて我を圍み
Wandizinga ndi kundizungulira ndi zowawa ndi zolemetsa.
Wandikhazika mu mdima ngati amene anafa kale.
7 我をかこみて出ること能はざらしめわが鏈索を重くしたまへり
Wandimangira khoma kotero kuti sindingathawe, wandimanga ndi maunyolo.
Ngakhale pamene ndifuwula kapena kupempha chithandizo, amakana pemphero langa.
9 斫たる石をもてわが道を塞ぎわが途をまげたまへり
Wanditsekera njira yanga ndi miyala yosema; ndipo wakhotetsa tinjira tanga.
10 その我に對することは伏て伺がふ熊のごとく潜みかくるる獅子のごとし
Wandidikirira ngati chimbalangondo, wandibisalira ngati mkango.
11 われに路を離れしめ 我をひきさきて獨くるしましめ
Wandikokera pambali ndi kundingʼambangʼamba, ndipo wandisiya wopanda thandizo.
Wakoka uta wake ndipo walunjikitsa mivi yake pa ine.
Walasa mtima wanga ndi mivi ya mʼphodo mwake.
14 われはわがすべての民のあざけりとなり 終日うたひそしらる
Ndinakhala choseketsa cha anthu anga onse; amandinyodola mʼnyimbo zawo tsiku lonse.
Wandidyetsa zowawa ndipo wandimwetsa ndulu.
16 小石をもてわが齒を摧き灰をもて我を蒙ひたまへり
Wathyola mano anga ndi miyala; wandiviviniza mʼfumbi;
17 なんぢわが靈魂をして平和を遠くはなれしめたまへば我は福祉をわすれたり
Wandichotsera mtendere; ndayiwala kuti kupeza bwino nʼchiyani.
18 是において我みづから言り わが氣力うせゆきぬ ヱホバより何を望むべきところ無しと
Choncho ndikuti, “Ulemerero wanga wachoka ndi zonse zimene ndimayembekeza kwa Yehova.”
19 ねがはくは我が艱難と苦楚茵蔯と膽汁とを心に記たまへ
Kukumbukira masautso anga ndi kusowa pokhala, zili ngati zowawa ndi ndulu.
20 わがたましひは今なほ是らの事を想ひてわが衷に鬱ぐ
Ine ndikuzikumbukira bwino izi, ndipo moyo wanga wathedwa mʼkati mwanga.
21 われこの事を心におもひ起せり この故に望をいだくなり
Komabe ndimakumbukira zimenezi, nʼchifukwa chake ndili ndi chiyembekezo.
22 われらの尚ほろびざるはヱホバの仁愛によりその憐憫の盡ざるに因る
Ife sitinawonongekeretu chifukwa chikondi cha Yehova ndi chachikulu, ndi chifundo chake ndi chosatha.
23 これは朝ごとに新なり なんぢの誠實はおほいなるかな
Zimaoneka zatsopano mmawa uliwonse; kukhulupirika kwanu nʼkwakukulu.
24 わが靈魂は言ふ ヱホバはわが分なり このゆゑに我彼を待ち望まん
Mu mtima mwanga ndimati, “Yehova ndiye zanga zonse; motero ndimamuyembekezera.”
25 ヱホバはおのれを待ち望む者とおのれを尋ねもとむる人に恩惠をほどこしたまふ
Yehova ndi wabwino kwa amene amayembekezera Iye, kwa munthu amene amafunafuna Iyeyo;
nʼkwabwino kudikira chipulumutso cha Yehova modekha.
Nʼkwabwino kuti munthu asenze goli pamene ali wamngʼono.
28 ヱホバこれを負せたまふなれば獨坐して默すべし
Akhale chete pa yekha, chifukwa Yehova wamusenzetsa golilo.
Abise nkhope yake mʼfumbi mwina chiyembekezo nʼkukhalapobe.
30 おのれを撃つ者に頬をむけ 充足れるまでに恥辱をうけよ
Apereke tsaya lake kwa iye amene angamumenye, ndipo amuchititse manyazi.
31 そは主は永久に棄ることを爲たまはざるべければなり
Chifukwa Ambuye satayiratu anthu nthawi zonse.
32 かれは患難を與へ給ふといへどもその慈悲おほいなればまた憐憫を加へたまふなり
Ngakhale amabweretsa zowawa, Iye adzawachitira chifundo, chifukwa chikondi chake ndi chosatha.
33 心より世の人をなやましかつ苦しめ給ふにはあらざるなり
Pakuti sabweretsa masautso mwadala, kapena zowawa kwa ana a anthu.
Kuphwanya ndi phazi a mʼndende onse a mʼdziko,
kukaniza munthu ufulu wake pamaso pa Wammwambamwamba,
36 人の詞訟を屈むることは主のよろこび給はざるところなり
kumana munthu chiweruzo cholungama— kodi Ambuye saona zonsezi?
37 主の命じたまふにあらずば誰か事を述んにその事即ち成んや
Kodi ndani angayankhule zinthu nʼkuchitika ngati Ambuye sanavomereze?
Kodi zovuta ndi zabwino sizituluka mʼkamwa mwa Wammwambamwamba?
39 活る人なんぞ怨言べけんや 人おのれの罪の罰せらるるをつぶやくべけんや
Kodi nʼchifukwa chiyani munthu aliyense wamoyo amadandaula akalangidwa chifukwa cha machimo ake?
40 我等みづからの行をしらべかつ省みてヱホバに歸るべし
Tiyeni tisanthule ndi kuyesa njira zathu, ndipo tiyeni tibwerere kwa Yehova.
41 我ら天にいます神にむかひて手とともに心をも擧べし
Tiyeni tikweze mitima yathu ndi manja athu kwa Mulungu kumwamba ndipo tinene kuti:
42 われらは罪ををかし我らは叛きたり なんぢこれを赦したまはざりき
“Ife tachimwa ndi kuwukira ndipo inu simunakhululuke.
43 なんぢ震怒をもてみづから蔽ひ 我らを追攻め殺してあはれまず
“Mwadzikuta ndi mkwiyo ndi kutilondola ndipo mwatitha mopanda chifundo.
44 雲をもてみづから蔽ひ 祈禱をして通ぜざらしめ
Mwadzikuta mu mtambo kotero mapemphero athu sakukufikani.
45 もろもろの民の中にわれらを塵埃となしたまへり
Mwatisandutsa zinyatsi ndi zinyalala pakati pa mitundu ya anthu.
“Adani anthu atitsekulira pakamwa.
Ife tadzazidwa ndi mantha pakuti tagwa mʼdzenje, tapasuka ndi kuwonongedwa.”
48 わが民の女の滅亡によりてわが眼には涙の河ながる
Misozi mʼmaso mwanga ikungoti mbwembwembwe chifukwa anthu anga akuwonongedwa.
Misozi idzatsika kosalekeza, ndipo sidzasiya,
50 天よりヱホバの臨み見て顧みたまふ時にまで至らん
mpaka Yehova ayangʼane pansi kuchokera kumwamba ndi kuona.
51 わが邑の一切の女等の故によりてわが眼はわが心をいたましむ
Mtima wanga ukupweteka poona zimenezi chifukwa cha akazi onse a mu mzinda.
52 故なくして我に敵する者ども鳥を追ごとくにいたく我をおひ
Akundisaka ngati mbalame, amene anali adani anga, popanda chifukwa.
53 わが生命を坑の中にほろぼし わが上に石を投かけ
Ayesa kundipha pondiponya mʼdzenje ndi kundiponya miyala;
54 また水わが頭の上に溢る 我みづから言り滅びうせぬと
madzi anamiza mutu wanga ndipo ndinkaganiza kuti imfa yayandikira.
Ndinayitana dzina lanu Inu Yehova, kuchokera mʼdzenje lozama.
56 なんぢ我が聲を聽たまへり わが哀歎と祈求に耳をおほひたまふなかれ
Inu munamva kudandaula kwanga. “Mundimvere kulira kwanga kopempha thandizo.”
57 わが汝を龥たりし時なんぢは近よりたまひて恐るるなかれと宣へり
Munafika pafupi pamene ndinakuyitanani, ndipo munati, “Usaope.”
58 主よなんぢはわが靈魂の訴を助け伸べ わが生命を贖ひ給へり
Inu Ambuye munandiwombola ku mlandu wanga; munapulumutsa moyo wanga.
59 ヱホバよ なんぢは我がかうむりたる不義を見たまへり 願はくは我に正しき審判を與へたまへ
Yehova, mwaona zoyipa zimene andichitira. Mundiweruzire ndinu!
60 なんぢは彼らが我を怨み われを害せんとはかるを凡て見たまへり
Mwaona kuzama kwa kubwezera kwawo, chiwembu chawo chonse pa ine.
61 ヱホバよなんぢは彼らが我を詈り 我を害せんとはかるを凡て聞たまへり
Inu Yehova mwamva kunyoza kwawo, chiwembu chawo chonse pa ine,
62 かの立て我に逆らふ者等の言語およびその終日われを攻んとて運らす謀計もまた汝これを聞たまへり
manongʼonongʼo a adani anga ondiwukira ine tsiku lonse.
63 ねがはくは彼らの起居をかんがみたまへ 我はかれらに歌ひそしらる
Tawaonani! Kaya ali pansi kapena kuyimirira, akundinyoza mu nyimbo zawo.
64 ヱホバよ なんぢは彼らが手に爲すところに循がひて報をなし
Inu Yehova, muwabwezere chowayenera, chifukwa cha zimene manja awo achita.
65 かれらをして心くらからしめたまはん なんぢの呪詛かれらに歸せよ
Phimbani mitima yawo, ndipo matemberero anu akhale pa iwo!
66 なんぢは震怒をもてかれらを追ひ ヱホバの天の下よりかれらをほろぼし絶たまはん
Muwalondole mwaukali ndipo muwawonongeretu pa dziko lapansi.