< ヨブ 記 17 >
1 わが氣息は已にくさり 我日すでに盡なんとし墳墓われを待つ
“Mtima wanga wasweka, masiku anga atha, manda akundidikira.
2 まことに嘲弄者等わが傍に在り 我目は彼らの辨爭ふを常に見ざるを得ず
Ndithudi, anthu ondiseka andizungulira; maso anga akupenyetsetsa mdani wanga.
3 願くは質を賜ふて汝みづから我の保證となりたまへ 誰か他にわが手をうつ者あらんや
“Inu Mulungu, patseni chikole chimene mukufuna. Ndani wina amene adzandiperekera ine chikole?
4 汝彼らの心を閉て悟るところ無らしめたまへり 必ず彼らをして愈らしめたまはじ
Inu mwatseka maganizo awo kuti asamvetse zinthu; choncho simudzawalola kuti apambane.
5 朋友を交付して掠奪に遭しむる者は其子等の目潰るべし
Ngati munthu apereka mnzake chifukwa cha chuma, ana ake sadzaona mwayi.
6 彼われを世の民の笑柄とならしめたまふ 我は面に唾せらるべき者となれり
“Mulungu wandisandutsa chisudzo chochiseka aliyense, munthu amene anthu amalavulira malovu nkhope yake.
7 かつまた我目は憂愁によりて昏み 肢體は凡て影のごとし
Mʼmaso mwanga mwada ndi chisoni; ndawonda ndi mutu womwe.
8 義しき者は之に驚き 無辜者は邪曲なる者を見て憤ほる
Anthu olungama akudabwa nazo zimenezi; anthu osachimwa akupsera mtima anthu osapembedza Mulungu.
9 然ながら義しき者はその道を堅く持ち 手の潔淨き者はますます力を得るなり
Komabe anthu olungama adzasunga njira zawo, ndipo anthu a makhalidwe abwino mphamvu zawo zidzanka zikuchuluka.
10 請ふ汝ら皆ふたたび來れ 我は汝らの中に一人も智き者あるを見ざるなり
“Tsono bwerani nonsenu, bwerezaninso mawu anuwo, sindidzapezapo munthu wanzeru pakati panupo.
11 わが日は已に過ぎ わが計る所わが心に冀ふ所は已に敗れたり
Masiku anga atha, zimene ndinakonza zalephereka, pamodzinso ndi zokhumba za mtima wanga.
Anthu awa amasandutsa usiku kukhala usana, nthawi ya usiku iwo amati ‘kwatsala pangʼono kucha.’
13 我もし俟つところ有ば是わが家たるべき陰府なるのみ 我は黑暗にわが牀を展ぶ (Sheol )
Ngati nyumba imene ndikuyiyembekezera ndi manda, ngati ndiyala bedi langa mu mdima, (Sheol )
14 われ朽腐に向ひては汝はわが父なりと言ひ 蛆に向ひては汝は我母わが姉妹なりと言ふ
ngati ndinena kwa dzenje la manda ‘ndinu abambo anga,’ ndiponso kwa mphutsi kuti, ‘ndinu amayi anga’ kapena ‘mlongo wanga,’
15 然ばわが望はいづくにかある 我望は誰かこれを見る者あらん
tsono chiyembekezo changa chili kuti? Ndani angaone populumukira panga?
16 是は下りて陰府の關に到らん 之と齊しく我身は塵の中に臥靜まるべし (Sheol )
Ndithu sindidzakhalanso ndi chiyembekezo chilichonse, polowa mʼmanda, pamene ndidzatsikira ku fumbi.” (Sheol )