< Salmi 67 >

1 Per il Capo de’ musici. Per strumenti a corda. Salmo. Canto. Iddio abbia mercé di noi, e ci benedica, Iddio faccia risplendere il suo volto su noi; (Sela)
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Salimo. Yehova atikomere mtima ndi kutidalitsa, achititse kuti nkhope yake itiwalire.
2 affinché la tua via sia conosciuta sulla terra, e la tua salvezza fra tutte le genti.
Kuti njira zanu zidziwike pa dziko lapansi, chipulumutso chanu pakati pa mitundu yonse.
3 Ti celebrino i popoli, o Dio, tutti quanti i popoli ti celebrino!
Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu; mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.
4 Le nazioni si rallegrino e giubilino, perché tu giudichi i popoli con equità, e sei la guida delle nazioni sulla terra. (Sela)
Mitundu yonse ya anthu isangalale ndi kuyimba mwachimwemwe, pakuti inu mumaweruza mitundu ya anthu mwachilungamo ndi kutsogolera mitundu ya anthu a dziko lapansi.
5 Ti celebrino i popoli, o Dio, tutti quanti i popoli ti celebrino!
Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu; mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.
6 La terra ha prodotto il suo frutto; Dio, l’Iddio nostro, ci benedirà.
Nthaka yabereka zokolola zake; tidalitseni Mulungu wathu.
7 Iddio ci benedirà, e tutte le estremità della terra lo temeranno.
Mulungu atidalitse kuti pamenepo malekezero onse a dziko lapansi apembedze Iyeyo.

< Salmi 67 >