< Salmi 6 >

1 Salmo di Davide, [dato] al Capo de' Musici, in Neghinot, sopra Seminit SIGNORE, non correggermi nella tua ira, E non gastigarmi nel tuo cruccio.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Molingana ndi seminiti. Salimo la Davide. Inu Yehova, musandidzudzule mu mkwiyo wanu, kapena kundilanga mu ukali wanu.
2 Abbi pietà di me, o Signore; perciocchè io [son] tutto fiacco; Sanami, Signore; perciocchè le mie ossa son tutte smarrite.
Ndichitireni chifundo Inu Yehova, pakuti ndalefuka; Inu Yehova chiritseni, pakuti mafupa anga ali pa ululu waukulu.
3 L'anima mia eziandio è grandemente smarrita; E tu, Signore, infino a quando?
Moyo wanga uli pa mazunzo aakulu. Mpaka liti, Inu Yehova, mpaka liti?
4 Rivolgiti, o Signore; riscuoti l'anima mia; Salvami, per amor della tua benignità.
Tembenukani Inu Yehova, ndipo mundilanditse; pulumutseni chifukwa cha chikondi chanu chosasinthika.
5 Perciocchè nella morte non [v'è] memoria di te; Chi ti celebrerà nel sepolcro? (Sheol h7585)
Palibe amene amakukumbukirani pamene wamwalira; Amakutamandani ndani ali ku manda? (Sheol h7585)
6 Io mi affanno ne' miei sospiri; Io allago tutta notte il mio letto, E bagno la mia lettiera colle mie lagrime.
Ine ndatopa ndi kubuwula; usiku wonse pa bedi panga pamadzaza ndi misozi yanga; ndimanyowetsa pogona panga ndi misozi.
7 L' occhio mio è consumato di fastidio; Egli è invecchiato per cagione di tutti i miei nemici.
Maso anga atupa chifukwa cha chisoni; akulephera kuona chifukwa cha adani anga.
8 Ritraetevi da me, [voi] tutti operatori d'iniquità; Perciocchè il Signore ha udita la voce del mio pianto.
Chokani kwa ine inu nonse amene mumachita zoyipa, pakuti Yehova wamva kulira kwanga.
9 Il Signore ha udita la mia supplicazione; Il Signore ha accettata la mia orazione.
Yehova wamva kupempha kwanga kofuna chifundo; Yehova walandira pemphero langa.
10 Tutti i miei nemici sieno confusi, e grandemente smarriti; Voltin le spalle, e sieno svergognati in un momento.
Adani anga onse adzachita manyazi ndipo adzakhala ndi mantha; adzabwerera msangamsanga mwa manyazi.

< Salmi 6 >