< Dagiti Salmo 95 >

1 Umaykayo ket kantaantayo ni Yahweh; kantaantayo a sirarag-o ti bato ti pannakaisalakantayo.
Bwerani, tiyeni timuyimbire Yehova mwachimwemwe, tiyeni tifuwule kwa Thanthwe la chipulumutso chathu
2 Sumrektayo iti ayanna nga addaan iti panagyaman; kantaantayo isuna kadagiti salmo a pagdayaw.
Tiyeni tibwere pamaso pake ndi chiyamiko ndipo mupembedzeni Iyeyo ndi zida zoyimbira ndi nyimbo.
3 Ta naindaklan ni Yahweh a Dios ken naindaklan nga Ari a kangatoan kadagiti amin a dios.
Pakuti Yehova ndi Mulungu wamkulu, mfumu yayikulu pamwamba pa milungu yonse.
4 Adda iti imana dagiti uneg ti daga, kukuana ti ngato dagiti banbantay.
Mʼmanja mwake muli maziko ozama a dziko lapansi, ndipo msonga za mapiri ndi zake.
5 Kukuana ti taaw, ta inaramidna daytoy, ken sinukog dagiti imana ti namaga a daga.
Nyanja ndi yake, pakuti anayilenga ndi Iye, ndipo manja ake anawumba mtunda wowuma.
6 Umaykayo, agrukbabtayo ken agkurnotayo; agparintumengtayo iti sangoanan ni Yahweh a namarsuatayo:
Bwerani, tiyeni tiwerame pomulambira, tiyeni tigwade pamaso pa Yehova Mlengi wathu;
7 Ta isuna ti Diostayo, ken datayo dagiti tattao iti pagarabanna ken dagiti karnero nga ay-aywananna. Ita, sapay koma ta mangngegyo ti timekna!
pakuti Iye ndiye Mulungu wathu ndipo ife ndife anthu a pabusa pake, ndi nkhosa za mʼdzanja lake. Lero ngati inu mumva mawu ake,
8 Saanyo a patangkenen dagiti pusoyo, a kas idiay Meriba, wenno kas iti aldaw ti Masa idiay let-ang,
musawumitse mitima yanu monga momwe munachitira pa Meriba, monga munachitira tsiku lija pa Masa mʼchipululu.
9 a nangkaritan dagiti kapuonanyo ti turayko ken pinadasda ti anusko, uray no nakitada dagiti aramidko.
Kumene makolo anu anandiyesa ndi kundiputa, ngakhale anaona zimene Ine ndinazichita.
10 Iti uppat a pulo a tawen, nakapungtotak iti dayta a henerasion ket kinunak, 'Daytoy ket tattao nga agalla-alla ti panagpuspusoda, saanda a binigbig dagiti wagasko.'
Kwa zaka makumi anayi ndinali wokwiya ndi mʼbado umenewo; ndipo ndinati, “Iwo ndi anthu amene mitima yawo imasochera ndipo sanadziwe njira zanga.”
11 Ngarud, nagkariak gapu iti ungetko a saandanto a pulos a makastrek iti lugar a paginanaak.”
Choncho ndili chikwiyire, ndinalumbira kuti, “Iwowa sadzalowa ku malo anga a mpumulo.”

< Dagiti Salmo 95 >