< Dagiti Salmo 90 >
1 O Apo, sika ti kamangmi kadagiti amin a henerasion.
Pemphero la Mose munthu wa Mulungu. Ambuye, mwakhala muli malo athu okhalamo pa mibado yonse.
2 Sakbay a naparsua dagiti banbantay, wenno pinarsuam ti daga ken ti lubong, ti agnanayon nga awan inggana, sika ti Dios.
Mapiri asanabadwe, musanalenge nʼkomwe dziko lapansi ndi dziko lonse, kuyambira muyaya mpaka muyaya Inu ndinu Mulungu.
3 Isublim ti tao iti tapok, ket kunaem, “Agsublikayo, dakayo a kaputotan ti sangkataoan”
Inu mumabwezera anthu ku fumbi, mumati, “Bwerera ku fumbi iwe mwana wa munthu.”
4 Ta iti rinibu a tawen iti panagkitam ket kasla laeng idi kalman no lumabas, ken kasla iti panagbantay iti rabii.
Pakuti zaka 1,000 pamaso panu zili ngati tsiku limene lapita kapena ngati kamphindi ka usiku.
5 Iyanudmo ida a kas iti panangiyanod iti layus ket maturogda; Iti agsapa, kasla da la ruot nga agtubo.
Inu mumasesa anthu mʼtulo ta imfa, iwo ali ngati udzu watsopano wa mmawa,
6 Iti agsapa, lumangto ken dumakkel daytoy; iti rabii, malaylay ken magango daytoy.
ngakhale kuti mmawa umaphuka watsopano, pofika madzulo wauma ndi kufota.
7 Pudno a maibuskami iti ungetmo, ken mabutengkami iti pungtotmo.
Ife tathedwa ndi mkwiyo wanu; ndipo taopsezedwa ndi kuyipidwa kwanu.
8 Ingkabilmo iti sangoanam dagiti nagkuranganmi, iti lawag ti imatangmo dagiti nakalemmeng a basbasolmi.
Mwayika mphulupulu zathu pamaso panu, machimo athu obisika poonekera pamaso panu.
9 Mapukaw ti biagmi babaen ti pungtotmo; sipapardas nga aglabas dagiti tawenmi a kasla iti sennaay.
Masiku athu onse amatha ali pansi pa ukali wanu; timatsiriza zaka zathu ndi kubuwula.
10 Pitopulo a tawen iti panagbiagmi, wenno walo pulo pay no nasalun-atkami; ngem uray pay dagiti kasasayaatan a tawtawenmi ket namarkaan iti riribuk ken ladingit. Wen, lumabasda a sipapardas, ket mapukawkami.
Kuchuluka kwa masiku athu ndi 70, kapena 80 ngati tili ndi mphamvu; komabe zaka zonsezi ndi za mavuto ndi nkhawa, zimatha mofulumira ndipo ife timawulukira kutali.
11 Siasino ti makaammo ti kabara ti ungetmo; maipada ti pungtotmo iti buteng a pabpabilgenna?
Kodi ndani amadziwa mphamvu ya mkwiyo wanu? Pakuti ukali wanu ndi waukulu ngati ulemu umene uyenera Inu.
12 Isu nga isuronakami a mangbilang ti biagmi tapno makapagbiagkami a sisisirib.
Tiphunzitseni kuwerenga masiku athu molondola, kuti tikhale ndi mtima wanzeru.
13 Tumaliawka, O Yahweh! Kasano pay ti kabayagna daytoy? Kaassiam dagiti adipenmo.
Lezani mtima Inu Yehova! Kodi mudzatikwiyira mpaka liti? Achitireni chifundo atumiki anu.
14 Pennekennakami iti kinapudnom iti tulagmo iti agsapa, tapno mabalinmi ti agrag-o ken agragsak kadagiti amin nga al-aldawmi.
Mutikhutitse mmawa ndi chikondi chanu chosatha, kuti tiyimbe ndi chimwemwe ndi kukhala okondwa masiku athu onse.
15 Paragsakennakami iti mamin-adu a kas iti kaadu dagiti al-aldaw a pinagsagabanakami ken kadagiti tawtawen a nagdalankami iti riribuk.
Tisangalatseni masiku ambiri monga masiku amene mwatisautsa, kwa zaka zambiri monga momwe tinaonera mavuto.
16 Bay-am a makita dagiti adipenmo ti aramidmo, ken bay-am a makita dagiti annakmi ti kinatan-okmo.
Ntchito zanu zionetsedwe kwa atumiki anu, kukongola kwanu kwa ana awo.
17 Maawattayo koma ti parabur ti Apo a Diostayo; parang-ayenna ti aramid dagiti imatayo; pudno unay, parang-ayenna ti aramid dagiti imatayo.
Kukoma mtima kwa Ambuye Mulungu wathu kukhale pa ife; tikhazikitsireni ntchito ya manja athu; inde, khazikitsani ntchito ya manja athu.