< Dagiti Salmo 80 >

1 Ipangagnakami, O Pastor iti Israel, sika a mangidadaulo kenni Jose a kasla maysa nga arban; sika nga agtugtugaw iti rabaw ti kerubim, agranniagka kadakami!
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Kakombo wa Pangano.” Salimo la Asafu. Tcherani khutu Inu mʼbusa wa Israeli, Inu amene mumatsogolera Yosefe monga nkhosa; Inu amene mumakhala pa mpando waufumu pakati pa akerubi, walani
2 Iti imatang ni Efraim, Benjamin ken Manases, pagtignayem ti pannakabalinmo; umayka ket isalakannakami.
kwa Efereimu, Benjamini ndi Manase. Utsani mphamvu yanu; bwerani ndi kutipulumutsa.
3 O Dios, pabaroennakami; pagranniagem ti rupam kadakami, ket maisalakankami.
Tibwezereni mwakale Inu Mulungu; nkhope yanu itiwalire kuti tipulumutsidwe.
4 Yahweh a Dios a Mannakabalin amin, kasano kabayag a makaungetka kadagiti tattaom no agkararagda?
Inu Mulungu Wamphamvuzonse, mpaka liti mkwiyo wanu udzanyeka kutsutsana ndi mapemphero a anthu anu?
5 Pinakanmo ida iti tinapay ti lulua ken inikkam ida iti adu a lulua nga inumenda.
Mwawadyetsa buledi wa misozi; mwachitisa iwo kumwa misozi yodzaza mbale.
6 Inaramidnakami a pagsusupiatan dagiti kaarrubami ket pagkakatawaandakami dagiti kabusormi.
Mwachititsa kuti tikhale gwero la mikangano pakati pa anansi athu, ndipo adani athu akutinyoza.
7 O Dios a Mannakabalin amin, pabaroennakami, Pagraniagem ti rupam kadakami ket maisalakankami.
Tibwezereni mwakale Inu Mulungu Wamphamvuzonse, nkhope yanu itiwalire kuti tipulumutsidwe.
8 Nangiruarka ti lanut manipud idiay Egipto; pinapanawmo dagiti nasion ken immulam daytoy.
Munatulutsa mpesa kuchoka ku Igupto; munathamangitsa anthu a mitundu ina ndi kuwudzala mpesawo.
9 Winaknitam ti daga a maipaay iti daytoy; rimmamut ken pinunnona iti daga.
Munawulimira munda wamphesawo, ndipo unamera ndi kudzaza dziko.
10 Naabbungan dagiti bantay iti linongna, dagiti kangatoan a sedro ti Dios kadagiti sangana.
Mapiri anaphimbidwa ndi mthunzi wake, mikungudza yamphamvu ndi nthambi zake.
11 Dimmanon dagiti sangana agingga iti taaw ken nagsaringit agingga iti Karayan Euphrates.
Unatambalitsa nthambi zake mpaka ku nyanja, mphukira zake mpaka ku mtsinje.
12 Apay a rinebbam dagiti paderna tapno dagiti amin a lumabas ket agpuros iti bungana.
Chifukwa chiyani mwagwetsa makoma ake kuti onse amene akudutsa athyole mphesa zake?
13 Dadaelen daytoy dagiti alingo iti kabakiran ken kanen daytoy dagiti narungsot nga ayup iti taltalon.
Nguluwe zochokera mʼnkhalango zikuwononga ndipo zirombo za mthengo zimawudya.
14 Tumalliawka, O Dios a Mannakabalin amin; tumannawagka manipud langit ket kitaennakami ken aywanam daytoy a lanut.
Bweraninso kwa ife Inu Mulungu Wamphamvuzonse! Yangʼanani pansi muli kumwambako ndipo muone! Uyangʼanireni mpesa umenewu,
15 Daytoy ti ramut nga immula ti makannawan nga imam, ti saringit a pinatubom.
muzu umene dzanja lanu lamanja ladzala, mwana amene inu munamukuza nokha.
16 Napuoran ken napukan daytoy; mapukaw koma dagiti kabusormo gapu iti panangbabalawmo.
Mpesa wanu wadulidwa ndi kutenthedwa ndi moto; pakudzudzula kwanu anthu anu awonongeka.
17 Adda koma ti imam iti tao nga adda iti makannawan nga imam, iti anak ti tao a pinapigsam para kenka.
Dzanja lanu likhale pa munthu amene ali ku dzanja lanu lamanja, mwana wa munthu amene mwalera nokha.
18 Ket saankaminto a tumallikod kenka; papigsaennakami ket awaganminto iti naganmo.
Ndipo ife sitidzatembenukira kumbali kuchoka kwa Inu; titsitsimutseni ndipo tidzayitana pa dzina lanu.
19 Pabaroennakami, O Yahweh, Dios a Mannakabalin amin, agraniagka kadakami ket maisalakankami.
Tibwezereni mwakale Inu Yehova Mulungu Wamphamvuzonse nkhope yanu itiwalire kuti tipulumutsidwe.

< Dagiti Salmo 80 >