< Dagiti Salmo 74 >

1 Apay nga agnanayon nga inlaksidnakami, O Dios? Apay a gumil-ayab ti pungtotmo maibusor iti karnero iti pagpaspasturam?
Ndakatulo ya Asafu. Nʼchifukwa chiyani mwatitaya ife kwamuyaya, Inu Mulungu? Chifukwa chiyani mkwiyo wanu ukutukutira pa nkhosa za busa lanu?
2 Lagipem dagiti tattaom, a pinilim idi un-unana a tiempo, a sinubbotmo nga agbalin a tawidmo, ken ti Bantay Sion a pagnanaedam.
Kumbukirani anthu amene munawagula kalekale, fuko la cholowa chanu, limene Inu munaliwombola, phiri la Ziyoni, kumene inuyo mumakhala.
3 Umaymo kitaen dagiti naan-anay a nadadael, amin a panangpirdi nga inaramid dagiti kabusor iti nasantoan a disso.
Tembenuzani mapazi kuloza ku mabwinja awa amuyaya chiwonongeko ichi chonse mdani wabweretsa pa malo opatulika.
4 Nagriyaw dagiti kabusormo iti tengnga ti pinilim a lugar; inkabilda dagiti banderada a pakigubat.
Adani anu anabangula pa malo pamene Inu munkakumana nafe; anayimika mbendera zawo monga zizindikiro zachigonjetso.
5 Arigda la dagiti agpukpukan iti kayo iti kabakiran.
Iwo anachita ngati anthu oti anyamula mbendera zawo kuti adule mitengo mʼnkhalango.
6 Minaso ken binurakda dagiti amin nakitikitan; binurakda dagitoy babaen kadagiti wasay ken maso.
Kenaka anaphwanya ndi nkhwangwa ndi akasemasema awo zonse zimene tinapachika.
7 Pinuoranda ti templom, tinulawanda ti pagnanaedam, renebbada daytoy.
Iwo anatentha malo anu opatulika mpaka kuwagwetsa pansi; anadetsa malo okhalamo dzina lanu.
8 Kinunada iti puspusoda, “Dadaelentayo amin dagitoy.” Pinuoranda amin a kukuam a disso a paguummongan iti dayta a lugar.
Ndipo anati mʼmitima yawo, “Tawatha kwathunthu.” Anatentha malo aliwonse amene Mulungu amapembedzedwerako mʼdzikomo.
9 Awanen ti makitami a nakaskasdaaw a pagilasinan manipud iti Dios; awanen iti profeta, ken awanen ti makaammo kadakami no kaano nga agpatingga daytoy.
Ife sitinapatsidwe chizindikiro chodabwitsa; palibe aneneri amene atsala ndipo palibe aliyense wa ife akudziwa kuti izi zidzatenga nthawi yayitali bwanji.
10 Kasano kapaut, O Dios, ti pananglalais ti kabusor kenka? Agnanayonto kadi a tabtabbaawan dagiti kabusor ti naganmo?
Kodi mpaka liti, mdani adzanyoze Inu Mulungu? Kodi amaliwongowa adzapeputsa dzina lanu kwamuyaya?
11 Apay a gawgawidam ti imam, ti makannawan nga imam? Iruarmo ti makannawan nga imam manipud iti pagan-anaymo ket dadaelem ida.
Chifukwa chiyani mukubweza dzanja lanu lamanja? Litulutseni kuchoka pachifuwa chanu ndipo muwawononge!
12 Nupay kasta, ti Dios isun ti arik sipu pay idi un-unana, a mangiyeg ti pannakaisalakan iti daga.
Koma Inu Mulungu, ndinu Mfumu yanga kuyambira kalekale; Mumabweretsa chipulumutso pa dziko lapansi.
13 Babaen iti bilegmo, ginuduam ti baybay, binurakmo dagiti ulo dagiti nakabutbuteng nga ayup ti baybay, nga adda iti uneg ti danum.
Ndinu amene munagawa nyanja ndi mphamvu yanu; munathyola mitu ya zirombo za mʼmadzi.
14 Rinumekmo dagiti ulo ti leviatan; impakanmo isuna kadagiti agnanaed iti let-ang.
Ndinu amene munaphwanya mitu ya Leviyatani ndi kuyipereka ngati chakudya cha zirombo za mʼchipululu.
15 Linukatam dagiti ubbog ken dagiti waig; pinagmagam dagiti agay-ayus a karayan.
Ndinu amene munatsekula akasupe ndi mitsinje, munawumitsa mitsinje imene siphwa nthawi zonse.
16 Kukuam ti aldaw, ken kukuam pay ti rabii; inkabilmo ti init ken bulan iti umiso a pagiananda.
Masana ndi anu ndipo usiku ndi wanunso; Inuyo munakhazikitsa dzuwa ndi mwezi.
17 Inkabilmo dagiti beddeng ti daga; inaramidmo ti tiempo ti pudot ken lam-ek.
Ndinu amene munakhazikitsa malire onse a dziko lapansi; munakhazikitsa chilimwe ndi dzinja.
18 Lagipem no kasano iti panangisawang ti kabusor iti makapasakit a sasao kenka, O Yahweh, ken tinabbaawan dagiti maag a tao iti naganmo.
Kumbukirani momwe mdani wakunyozerani Inu Yehova, momwe anthu opusa apeputsira dzina lanu.
19 Saanmo nga iyawat ti biag ti kalapatim iti atap nga ayup. Ti biag dagiti tattaom a naidadanes, saanmo a liplipatan iti agnanayon.
Musapereke moyo wa nkhunda yanu ku zirombo zakuthengo; nthawi zonse musayiwale miyoyo ya anthu anu osautsidwa.
20 Lagipem ti tulagmo, ta dagiti nasipnget a rehion iti daga ket napnoan kadagiti lugar ti kinaranggas.
Mukumbukire pangano lanu, pakuti malo obisika a mʼdziko asanduka mochitira zachiwawa zochuluka.
21 Saanmo nga ipalubos a maibabain dagiti naidadanes; idaydayaw koma dagiti nakurapay ken naidadanes ti naganmo.
Musalole kuti osautsidwa abwerere mwamanyazi; osauka ndi osowa atamande dzina lanu.
22 Tumakderka, O Dios; ikalintegam ti dayawmo; lagipem ti agmalmalem a pananglalais dagiti maag kenka.
Dzukani Inu Mulungu ndipo dzitetezeni pa mlandu; kumbukirani momwe opusa akukunyozerani tsiku lonse.
23 Saanmo a liplipatan ti timek dagiti kabusormo wenno ti panagririyaw dagiti saan nga agsarsardeng a mangkarkarit kenka.
Musalekerere phokoso la otsutsana nanu, chiwawa cha adani anu, chimene chikumveka kosalekeza.

< Dagiti Salmo 74 >