< Dagiti Salmo 64 >
1 O Dios, denggem ti timekko, denggem daytoy ararawko; annadam daytoy biagko iti panagbutengko kadagiti kabusorko.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Ndimvereni Mulungu pomwe ndikunena madandawulo anga; tetezani moyo wanga ku chiopsezo cha mdani.
2 Ilimmengnak iti nalimed a panagplano dagiti managdakdakes, manipud iti ringgor dagiti managbasol.
Ndibiseni ku chiwembu cha anthu oyipa, ku gulu laphokoso la anthu ochita zoyipa.
3 Pinatademda dagiti dilada a kasla kampilan; dagiti napapait a sasaoda, kasla pana nga imbiatda
Iwo amanola malilime awo ngati malupanga, amaponya mawu awo olasa ngati mivi.
4 tapno mapanada ti awan basbasolna manipud iti nalimed a lugar; kellaat a panaenda isuna ket awan pagbutnganda.
Iwo amaponya mivi yawo ali pa malo wobisala kwa munthu wosalakwa; amamulasa modzidzimutsa ndi mopanda mantha.
5 Allukoyenda dagiti babbagida iti dakes a panggep; agtutulagda iti nalimed tapno mangisagana kadagiti palab-og; kunada, “Siasino ngay ti makakita kadatayo?”
Iwo amalimbikitsana wina ndi mnzake pa chikonzero chawo choyipa, amayankhula zobisa misampha yawo; ndipo amati, “Adzayiona ndani?”
6 Agaramidda kadagiti dakes a panggep; “Nalpastayon,” kunada, “ti naannad a plano.” Nauneg ti kaunggan a panunot ken puso ti tao.
Iwo amakonzekera zosalungama ndipo amati, “Takonza ndondomeko yabwino kwambiri!” Ndithu maganizo ndi mtima wa munthu ndi zachinyengo.
7 Ngem panaen ida ti Dios; ket kellaat a masugatanda babaen kadagiti panana.
Koma Mulungu adzawalasa ndi mivi; mwadzidzidzi adzakanthidwa.
8 Maitibkoldanto, agsipud ta maibusor kadakuada dagiti dilada; agwingiwingto amin dagiti makakita kadakuada.
Iye adzatembenuza milomo yawoyo kuwatsutsa ndi kuwasandutsa bwinja; onse amene adzawaona adzagwedeza mitu yawo mowanyoza.
9 Agbutengto dagiti amin a tattao ket ipadamagdanto dagiti inaramid ti Dios. Sisisiribdanto a mangpanunot iti inaramidna.
Anthu onse adzachita mantha; adzalengeza ntchito za Mulungu ndi kulingalira mozama zomwe Iye wazichita.
10 Agragsakto dagiti nalinteg gapu iti inaramid ni Yahweh ken agkamangdanto kenkuana; amin dagiti naimbag, ipannakkeldanto isuna.
Lolani wolungama akondwere mwa Yehova ndi kubisala mwa Iye, owongoka mtima onse atamande Iye!