< Dagiti Salmo 57 >

1 Kaasiannak, O Dios, kaasiannak, ta agkamangak kenka agingga a malpas dagiti pakariribukak. Agtalinaedak iti sirok dagiti payakmo nga agpaay a salaknib agingga a malpas daytoy a pannakadadael.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Musawononge.” Ndakatulo ya Davide, pamene anathawa Sauli kupita ku phanga. Mundichitire chifundo, Inu Mulungu mundichitire chifundo, pakuti mwa Inu moyo wanga umathawiramo. Ndidzathawira mu mthunzi wa mapiko anu mpaka chiwonongeko chitapita.
2 Umasugakto kenka O Dios a Kangatoan, iti Dios, a mangted iti amin a kasapulak.
Ine ndikufuwulira kwa Mulungu Wammwambamwamba, kwa Mulungu amene amakwaniritsa cholinga chake pa ine.
3 Manipud langit, sungbatannak ket isalakannak, inton babalawennak ti tao nga agtarigagay a mangalun-on kaniak; (Selah) ipaayto ti Dios kaniak ti kinapudno iti tulagna ken ti kinamatalekna.
Mulungu amanditumizira kuchokera kumwamba ndi kundipulumutsa, kudzudzula iwo amene akundithamangitsa kwambiri. Mulungu amatumiza chikondi chake ndi kukhulupirika kwake.
4 Kaduak dagiti leon; addaak kadagidiay nakasagana a mangalun-on kaniak. Addaak kadagiti tattao a kasla gayang ken pana dagiti ngipenda, ken natadem a kampilan dagiti dilada.
Ine ndili pakati pa mikango, ndagona pakati pa zirombo zolusa; anthu amene mano awo ndi milomo yawo ndi mivi, malilime awo ndi malupanga akuthwa.
5 Maitan-okka, O Dios, iti tangatang; maitag-ay koma ti dayagmo iti entero a daga.
Mukwezekedwe Inu Mulungu, kuposa mayiko onse akumwamba; mulole kuti ulemerero wanu ukhale pa dziko lonse lapansi.
6 Nangipakatda iti iket nga agpaay kadagiti sakak; Nagtuokak. Nangkalida ti abut iti sangoanak. Natnagda a mismo iti tengnga daytoy! (Selah)
Iwo anatchera mapazi anga ukonde ndipo ndinawerama pansi mosautsidwa. Anakumba dzenje mʼnjira yanga koma agweramo okha mʼmenemo.
7 Natalged ti pusok, O Dios, natalged ti pusok; agkantaak, wen, agkantaak ti pagdaydayaw,
Mtima wanga ndi wokhazikika, Inu Mulungu mtima wanga ndi wokhazikika. Ndidzayimba nyimbo, nyimbo yake yamatamando.
8 Agriingka, O kararuak, agriingka, saltero ken arpa; riingek ti bannawag.
Dzuka moyo wanga! Dzukani zeze ndi pangwe! Ndidzadzuka mʼbandakucha.
9 Agyamanak kenka, O Apo, kadagiti tattao; agkantaak kadagiti pagdaydayaw kenka kadagiti nasion.
Ndidzakutamandani Ambuye, pakati pa mitundu ya anthu, ndidzayimba za Inu pakati pa mayiko.
10 Ta ti kinapudnom iti tulagmo ket naindaklan aggingga kadagiti langit, ken dumanon kadagiti tangatang ti kinamatalekmo.
Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu, kufikira ku mayiko akumwamba; kukhulupirika kwanu kwafika ku mitambo.
11 Maintan-okka, O Dios, iti tangatang; maitan-ok koma ti dayagmo iti entero a daga.
Mukwezekedwe Inu Mulungu kuposa mayiko akumwamba, mulole kuti ulemerero wanu ukhale pa dziko lonse lapansi.

< Dagiti Salmo 57 >