< Dagiti Salmo 56 >

1 Maasika kaniak, O Dios, ta kayatnak nga alun-onen ti maysa a tao; agmalmalem a dardarupen ken idaddadanesnak.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Njiwa pa Mtengo wa Thundu wa Kutali.” Mikitamu ya Davide, pamene Afilisti anamugwira ku Gati. Mundichitire chifundo Inu Mulungu, pakuti anthu akundithamangitsa kwambiri; tsiku lonse akundithira nkhondo.
2 Agmalmalem a kayatdak nga alun-onen dagiti kabusorko; ta adu dagiti natangsit a dumarup kaniak.
Ondinyoza akundithamangitsa tsiku lonse, ambiri akumenyana nane monyada.
3 No mabutengak, agtalekak kenka.
Ndikachita mantha ndimadalira Inu.
4 Iti Dios, a daydayawek ti saona—agtalekak iti Dios; saanakto nga agbuteng; ania ti mabalin nga aramiden ti tao kaniak?
Mwa Mulungu, amene mawu ake ine ndimatamanda, mwa Mulungu ine ndimadaliramo; sindidzachita mantha. Kodi munthu amene amafa angandichite chiyani?
5 Agmalmalem a baliktadenda dagiti sasaok; amin a panagpanpanunotda ket maibusor kaniak para iti pakadaksan.
Tsiku lonse amatembenuza mawu anga; nthawi zonse amakonza zondivulaza.
6 Agu-ummongda, aglemmengda, ket sipsiputanda amin nga addangko, a kas iti panangurayda iti biagko.
Iwo amakambirana, amandibisalira, amayangʼanitsitsa mayendedwe anga ndipo amakhala ndi chidwi chofuna kuchotsa moyo wanga.
7 Saanmo nga ipalubos a makalibasda nga agar-aramid iti kinadakes. Ipababam dagiti tattao iti ungetmo, O Dios.
Musalole konse kuti athawe; mu mkwiyo wanu Mulungu mugwetse mitundu ya anthu.
8 Bilangem dagiti pannakaiyaw-awanko ken ikabilmo dagiti luluak iti boteliam; saanda aya a nailista iti bukodmo a libro?
Mulembe za kulira kwanga, mulembe chiwerengero cha misozi yanga mʼbuku lanu. Kodi zimenezi sizinalembedwe mʼbuku lanulo?
9 Ket agsanudto dagiti kabusorko iti aldaw nga umawagak kenka; daytoy ti ammok, adda ti Dios kaniak.
Adani anga adzabwerera mʼmbuyo pamene ndidzalirira kwa Inu. Pamenepo ndidzadziwa kuti Mulungu ali ku mbali yanga.
10 Iti Dios, a daydayawek ti saona—kenni Yahweh, a daydayawek ti saona—
Mwa Mulungu amene mawu ake ndimawatamanda, mwa Yehova amene mawu ake ndimawatamanda,
11 Agtalekak iti Dios; saanakto nga agbuteng, ania ti mabalin nga aramidek ti tao kaniak?
mwa Mulungu ine ndimadalira ndipo sindidzachita mantha. Kodi munthu angandichite chiyani?
12 Adda kaniak ti pagrebbengan a mangtungpal kadagiti karik kenka, O Dios; agidatonakto iti pagyamanko kenka.
Ndiyenera kuchita zomwe ndinalumbira kwa Mulungu; ndidzapereka nsembe zanga zachiyamiko kwa inu.
13 Ta inispalmo ti biagko manipud iti patay; inlisim dagiti sakak manipud iti pannakatinnag, tapno makapagnaak iti sangoanan ti Dios iti lawag ti sibibiag.
Pakuti mwawombola moyo wanga ku imfa ndi mapazi anga kuti ndingagwe, kuti ndiyende pamaso pa Mulungu mʼkuwala kwa moyo.

< Dagiti Salmo 56 >