< Dagiti Salmo 42 >

1 Kas iti panagal-al ti ugsa iti pannakawawna iti danum ti waig, kasta ti pannakawawko kenka, O Dios.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Ndakatulo ya ana a Kora. Monga mbawala ipuma wefuwefu kufunafuna mitsinje yamadzi, kotero moyo wanga upuma wefuwefu kufunafuna Inu Mulungu.
2 Mawawak para iti Dios, para iti sibibiag a Dios; kaanonto nga umayak ket sumangoak iti sangoanan ti Dios?
Moyo wanga uli ndi ludzu lofuna Mulungu, lofuna Mulungu wamoyo. Kodi ndipite liti kukakumana ndi Mulungu?
3 Dagiti luak ti nagbalin a taraonko iti aldaw ken rabii, kabayatan a kankanayon nga ibagbaga dagiti kabusorko kaniak, “Sadino ti ayan ti Diosmo?”
Misozi yanga yakhala chakudya changa usana ndi usiku, pamene anthu akunena kwa ine tsiku lonse kuti, “Mulungu wako ali kuti?”
4 Malagipko dagitoy a banbanag kas ibuyatko ti kararuak: no kasano a nakipanak kadagiti adu a tattao ken indauloak ida iti balay ti Dios nga addaan timek ti rag-o ken dayaw, dagiti adu a mangramrambak iti fiesta.
Zinthu izi ndimazikumbukira pamene ndikukhuthula moyo wanga: momwe ndinkapitira ndi gulu lalikulu, kutsogolera mayendedwe a ku Nyumba ya Mulungu ndi mfuwu yachimwemwe ndi mayamiko pakati pa anthu a pa chikondwerero.
5 Apay a nakadumogka, O kararuak, ken apay a madanaganka iti kaunggak? Mangnamnamaka iti Dios, ta agdayawak pay kenkuana para iti tulong ti presensiana.
Nʼchifukwa chiyani uli ndi chisoni, iwe moyo wanga? Nʼchifukwa chiyani wakhumudwa iwe mʼkati mwanga? Yembekezera Mulungu, pakuti ndidzamulambirabe, Mpulumutsi wanga ndi
6 O Diosko, nakadumog ti kararuak iti kaunggak, ngarud malagipka manipud iti daga idiay Jordan, manipud kadagiti tallo a tapaw ti Bantay Hermon, ken manipud iti turod ti Mizar.
Mulungu wanga. Moyo wanga uli ndi chisoni mʼkati mwanga kotero ndidzakumbukira Inu kuchokera ku dziko la Yorodani, ku mitunda ya Herimoni kuchokera ku phiri la Mizara.
7 Ti kaadalman ayabanna ti sabali a kaadalman iti karasakas ti panagdissoor dagiti danummo; naglasat dagiti dalluyon ken palongmo kaniak.
Madzi akuya akuyitana madzi akuya mu mkokomo wa mathithi anu; mafunde anu onse obwera mwamphamvu andimiza.
8 Nupay kasta, bilinento ni Yahweh ti kinapudnona ti tulagna iti aldaw; addanto kaniak ti kantana iti rabii, maysa a kararag iti Dios ti biagko.
Koma usana Yehova amalamulira chikondi chake, nthawi ya usiku nyimbo yake ili nane; pemphero kwa Mulungu wa moyo wanga.
9 Ibagakto iti Dios, a batok, Apay a nalipatannak? Apay nga agtultuloy nga agladladingitak gapu iti panangidadanes dagiti kabusor?”
Ine ndikuti kwa Mulungu Thanthwe langa, “Nʼchifukwa chiyani mwandiyiwala? Nʼchifukwa chiyani ndiyenera kuyenda ndikulira, woponderezedwa ndi mdani?”
10 A kas kampilan kadagiti tulangko, a tubtubngarendak dagiti kabusorko, kabayatan a kanayon nga ibagbagada kaniak, “Sadino ti ayan ti Diosmo?”
Mafupa anga ali ndi ululu wakufa nawo pamene adani anga akundinyoza, tsiku lonse akunena kuti, “Mulungu wako ali kuti?”
11 Apay a nakadumogka, kararuak? Apay a maringgoranka iti kaunggak? Mangnamnamaka iti Dios, ta agdayawak pay kenkuana, nga isu ti tulong iti rupak ken Diosko.
Bwanji ukumva chisoni, iwe mtima wanga? Chifukwa chiyani ukuvutika chonchi mʼkati mwanga? Khulupirira Mulungu, pakuti ndidzamutamandanso, Iye amene ali thandizo langa ndi Mulungu wanga.

< Dagiti Salmo 42 >