< Dagiti Salmo 38 >
1 O Yahweh, saannak a tubngaren iti ungetmo; saannak a dusaen iti pungtotmo.
Salimo la Davide. Kupempha. Yehova musandidzudzule mutapsa mtima kapena kundilanga muli ndi ukali.
2 Ta sinugatnak dagiti panam; ken italtalmegnak dagiti imam.
Pakuti mivi yanu yandilasa, ndipo dzanja lanu latsika ndipo landifikira.
3 Masakit ti entero a bagik gapu iti ungetmo, saan a nasalun-at dagiti tulangko gapu iti basolko.
Chifukwa cha ukali wanu mulibe thanzi mʼthupi langa; mafupa anga alibe mphamvu chifukwa cha tchimo langa.
4 Ta linapunosnak dagiti kinadakesko; nadagsenda unay nga awitko.
Kulakwa kwanga kwandipsinja ngati katundu wolemera kwambiri kuposa mphamvu zanga.
5 Agnunog ken bumangsit dagiti sugatko gapu kadagiti minamaag a basbasolko.
Mabala anga akuwola ndipo akununkha chifukwa cha uchitsiru wa moyo wanga wauchimo.
6 Nagdumog ken naibabainak iti inaldaw; agdungdung-awak nga agmalmalem.
Ine ndapindika msana ndipo ndawerama kwambiri; tsiku lonse ndimangolira.
7 Ta inabaknak ti bain, ket agsaksakit ti entero a bagik.
Msana wanga wagwidwa ndi ululu wosasimbika, mulibe thanzi mʼthupi langa.
8 Agpipikel ken agkakapsutak; agasugak gapu iti ut-ot ti pusok.
Ndilibe mphamvu ndipo ndakunthidwa kwathunthu; ndikubuwula ndi ululu wa mumtima.
9 O Apo, maawatam dagiti tarigagay ti kaunggan ti pusok, ket saan a mailemmeng kenka dagiti as-asugko.
Zokhumba zanga zonse zili poonekera pamaso panu Ambuye, kusisima kwanga sikunabisike kwa Inu.
10 Agkebbakebba ti pusok, agkakapsutak, ken aglidem ti panagkitak.
Mtima wanga ukugunda, mphamvu zanga zikutha; ngakhale kuwala kwachoka mʼmaso mwanga.
11 Inadaywannak dagiti gagayyem ken kakaduak gapu iti kasasaadko; saandak nga asitgan dagiti kaarrubak.
Abwenzi anga ndi anzanga akundipewa chifukwa cha mabala anga; anansi anga akhala kutali nane.
12 Agipakat kadagiti silo para kaniak dagiti agpanggep iti biagko. Agmalmalem nga agsasao kadagiti makadadael ken makaallilaw a sasao dagiti agtarigagay a mangdangran kaniak.
Iwo amene akufunafuna moyo wanga atchera misampha yawo, oti andipwetekewo amayankhula za kuwonongeka kwanga; tsiku lonse amakonza zachinyengo.
13 Ngem siak, kaslaak maysa a tuleng a tao nga awan pulos mangngegna; kaslaak maysa nga umel a tao nga awan pulos maibagana.
Ine ndili ngati munthu wosamva amene sangamve, monga wosayankhula, amene sangathe kutsekula pakamwa pake;
14 Kaslaak maysa a tao a saan a makangngeg ken awan maisungbatna.
Ndakhala ngati munthu amene samva, amene pakamwa pake sipangathe kuyankha.
15 Awan duadua, nga urayenka, O Yahweh; sumungbatka, Apo a Diosko.
Ndikudikira Inu Yehova; mudzayankha, Inu Ambuye Mulungu wanga.
16 Ibagak daytoy tapno saandak a pagkakatawaan dagiti kabusorko. No maikaglis ti sakak, agaramidda kadagiti nakaam-amak a banbanag kaniak.
Pakuti Ine ndinati, “Musawalole kuti akondwere kapena kudzikweza okha pa ine pamene phazi langa laterereka.”
17 Ta dandaniakon maitublak, ket kanayon nga agsagsagabaak.
Pakuti ndili pafupi kugwa, ndipo ndikumva kuwawa nthawi zonse.
18 Ipudnok ti basolko; maseknanak iti nagbasolak.
Ndikuvomereza mphulupulu zanga; ndipo ndavutika ndi tchimo langa.
19 Ngem adu dagiti kabusorko, adu dagiti gumurgura kaniak nga awan gapgapuna.
Ambiri ndi adani anga amphamvu; amene amandida popanda chifukwa alipo ochuluka kwambiri.
20 Sinubadanda iti kinadakes ti kinaimbagko; pabpabasolendak uray no ikalikagumko ti nasayaat.
Iwo amene amandibwezera zoyipa mʼmalo mwa zabwino amandinyoza pamene nditsatira zabwino.
21 Saannak a panawan, O Yahweh; a Diosko, saanka nga umadayo kaniak.
Inu Yehova, musanditaye; musakhale kutali ndi ine Mulungu wanga.
22 Darasem ti umay a tumulong kaniak, O Apo, a salakanko.
Bwerani msanga kudzandithandiza, Inu Ambuye Mpulumutsi wanga.