< Dagiti Salmo 12 >

1 Tumulongka, O Yahweh, ta nagpukaw dagiti nadiosan; awanen dagiti napudno.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Monga mwa mayimbidwe seminiti. Salimo la Davide. Thandizeni Yehova pakuti palibe munthu wokhulupirika; okhulupirika akusowa pakati pa anthu.
2 Agibagbaga ti tunggal maysa iti parbo a sasao iti kaarrubana; agsasao ti tunggal maysa nga addaan iti managpasablog a dila ken manangallilaw a puso.
Aliyense amanamiza mʼbale wake; ndi pakamwa pawo pabodza amayankhula zachinyengo.
3 O Yahweh, putdem dagiti amin a managpasablog a bibig, tunggal dila a mangipabpablaak iti nalabes a banbanag.
Inu Yehova tsekani milomo yonse yachinyengo ndi pakamwa paliponse podzikuza.
4 Dagitoy dagiti nagkuna, “Agballigikami babaen kadagiti dilami. No agsaokami, siasino ti makabael a mangituray kadakami?”
Pakamwa pamene pamati, “Ife tidzapambana ndi kuyankhula kwathu; pakamwapa ndi pathupathu, tsono mbuye wathu ndani?”
5 Gapu iti kinaranggas a maibusor kadagiti napanglaw, gapu iti as-asug dagiti agkasapulan, bumangonakto,” kuna ni Yahweh. “Ipaaykonto ti kinatalged a kalkalikagumanda.”
“Chifukwa cha kuponderezedwa kwa anthu opanda mphamvu ndi kubuwula kwa anthu osowa, Ine ndidzauka tsopano,” akutero Yehova, “Ndidzawateteza kwa owazunza.”
6 Nasin-aw dagiti sasao ni Yahweh, kasla pirak a napadalus iti naminpito iti maysa nga orno iti rabaw ti daga.
Ndipo mawu a Yehova ndi angwiro monga siliva oyengedwa mʼngʼanjo yadothi, oyengedwa kasanu nʼkawiri.
7 Sika ni Yahweh! Salsalaknibam ida. Ay-aywanam dagiti nadiosan a tattao manipud iti daytoy nadangkes a kaputotan ken iti agnanayon.
Inu Yehova mudzatitchinjiriza ndipo mudzatiteteza kwa anthu otere kwamuyaya.
8 Magna dagiti nadangkes iti tunggal suli no maitan-ok ti kinadakes kadagiti annak dagiti tattao.
Oyipa amangoyendayenda ponseponse anthu akamayamikira zochita zawo.

< Dagiti Salmo 12 >