< Dagiti Salmo 112 >

1 Idaydayawyo ni Yahweh. Nagasat ti tao nga agtultulnog kenni Yahweh, nga agragragsak unay kadagiti bilbilinna.
Tamandani Yehova. Wodala munthu amene amaopa Yehova, amene amakondwera kwambiri ndi malamulo ake.
2 Agbalinto a nabileg dagiti kaputotanna iti rabaw ti daga; mabendisionanto dagiti kaputotan ti nadiosan a tao.
Ana ake adzakhala amphamvu mʼdziko; mʼbado wa olungama mtima udzadalitsidwa.
3 Sanikua ken kinabaknang ket adda iti balayna; ti kinalintegna agtalinaed iti agnanayon.
Kulemera ndi chuma zili mʼnyumba yake, ndipo chilungamo chake ndi chosatha.
4 Adda iti agraniag a lawag iti kasipngetan iti nadiosan a tao; naparabur, manangngaasi, ken nalinteg isuna.
Ngakhale mu mdima kuwala kumatulukira olungama mtima; wokoma mtima, wachifundo ndi wowongoka mtima.
5 Nasayaat ti mapasamak iti tao a naparabur ken agpabulod iti kuarta, a napudno kadagiti panagtrabahona.
Zinthu zabwino zidzabwera kwa iye amene amapereka mowolowamanja ndi wokongoletsa mwaufulu, amene amachita ntchito yake mwachilungamo.
6 Ta saanto pulos isuna a magaraw; agnanayonto a malaglagip ti nalinteg a tao.
Ndithu sadzagwedezeka; munthu wolungama sadzayiwalika mpaka muyaya.
7 Saanna a kabuteng dagiti dakes a damag; natalged isuna nga agtaltalek kenni Yahweh.
Saopa akamva zoyipa zimene zachitika; mtima wake ndi wokhazikika ndipo amadalira Yehova.
8 Natalna ti pusona, a saan nga agbuteng, agingga a makitana ti balligi manipud kadagiti kabusorna.
Mtima wake ndi wotetezedwa, sadzakhala ndi mantha; potsiriza pake adzayangʼana adani ake mwachipambano.
9 Naparabur isuna a mangmangted kadagiti marigrigat; ti kinalintegna ket agtalinaed iti agnanayon; mapadayawanto isuna.
Wopereka mphatso zake mowolowamanja kwa osauka, chilungamo chake chimanka mpaka muyaya; nyanga yake idzakwezedwa mwaulemu.
10 Makapungtot no makita daytoy ti managdakdakes a tao; agngaretnget ti ngipenna ket pumanaw isuna; mapukawto ti tarigagay dagiti managdakdakes a tattao.
Munthu woyipa adzaona zimenezi ndipo adzapsa mtima; adzakukuta mano ake ndipo adzasungunuka. Zolakalaka za anthu oyipa sizidzachitika konse.

< Dagiti Salmo 112 >