< Dagiti Salmo 111 >

1 Idaydayawyo ni Yahweh. Agyamanak kenni Yahweh iti amin a pusok iti gimong dagiti nalinteg, iti panagtitiponda.
Tamandani Yehova. Ndidzathokoza Yehova ndi mtima wanga wonse mʼbwalo la anthu olungama mtima ndi pa msonkhano.
2 Naindaklan dagiti aramid ni Yahweh, a sigagagar nga ur-urayen dagiti amin nga agtartarigagay kadagitoy.
Ntchito za Yehova nʼzazikulu; onse amene amakondwera nazo amazilingalira.
3 Naindaklan ken natan-ok ti aramidna, ken agtalinaed iti agnanayon ti kinalintegna.
Zochita zake ndi za ulemerero ndi zaufumu, ndipo chilungamo chake ndi chosatha.
4 Agar-aramid isuna kadagiti nakakaskasdaaw a banbanag a saan a malipatan; naparabur ken manangnga-asi ni Yahweh.
Iye wachititsa kuti zodabwitsa zake zikumbukirike; Yehova ndi wokoma mtima ndi wachifundo.
5 Ik-ikanna ti taraon dagiti napudno a sumursurot kenkuana. Kankanayonna a laglagipen ti tulagna.
Amapereka chakudya kwa amene amamuopa Iye; amakumbukira pangano lake kwamuyaya.
6 Impakitana dagiti pannakabalinna babaen kadagiti aramidna kadagiti tattaona iti panangitedna kadakuada iti tawid dagiti nasion.
Waonetsa anthu ake mphamvu ya ntchito zake, kuwapatsa mayiko a anthu a mitundu ina.
7 Napudno ken nalinteg dagiti aramid dagiti imana; mapangnamnamaan dagiti amin a bilinna.
Ntchito za manja ake ndi zokhulupirika ndi zolungama; malangizo ake onse ndi odalirika.
8 Naaramid dagitoy nga agtalinaed iti agnanayon, a masapul a suroten a sipupudno ken sisasayaat.
Malamulo ndi okhazikika ku nthawi za nthawi, ochitidwa mokhulupirika ndi molungama.
9 Intedna ti balligi kadagiti tattaona; insaadna ti katulaganna iti agnanayon; nasantoan ken makapasiddaaw ti naganna.
Iyeyo amawombola anthu ake; anakhazikitsa pangano lake kwamuyaya dzina lake ndi loyera ndi loopsa.
10 Ti panangraem kenni Yahweh ket isu ti rugrugi ti kinasirib; dagiti mangar-aramid kadagiti bilinna ket addaan iti nasayaat a pannakaawat. Ti dayawna ket agtalinaed iti agnanayon.
Kuopa Yehova ndicho chiyambi cha nzeru; onse amene amatsatira malangizo ake amamvetsa bwino zinthu. Iye ndi wotamandika mpaka muyaya.

< Dagiti Salmo 111 >