< Nehemias 8 >

1 Naguummong dagiti amin a tattao idiay nalawa a disso iti sango ti Ruangan ti Danum para iti maysa a panggep. Kiniddawda kenni Ezra nga eskriba nga iyegna ti Libro ti Linteg ni Moises nga imbilin ni Yahweh iti Israel.
Anthu onse anasonkhana ngati munthu mmodzi pabwalo limene lili patsogolo pa Chipata cha Madzi. Iwo anawuza mlembi Ezara kuti abwere ndi buku la malamulo a Mose limene Yehova anapereka kwa Aisraeli.
2 Iti umuna nga aldaw iti maikapito a bulan, inyeg ni Ezra a padi ti linteg iti sangoanan ti gimong, babbai man wenno lallaki, ken kadagiti amin a makangngeg ken makaawat.
Choncho pa tsiku loyamba la mwezi wachisanu ndi chiwiri wansembe Ezara, anabwera ndi buku la malamulo ku msonkhano wa amuna, akazi ndi ana onse amene ankatha kumvetsa zinthu bwino.
3 Sinangona ti nalawa a disso iti sango ti Ruangan ti Danum, ket binasana daytoy manipud iti agsapa agingga iti agmatuon, iti sangoanan dagiti lallaki ken babbai, ken iti siasinoman a makaawat. Ket dimngeg a nasayaat dagiti tattao iti Libro ti Linteg.
Choncho Ezara anawerenga bukulo atayangʼana bwalo la Chipata cha Madzi kuyambira mmawa mpaka masana pamaso pa amuna, akazi ndi onse amene ankamvetsa bwino zinthu. Ndipo anthu onse anatchera khutu kuti amve malamulowo.
4 Ket nagtakder ni Ezra nga eskriba iti nangato a kayo a plataforma nga inaramid dagiti tattao para iti daytoy a panggep. Nakatakder iti makannawanna da Mattitias, Sema, Anaias, Urias, Hilkias ken Maaseias; ken nakatakder iti makannigidna da Pedaias, Misael, Malkija, Hasum, Hasbaddana, Zacarias ken Mesullam.
Mlembi Ezara anayimirira pa nsanja ya mitengo imene anthu anamanga chifukwa cha msonkhanowu. Ku dzanja lake lamanja kunayimirira Matitiya, Sema, Anaya, Uriya, Hilikiya ndi Maaseya, ndipo kudzanja lake lamanzere kunali Pedaya, Misaeli, Malikiya, Hasumu, Hasibadana, Zekariya ndi Mesulamu.
5 Linuktan ni Ezra ti libro iti imatang dagiti amin a tattao gapu ta nakatakder isuna iti ngatoenda, ket nagtakder dagiti amin a tattao apaman a naluktanna daytoy.
Tsono Ezara anatsekula buku, akuona popeza anayima pa nsanja. Pamene anafutukula bukulo anthu onse anayimirira.
6 Nagyaman ni Ezra kenni Yahweh, ti naindaklan a Dios ken inngato dagiti amin a tattao dagiti imada ket insungbatda, “Sapay koma ta kasta! Sapay koma ta kasta!” Kalpasanna, nagpaklebda ket nagdaydayawda kenni Yahweh.
Ezara anatamanda Yehova, Mulungu wamkulu, ndipo anthu onse anakweza manja awo ndi kuyankha kuti, “Ameni, ameni.” Pambuyo pake onse anaweramitsa pansi mitu yawo napembedza Yehova akanali chizolikire choncho.
7 Tinulongan da Jesua, Bani, Serebias, Jamin, Akkub, Sabbetai, Hodias, Maaseias, Kelita, Azarias, Josabad, Hanan, Pelaias ken dagiti Levita dagiti tattao tapno maawatanda ti linteg kabayatan nga adda latta kadagiti puestoda dagiti tattao.
Anthuwo atayimiriranso Alevi awa: Yesuwa, Bani, Serebiya, Yamini, Akubu, Sabetayi, Hodiya, Maaseya, Kerita, Azariya, Yozabadi, Hanani ndi Pelaya anawathandiza kuti amvetse bwino malamulowo.
8 Ken binasada iti libro, ti linteg ti Dios, ket inlawlawagda daytoy babaen iti panangipatarus ken panangitedda iti kaipapanan daytoy tapno maawatan dagiti tattao ti naibasa.
Iwo anawerenga buku la malamulo a Mulungu momveka bwino ndi kutanthauzira mawuwo kuti anthu amvetse bwino zowerengedwazo.
9 Ni Nehemias a gobernador, ni Ezra a padi ken eskriba, ken dagiti Levita a mangipalpalawag kadagiti tattao ket kinunada kadagiti amin a tattao, “Nasantoan daytoy nga aldaw kenni Yahweh a Diosyo. Saankayo nga agladingit wenno agsangit.” Ta nagsasangit dagiti amin a tattao idi nangngegda dagiti sasao manipud iti linteg.
Tsono bwanamkubwa Nehemiya pamodzi ndi wansembe ndi mlembi Ezara komanso Alevi amene amaphunzitsa anthu anati kwa anthu onse, “Lero ndi tsiku lopatulika kwa Yehova Mulungu wanu. Musakhale ndi chisoni ndipo musalire.” Anayankhula choncho popeza anthu onse ankalira atamva mawu a buku la malamulo lija.
10 Ket kinunana ni Nehemias kadakuada, “Agawidkayon, mangankayo iti naimas a taraon ken uminumkayo iti nasam-it, ket mangtedkayo kadagiti awan ti naisaganana gapu ta nasantoan daytoy nga aldaw iti Apotayo. Saankayo nga agladingit, ta ti rag-o ni Yahweh ti pigsayo.”
Nehemiya anatinso, “Pitani, kachiteni phwando ku nyumba ndipo mukawagawireko ena amene alibe kanthu kalikonse popeza lero ndi tsiku lopatulika kwa Yehova. Musakhale ndi chisoni, pakuti chimwemwe cha Yehova ndiye mphamvu yanu.”
11 Isu a pinagulimek dagiti Levita dagiti tattao a kunada, “Agtalnakayo! ta nasantoan daytoy nga aldaw. Saankayo nga agladingit.”
Alevi anakhalitsa bata anthu onse powawuza kuti, “Khalani chete, pakuti lero ndi tsiku lopatulika ndipo musakhale ndi chisoni.”
12 Ket nagawid dagiti tattao tapno mangan, uminum, mangibingay iti makan, ken agrambakda nga addaan iti kasta unay a rag-o gapu ta naawatanda dagiti sasao a naipakaammo kadakuada.
Anthu onse anachoka kupita kukadya ndi kumwa. Chakudya china anatumiza kwa anzawo. Choncho panali chikondwerero chachikulu popeza tsopano anali atamvetsa bwino mawu a Mulungu amene anawawerengera ndi kuwafotokozerawo.
13 Iti maikadua nga aldaw, dagiti panguloen dagiti kapuonan ti pamilia manipud kadagiti amin a tattao, dagiti padi ken dagiti Levita ket sangsangkamaysada a napan kenni Ezra nga eskriba tapno adalenda dagiti sasao ti linteg.
Mmawa mwake atsogoleri a mabanja pamodzi ndi ansembe ndi alevi anasonkhana kwa Ezara, mlembi wa malamulo kuti aphunzire mawu a malamulowo.
14 Ket nakitada a nakailanad iti linteg no kasano nga imbilin ni Yahweh babaen kenni Moises a rumbeng nga agnaed kadagiti tolda dagiti tattao ti Israel kabayatan ti fiesta iti maikapito a bulan.
Tsono anapeza kuti zinalembedwa mʼbuku la malamulo kuti Yehova analamula kudzera mwa Mose kuti Aisraeli azikhala mʼzithando pa nthawi yonse ya chikondwerero cha mwezi wachisanu ndi chiwiri.
15 Rumbeng nga iwaragawagda iti amin a siudadda ken iti Jerusalem, a kunada, “Mapankayo idiay katurturodan, ken mangalakayo kadagiti sanga ti kayo nga olibo ken balang nga olibo, sangsanga ti mirto, sangsanga ti palma ken sangsanga dagiti narukbos a kayo tapno agaramidkayo kadagiti abong-abong,” a kas naisurat.
Choncho analengeza ndi kufalitsa mʼmizinda yawo yonse ndi mu Yerusalemu kuti, “Pitani ku phiri mukadule nthambi za mtengo wa olivi, za mtengo wa olivi wa kutchire, za mtengo wa mchisu, za mtengo wa mgwalangwa ndiponso za mitengo ina ya masamba, zomangira zithando monga zalembedweramu ndi kubwera nazo.”
16 Isu a napan nangala dagiti tattao kadagiti sanga ket nagaramidda kadagiti abong-abong iti tuktok dagiti babbalayda, kadagiti paraanganda, kadagiti paraangan ti balay ti Dios, iti nalawa a disso iti abay ti Ruangan ti Danum ken iti plasa iti abay ti Ruangan ni Efraim.
Choncho anthu anapita kukatenga nthambi ndipo aliyense anadzimangira misasa pa denga ya nyumba yake, mʼmabwalo awo, mʼmabwalo a Nyumba ya Mulungu, mʼbwalo la pa Chipata cha Madzi ndiponso mʼbwalo la pa Chipata cha Efereimu.
17 Ket nagaramid dagti amin a gimong dagiti nakasubli manipud iti pannakaitalawda a kas balud kadagiti abong-abong sada nagyan kadagitoy. Agsipud ta saan a rinambakan dagiti tattao ti Israel daytoy a fiesta manipud iti aldaw ni Josue a putot ni Nun agingga iti dayta nga aldaw. Ket kasta unay ti rag-oda.
Gulu lonse la anthu limene linabwera ku ukapolo linamanga misasa ndipo linakhala mʼmenemo. Kuyambira nthawi ya Yoswa mwana wa Nuni mpaka tsiku limenelo nʼkuti Aisraeli asanachitepo zimenezi. Choncho panali chimwemwe chachikulu.
18 Manipud iti umuna nga aldaw agingga iti maudi, inaldaw nga agbasa ni Ezra manipud iti Libro iti Linteg ti Dios. Rinambakanda ti fiesta iti pito nga aldaw ken iti maikawalo nga aldaw ket nangangayda iti napasnek a panagguummong a kas panagtulnog iti paglintegan.
Tsiku ndi tsiku, kuyambira tsiku loyamba mpaka lomaliza, Ezara ankawerenga buku la malamulo a Mulungu. Anthu anachita chikondwerero masiku asanu ndi awiri. Pa tsiku lachisanu ndi chitatu panachitika msonkhano potsata buku la malamulo lija.

< Nehemias 8 >