< Malakias 4 >

1 Ta kitaenyo, umadanin ti aldaw, gumilgil-ayab a kasla hurno, inton amin dagiti natangsit ken amin a nadangkes ket agbalinto a kasla garami. Ti dumteng nga aldaw ti manguram kadakuada,” kuna ni Yahweh a Mannakabalin amin, “ket daytoy ti mangkisap kadakuada agingga nga awan iti matda uray ramut wenno sanga.
Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ndithu tsiku likubwera; lidzayaka ngati ngʼanjo. Anthu onse odzikuza, ndi aliyense ochita zoyipa adzapsa ngati chiputu, ndipo pa tsiku limene likubweralo adzapserera ndi moto. Sipadzatsalira muzu kapena nthambi.
2 Ngem dakayo nga agbuteng iti naganko, agsingisingto ti init iti kinalinteg nga adda pannakaagas kadagiti payyakna. Aglalagtokayto a rummuar a kasla kadagiti baka manipud iti kulungan.
Koma inu amene mumaopa dzina langa, dzuwa lachilungamo lidzakutulukirani lili ndi kuwala kokuchiritsani. Ndipo inu mudzatuluka ndi kulumphalumpha ngati ana angʼombe amene atulutsidwa mʼkhola.
3 Ket ibadebaddekyonto dagiti nadangkes, ta agbalindanto a dapu kadagiti dapanyo iti tiempo nga agtignayak,” kuna ni Yahweh a Mannakabalin amin.
Tsiku limenelo inu mudzapondereza anthu oyipa; adzakhala phulusa ku mapazi anu pa tsiku limene Ine ndidzachite zinthu zimenezi,” akutero Yehova Wamphamvuzonse.
4 “Laglagipenyo ti agtulnog iti linteg ni Moises nga adipenko, dagiti pagalagadan ken dagiti paglintegan nga imbilinko kenkuana idiay Horeb para iti entero nga Israel.
Kumbukirani zophunzitsa za mtumiki wanga Mose, malamulo ndi malangizo amene ndinamupatsa pa Horebu kuti awuze Aisraeli onse.
5 Adtoy, ibaonko ni Elias a propeta sakbay a dumteng ti nakaro ken nakaam-amak nga aldaw ni Yahweh.
“Taonani, ndidzakutumizirani mneneri Eliya lisanafike tsiku lalikulu ndi loopsa la Yehova.
6 Pagkaykaysaennanto ti puso dagiti ama kadagiti annak, ken ti puso dagiti annak kadagiti amada; tapno saanak nga umay ken dumarup iti daga a mangiwayat iti naan-anay a pannakadadael.”
Iye adzabweza mitima ya makolo kwa ana awo, ndi mitima ya ana kwa makolo awo. Kupanda kutero ndidzabwera kudzakantha dziko lanu ndi temberero.”

< Malakias 4 >