< Uk-ukom 21 >

1 Ita, nagkari dagiti lallaki ti Israel idiay Mizpa, “Awan kadatayo ti mangipaasawa iti anakna a babai iti Benjaminita.”
Aisraeli anali atalumbira ku Mizipa kuti, “Palibe mmodzi wa ife adzapereke mwana wake wamkazi kuti akwatiwe ndi mwamuna wa fuko la Benjamini.”
2 Kalpasanna, napan dagiti tattao idiay Betel ket nagtugawda sadiay iti sangoanan ti Dios agingga iti rabii, ken nasaem a nagladingitda iti napigsa.
Anthu anapita ku Beteli kumene anakakhala pansi pamaso pa Mulungu mpaka madzulo. Iwo anakweza mawu nalira kwambiri.
3 Kinunada, “O Yahweh a Dios ti Israel, apay a napasamak daytoy iti Israel, a maysa kadagiti tribumi ti awan tatta nga aldaw?”
Iwo ankanena kuti, “Yehova Mulungu wa Israeli, nʼchifukwa chiyani izi zachitika mʼdziko la Israeli kuti lero fuko limodzi lisowe mu Israeli?”
4 Iti sumaruno nga aldaw, nasapa a bimmangon dagiti tattao ket nangipatakderda iti altar sadiay ken nangidatonda kadagiti daton a mapuoran ken kadagiti daton a pakikappia.
Mmawa mwake anthu anadzuka namanga guwa lansembe ndi kupereka nsembe zopsereza ndi nsembe zachiyanjano.
5 Kinuna dagiti tattao ti Israel, “Siasino kadagiti amin a tribu ti Israel ti saan nga immay iti taripnong ni Yahweh?” Ta nangaramidda iti napateg a kari maipanggep iti siasinoman a saan a simmang-at kenni Yahweh idiay Mizpa. Kinunada, “Awan duadua a mapapatay isuna.”
Kenaka Aisraeli anafunsa kuti, “Kodi ndani pakati pa mafuko a Israeli sanafike ku msonkhano wa Yehova?” Anatero chifukwa anachita malumbiro aakulu okhudza munthu amene alephere kupita ku Mizipa ndi kuti woteroyo ayenera kuphedwa.
6 Naasian dagiti tattao ti Israel kadagiti kakabsatda a Benjaminita. Kinunada, “Ita nga aldaw, maysa a tribu ti naisina iti Israel.
Tsono Aisraeli anamva chisoni chifukwa cha abale awo, Abenjamini. Iwo anati, “Lero fuko limodzi lachotsedwa mu Israeli.
7 Siasino ti mangipaay kadagiti asawaen dagidiay a nabati, agsipudta nagkaritayo kenni Yahweh a saantayo a palubosan ti siasinoman kadakuada a mangasawa kadagiti annaktayo a babbai?”
Kodi tingawapezere bwanji anthu otsalawa akazi woti awakwatire? Paja ife tinalumbira kwa Yehova kuti sitidzapereka ana anthu aakazi kuti awakwatire.
8 Kinunada, “Siasino kadagiti tribu ti Israel ti saan a simmang-at kenni Yahweh idiay Mizpa?” Naduktalan nga awan ti immay iti panagtitipon manipud idiay Jabes Galaad.
Kenaka anafunsa kuti, ‘Kodi mu fuko la Israeli ndani amene sanabwere pamaso pa Yehova ku Mizipa?’” Tsono panapezeka kuti panalibe ndi mmodzi yemwe wochokera ku Yabesi Giliyadi amene anapita ku msonkhano ku misasa kuja.
9 Ta idi naurnos dagiti tattao iti nasayaat, adtoy, awan kadagiti agnanaed idiay Jabes Galaad ti adda sadiay.
Pamene anthu anawerengana anangoona kuti anthu a ku Yabesi Giliyadi palibe.
10 Nangibaon ti taripnong iti 12, 000 a katuturedan a lallaki a nabilin a mapanda idiay Jabes Galaad ket rautenda ida ken papatayenda ida, uray dagiti babbai ken ubbing.
Choncho msonkhano unatumiza anthu ankhondo 12,000 ndi kuwalamula kuti, “Mukaphe anthu onse okhala ku Yabesi Giliyadi, kuphatikizapo akazi ndi ana.”
11 “Aramidenyo daytoy: masapul a papatayenyo ti tunggal lalaki ken tunggal babai a nakikaidda iti lalaki.”
Izi ndi zimene mukachite. “Mukaphe mwamuna aliyense ndi mkazi aliyense amene anadziwapo mwamuna.”
12 Nakasarak dagiti lallaki iti 400 a babbalasang kadagiti agnanaed idiay Jabes Galaad a saan pulos a nakikaidda iti lalaki, ket impanda ida iti kampo idiay Silo, idiay Canaan.
Iwo anapeza atsikana 400 pakati pa anthu okhala mu Yabesi Giliyadi amene anali asanadziwepo mwamuna ndipo anabwera nawo ku misasa ku Silo mʼdziko la Kanaani.
13 Nangipatulod iti mensahe ti entero a taripnong ket imbagada kadagiti tattao ti Benjamin nga adda idiay bato ti Rimmon a makikapkappiada kadakuada.
Kenaka msonkhano wonse unatumiza uthenga kwa Abenjamini amene ankakhala ku thanthwe la Rimoni kuwawuza kuti nkhondo yatha.
14 Isu a nagsubli dagiti Benjaminita iti dayta a tiempo ket naited kadakuada dagiti babbai idiay Jabes Galaad. Ngem awan ti umdas a babbai a para kadakuada amin.
Choncho Abenjamini anabwera nthawi imeneyo ndipo Aisraeli anawapatsa akazi a ku Yabesi Giliyadi amene sanaphedwe. Koma sanapezeke owakwanira.
15 Nagbabawi dagiti tattao gapu iti napasamak iti Benjamin, gapu ta nangaramid ni Yahweh iti pannakabingay iti nagbabaetan dagiti tribu ti Israel.
Aisraeli anamvera chisoni Abenjamini, chifukwa Yehova anachita ngati waligwerula dzino fuko la Israeli.
16 Ket kinuna dagiti mangidadaulo iti entero a taripnong, “Kasanotayo nga ibirukan dagiti nabati a Benjaminita kadagiti babbai nga asawaenda, agsipud ta napapatayen dagiti babbai ti Benjamin?”
Choncho akuluakulu a msonkhano anati, “Kodi tikawapezera kuti akazi anthu otsalirawa kuti awakwatire popeza kuti akazi a fuko la Benjamini anaphedwa?”
17 Kinunada, “Masapul nga adda ti tawid para kadagiti nakalasat iti Benjamin, tapno saan a madadael ti maysa a tribu iti Israel.
Iwo anati, “Abenjamini amene anapulumukawa ayenera kukhala ndi zidzukulu, kuti mtundu wa Israeli usafafanizike.
18 Saantayo a mabalin nga ikkan ida kadagiti asawaenda manipud kadagiti annaktayo a babbai. Ta nagkari dagiti tattao ti Israel, 'Mailunod koma ti siasinoman a mangted iti babai nga asawaen ti Benjamin.’”
Ife sitingathe kuwapatsa ana anthu aakazi kuti akwatire. Paja tinalumbira kuti, ‘Akhale wotembereredwa aliyense amene adzapereka mwana wake wamkazi kwa mwamuna wa fuko la Benjamini kuti akwatire.’
19 Isu a kinunada, “Ammoyo nga adda iti tinawen a fiesta para kenni Yahweh idiay Silo (nga adda iti amianan ti Betel, dayaen ti kalsada a sumang-at idiay Sikem manipud idiay Betel, ken abagatan ti Lebona).”
Ndipo anati, ‘Paja ku Silo kuli chikondwerero cha chaka ndi chaka cholemekeza Yehova. Tsono Silo ali kumpoto kwa Beteli, kummawa kwa msewu wochokera ku Beteli kupita ku Sekemu, ndiponso kummwera kwa Lebona.’”
20 Binilinda dagiti lallaki ti Benjamin a kinunada, “Mapankayo aglemmeng iti nalimed ket aguraykayo kadagiti kaubasan.
Choncho anawalamulira Abenjamini aja kuti, “Pitani mukabisale mʼminda ya mpesa
21 Siputanyo ti oras a rummuar dagiti agsala a babbai manipud Silo, ket dardarasenyo a rummuar kadagiti kaubasan ket masapul a mangiguyod ti tunggal maysa kadakayo iti asawaenna manipud kadagiti babbai ti Silo, kalpasanna, agsublikayo iti daga ti Benjamin.
ndipo mukakhale tcheru. Ana aakazi a ku Silo akadzatulukira kudzavina nawo magule, pomwepo inu mutuluke minda ya mpesa ndi kukawagwira aliyense wake ndi kupita nawo ku dziko la Benjamini.
22 Inton umay dagiti amma wenno kakabsatda a lallaki tapno agririda kadakami, ibagaminto kadakuada, “Maasikayo kadakami! Pagtalinaedenyo ida gapu ta saankami a nakaala kadagiti babbai a maasawa bayat ti gubat. Ket awan basolyo maipapan iti kari, gapu ta saanyo nga inted kadakuada dagiti annakyo.”'
Ngati abambo awo kapena alongo awo adzabwera kudzadandaula kwa ife, tidzawawuza kuti, ‘Chonde, tikomereni mtima powalola kuti atenga ana anu aakaziwo popeza kuti ife sitinawapezere akazi pomenya nkhondo. Inunso simunachite kuwapatsa. Mukanatero ndiye mukanapalamula.’”
23 Kasta ti inaramid dagiti tattao ti Benjamin, nangalada kadagiti asawaenda segun iti bilang a kasapulanda manipud kadagiti babbai nga agsasala, ket innalada ida tapno agbalin nga assawada. Napanda ket nagsublida iti lugar a tawidda; binangonda manen dagiti ili ket nagnaedda kadagitoy.
Abenjamini anachitadi zimenezi. Mwa akazi amene ankavina aja anagwirapo ena, malingana ndi chiwerengero chawo, nawatenga kuti akhale akazi awo. Kenaka ananyamuka kubwerera ku dziko la kwawo, nakamanganso mizinda yawo ndi kumakhalamo.
24 Ket pinanawan dagiti tattao ti Israel dayta a lugar ket nagawidda, tunggal maysa iti bukodna a tribu ken puli, ken tunggal maysa iti bukodna a tawid.
Pambuyo pake Aisraeli anachoka kumeneko ndi kubwerera kwawo, ku mafuko ndi ku mabanja awo, aliyense ku dera la cholowa chake.
25 Kadagidiay nga aldaw, awan ti ari ti Israel. Inaramid ti tunggal maysa ti nasayaat kadagiti bukodna a panagkita.
Masiku amenewo kunalibe mfumu ku Israeli. Aliyense ankangochita zimene zomukomera yekha.

< Uk-ukom 21 >