< Josue 2 >

1 Sililimed ngarud a nangibaon ni Josue nga anak ni Nun iti dua a lallaki a kas espia manipud Settim. Kinunana, “Mapankayo iti entero a daga, nangnangruna iti Jerico.” Napanda ket dimtengda iti balay ti maysa a balangkantis nga agnagan iti Rahab, ket nagdagusda sadiay.
Tsono Yoswa mwana wa Nuni anatuma anthu awiri okazonda dziko mwachinsinsi kuchokera ku Sitimu. Iye anawawuza kuti, “Pitani mukaone dzikolo makamaka mzinda wa Yeriko.” Kotero iwo anapita ndipo anakafika ku nyumba ya mkazi wadama dzina lake Rahabe, ndipo anagona kumeneko.
2 Naipakaammo daytoy iti ari ti Jerico, “Immay ditoy dagiti lallaki manipud Israel a mangsiim iti daga.”
Mfumu ya Yeriko inawuzidwa kuti, “Aisraeli ena afika mu mzinda muno usiku uno kudzazonda dziko.”
3 Nangipadanon ti ari iti sao kenni Rahab ket kinunana, “Iruarmo dagiti lallaki nga immay kenka a simrek iti balaymo, ta immayda a mangsiim iti entero a daga.”
Choncho Mfumu ya Yeriko inatumiza uthenga kwa Rahabe kuti, “Atulutse anthu amene abwera ku nyumba kwakowo chifukwa iwo abwera kuti adzazonde dzikoli.”
4 Ngem innalan idi ti babai dagiti dua a lallaki ket inlemmengna ida. Ket kinunana, “Wen, immay kaniak dagiti lallaki, ngem saanko nga ammo no sadino ti naggapuanda.
Koma pa nthawiyi nʼkuti mkaziyo atatenga amuna awiriwo ndi kuwabisa. Tsono anayankha kuti, “Inde, anthuwo anafikadi ku nyumba kuno. Koma sindinadziwe kumene anachokera.
5 Pimmanawda idi sumipnget, idi agrikep ti ruangan ti siudad. Saanko nga ammo ti napananda. Mabalin a matiliwyo ida no darasenyo ida a kamaten.”
Iwo achoka kuno ndi chisisira, chipata cha mzinda chili pafupi kutsekedwa. Ndiye sindidziwa kumene alowera. Koma mukawalondola msanga muwapeza.”
6 Ngem pinaulina idi ida iti bubungan ti balay ket inlemmengna ida kadagiti kayo ti lino nga inkabilna iti rabaw daytoy.
Koma nʼkuti atawakweza pa denga azondiwo ndi kuwabisa pansi pa mapesi a thonje amene iye anawayika pa dengapo.
7 Kinamat ngarud dagiti lallaki dagiti dua nga espia nga agturong iti pagballasiwan ti Jordan. Ket nagrikep dagiti ruangan apaman a nakaruar dagiti mangkamkamat.
Nthumwi za mfumu zija zitatuluka ndipo chipata chinatsekedwa. Nthumwizo zinapita kukawafunafuna azondi aja mpaka ku dooko la Yorodani.
8 Saan pay a nakaidda dagiti dua nga espia idi inuli ida ti babai idiay pangatepan.
Azondiwo asanagone, Rahabe anakwera pa denga
9 Kinunana, “Ammok nga inted kadakayo ni Yahweh ti daga ta immay kadakami ti panagbuteng kadakayo. Agrunaw iti sangoananyo ti amin nga agnanaed iti daga.”
ndipo anawawuza kuti, “Ine ndikudziwa kuti Yehova wakupatsani dziko lino ndipo tili ndi mantha. Anthu onse a mʼdziko lino ali ndi mantha chifukwa cha inu.
10 Nangngeganmi no kasano a pinamaga ni Yahweh ti danum ti Baybay dagiti Runo para kadakayo idi rimuarkayo manipud Egipto. Ken nangngeganmi ti inaramidyo kadagiti dua nga ari dagiti Amorreo idiay bangir ti Jordan—ni Sihon ken ni Og— a naan-anay a dinadaelyo.
Ife tinamva mmene Yehova anawumitsira madzi a Nyanja Yofiira inu mukufika pamene munatuluka mʼdziko la Igupto. Tamvanso zimene munachita kwa Sihoni ndi Ogi, mafumu awiri a Aamori amene ali kummawa kwa Yorodani. Inu munawawononga kotheratu.
11 Apaman a nangngeganmi daytoy, narunaw dagiti pusomi ket awan ti nabati a tured iti siasinoman—ta ni Yahweh a Diosyo ket Dios sadi-langit ken iti rabaw ti daga.
Titamva zimenezi, ife tinataya mtima ndipo aliyense wa ife ali ndi mantha chifukwa cha inu. Tikudziwa kuti Yehova Mulungu wanu ndi Mulungu wa kumwamba ndi dziko lapansi.
12 Ita ngarud, pangngaasiyo ta isapatayo kaniak babaen kenni Yahweh a kas iti panangngaasik kadakayo, kaassianyonto met iti balay ti amak. Ikkandak iti natalged a pagilasinan
Choncho mulumbire pamaso pa Yehova ndi kundipatsa chizindikiro choti mudzachitadi zimene mwalonjeza, kuti monga inu ndakuchitirani chifundo, inunso mudzachitira chifundo a pa banja la abambo anga.
13 nga ispalenyonto ti biag ti amak, inak, kakabsatko a lallaki ken babbai, ken dagiti amin a pamiliada, ken isalakandakaminto manipud iti ipapatay.”
Inu mulonjeze kuti simudzapha abambo anga ndi amayi anga, abale anga ndi alongo anga ndi mabanja awo omwe.”
14 Kinuna dagiti lallaki kenkuana, “Para kenka ti biagmi, uray agingga iti patay! No saanmo a sarsaritaen ti maipapan iti rantami, maasi ken napudnokaminto ngarud kenka inton ited ni Yahweh daytoy a daga kadakami.”
Anthuwo anamuyankha kuti, “Ife ndife okonzeka kufa chifukwa cha inu. Ngati iwe sudzawulula zimene tachitazi, ndiye kuti ife tidzakukomera mtima ndi kusunga pangano lathu ndi iwe, Yehova akadzatipatsa dziko lino.”
15 Pinaulogna ngarud ida idiay tawa babaen iti tali. Ti balay a pagnanaedanna ket naikapet iti pader ti siudad.
Popeza nyumba ya Rahabe inali pa linga la mzindawo, azondi aja anatulukira pa zenera. Rahabe anawatsitsa pansi ndi chingwe.
16 Kinunana kadakuada, “Mapankayo kadagiti turturod ket aglemmengkayo ta no saan ket masarakandakayo dagiti mangkamkamat kadakayo. Aglemmengkayo sadiay iti tallo nga aldaw agingga a makasubli dagiti mangkamkamat. Ket mapankayo iti dalanyo.”
Iye anawawuza kuti, “Pitani ku mapiri kuti okuthamangiraniwo asakupezeni. Mukabisale kumeneko masiku atatu mpaka iwo atabwerera, ndipo kenaka muzikapita kwanu.”
17 Kinuna dagiti dua nga espia kenni Rahab, “Awanto iti pagrebbenganmi kadagiti impasapatam kadakami, no saanmo nga aramiden daytoy:
Anthuwo anati kwa iye, “Lonjezo limene watichititsa ifeli tidzalisungadi
18 Inton serkenmi ti daga, masapul a mangigalutka iti nalabaga a tali iti tawa a nangipaulogam kadakami, ket ummongem iti uneg ti balaymo ti ama ken inam, dagiti kakabsatmo ken amin a sangkabbalayan ti amam.
tikadzalowa mʼdzikoli, iwe udzamangirire kansalu kofiira pa zenera limene unatitulutsira, ndi kusonkhanitsa abambo ako, amayi ako, abale ako ndi banja lako lonse mʼnyumba muno.
19 Siasinoman a rumuar manipud kadagiti ruangan ti balaymo, addanto iti rabaw ti uloda iti darada ket awanto ti pakabasolanmi. Ngem no madangran ti siasinoman kadakayo iti uneg ti balay, ti darananto ket adda iti rabaw ti ulomi.
Ngati wina aliyense adzatuluka mʼnyumbamo kuti azikayendayenda mu msewu, magazi ake adzakhala pamutu pake, ife sitidzapalamula kanthu. Koma wina aliyense wokhala mʼnyumba mwakomo akadzaphedwa, mlandu udzakhala wathu.
20 Ngem no ibagam daytoy a rantami, awanto ngarud ti pagrebbenganmi a mangtungpal iti inkarimi.
Komanso iwe ukangowulula zimene ife tikuchitazi ndiye kuti ife sitidzasunga zimene talonjezazi.”
21 Simmungbat ni Rahab, “Mapasamak koma ti kinunayo.” Pinalubosanna ida ket pimmanawda. Ket nangigalut isuna iti nalabaga a tali iti tawa.
Rahabe anayankha kuti, “Zikhale monga mwaneneramo.” Kenaka iye anawatulutsa ndipo iwowo anapita. Pambuyo pake Rahabe anamangirira kansalu kofiira pa zenera paja.
22 Pimmanawda ket napanda idiay turturod ket nagtalinaedda sadiay iti tallo nga aldaw agingga a nagsubli dagiti mangkamkamat kadakuada. Sinapsapul ida dagiti mangkamkamat kadagiti daldalan ngem awan ti nasarakanda.
Azondi aja anachoka napita ku mapiri ndipo anakhalako masiku atatu. Apa nʼkuti otumidwa ndi mfumu aja atawafunafuna ponseponse nʼkubwerera osawapeza.
23 Nagsubli dagiti dua a lallaki ket nagballasiwda a nagsublida kenni Josue nga anak ni Nun, ket imbagada kenkuana amin a napasamak kadakuada.
Pambuyo pake azondi awiri aja anayamba ulendo wobwerera kwawo. Anatsika ku mapiri kuja, nawoloka mtsinje mpaka anakafika kwa Yoswa mwana wa Nuni. Ndipo anamuwuza zonse zimene zinawachitikira.
24 Ket kinunada kenni Josue, “Pudno nga inted ni Yahweh daytoy a daga kadatayo. Agrunrunaw amin nga agnanaed iti daydiay a daga gapu kadatayo.
Iwo anati kwa Yoswa, “Ndithu, Yehova wapereka dziko lonse mʼmanja mwathu. Anthu onse kumeneko akuchita nafe mantha.”

< Josue 2 >