< Job 33 >
1 Isu nga ita, Job, agpakaasiak kenka, denggem ti ibalikasko; dumngegka kadagiti amin a sasaok.
“Koma tsopano, inu abambo Yobu chonde mverani mawu anga; mutcherere khutu zonse zimene ndinene.
2 Kitaem ita, inyungapkon dagiti ngiwatko; nagsaon ti dilak iti ngiwatko.
Tsopano ndiyamba kuyankhula; mawu anga ali pa msonga ya lilime langa.
3 Iyebkas dagiti sasaok ti kinalinteg ti pusok; ti ammo ti bibigko, ibagada a sipupudno.
Mawu anga akuchokera mu mtima wolungama; pakamwa panga pakuyankhula zoonadi zimene ndikuzidziwa.
4 Inaramidnak ti Espiritu ti Dios; ti anges ti Mannakabalin amin ket inikkannak iti biag.
Mzimu wa Mulungu wandiwumba, mpweya wa Wamphamvuzonse umandipatsa moyo.
5 No kabaelam, sungbatannak; isaganam dagiti sasaom iti sangoanak ket tumakderka.
Mundiyankhe ngati mungathe; konzekani tsopano kuti munditsutse.
6 Kitaem, agpadata iti imatang ti Dios; nasukogak met manipud iti dadamilien a daga.
Ine ndili monga inu pamaso pa Mulungu; nanenso ndinachokera ku dothi.
7 Kitaem, ti pangbutengko ket saannaka a pagbutngen; wenno ti panangtalmegko ket saan a mangpadagsen kenka.
Musachite mantha ndipo musandiope ayi, Ine sindikupanikizani kwambiri ayi.
8 Pudno a nagsaoka iti panagdengngegko; nangngegko ti timek dagiti sasaom a mangibagbaga,
“Koma inu mwayankhula ine ndikumva, ndamva mawu anuwo onena kuti,
9 'Nadalusak ken awan ti naglabsingak; awan dakes nga aramidko ken awan ti basolko.
‘Ndine wolungama mtima ndi wopanda tchimo; ndine woyera mtima ndipo ndilibe cholakwa.
10 Kitaem, agsapsapul ti Dios iti gundaway a mangdarup kaniak; ibilbilangnak a kas kabusorna.
Komatu Mulungu wapeza zifukwa zoti anditsutsire nazo; Iye akundiyesa ngati mdani wake.
11 Kawkawaranna dagiti sakak; sipsiputanna ti amin a dalanko.
Iyeyo wamanga mapazi anga mʼzigologolo, akulonda mayendedwe anga onse.’
12 Kitaem, sungbatankanto: biddut ti panangibagam iti daytoy, ta natantan-ok ti Dios ngem iti tao.
“Koma ine ndi kuti kwa inu, inuyo simukukhoza pa zimenezi, pakuti Mulungu ndi wamkulu kupambana munthu.
13 Apay a makisuppiatka kenkuana? Saan a masapul nga ipalawagna iti aniaman kadagiti ar-aramidenna.
Chifukwa chiyani mukudandaula kwa Iye kuti sayankha mawu ena aliwonse a munthu?
14 Ta agsasao ti Dios iti maminsan— wen, mamindua uray no saan a madlaw ti tao daytoy.
Pajatu Mulungu amayankhula mwa njira zosiyanasiyana, ngakhale munthu sazindikira zimenezi.
15 Iti tagtagainep, iti sirmata iti rabii, no narnekanen ti turog dagiti tattao, iti pannakairedep iti pagiddaan—
Mʼmaloto, mʼmasomphenya usiku, pamene anthu ali mʼtulo tofa nato pamene akungosinza chabe pa bedi,
16 ket luklukatan ti Dios dagiti lapayag dagiti tattao, ken butbutngenna ida babaen kadagiti pangta,
amawanongʼoneza mʼmakutu ndi kuwaopseza ndi machenjezo ake,
17 tapno guyudenna ti tao manipud iti panagbasbasolna, ken iyadayona ti kinatangsit kenkuana.
kumuchotsa munthu ku zoyipa, ndi kuthetseratu kunyada kwake,
18 Iyad-adayo ti Dios ti biag ti tao manipud iti abot, ti biagna manipud iti ibaballasiw iti patay.
kumulanditsa munthu ku manda, kuti moyo wake usawonongeke ndi lupanga.
19 Nadusa pay ti tao iti ut-ot iti pagiddaanna, nga addaan iti agtultuloy nga ut-ot kadagiti tulangna,
“Mwina Mulungu amalanga munthu ndi matenda ndi ululu ali pa bedi pake, nthawiyo thupi lake lonse limangophwanya,
20 tapno kagura ti biagna ti taraon, ken kagura ti kararuana dagiti naisangsangayan a taraon.
kuti asakhalenso ndi chilakolako cha chakudya, ndipo amanyansidwa ndi chakudya chabwino chomwe.
21 Umres ti lasagna tapno saanen a makita; dagiti tulangna, a saan idi a makita, ita agparangdan.
Thupi lake limawonda ndipo mafupa ake, omwe anali obisika, tsopano amaonekera poyera.
22 Agpayso, umas-asidegen ti kararuana iti abot, ti biagna kadagidiay nga agtarigagay a mangdadael iti daytoy.
Munthuyo amayandikira ku manda, moyo wake umayandikira kwa amene amabweretsa imfa.
23 Ngem no adda anghel nga agbalin a mangibabaet para kenkuana, maysa manipud kadagiti rinibribu nga anghel tapno ipakitana kenkuana ti umno nga aramidenna,
“Koma patakhala mngelo ngati mthandizi, mmodzi mwa ambirimbiri oterewa, adzafotokoza zimene zili zoyenera,
24 ket no naasi ti anghel kenkuana ket ibagana iti Dios, 'Isalakanmo daytoy a tao iti pannakatnagna iti abot; nakasarakak iti pangsubbot kenkuana,'
kudzamukomera mtima ndi kunena kuti, ‘Mupulumutseni kuti asapite ku manda; ine ndapeza cholowa mʼmalo mwa moyo wake,’
25 ket agbalinto a nalaslasbang ti lasagna ngem iti lasag ti ubing; agsubli isuna kadagiti aldaw ti kabanbannuaganna.
pamenepo thupi lake lidzasanduka lasee ngati la mwana; ndipo adzabwezeretsedwanso kukhala ngati mʼmasiku a unyamata wake.
26 Agkararag isuna iti Dios ket maasinto ti Dios kenkuana, tapno makitkitana ti rupa ti Dios nga addaan iti rag-o. Itedto ti Dios ti balligi iti tao.
Akapemphera kwa Mulungu, iyeyo adzalandiridwa. Mulungu adzamulandira mwa chimwemwe ndipo adzamubwezeretsa pamalo ake oyamba.
27 Ket agkantanto dayta a tao iti sangoanan dagiti dadduma a tattao ket ibagana, 'Nagbasolak ken sinalungasingko ti pudno, ngem saan a nadusa ti basolko.
Ndipo adzabwera kwa anzake ndi kunena kuti, ‘Ndinachimwa ndipo sindinachite zolungama, koma sindinalangidwe koyenerana ndi kuchimwa kwanga.
28 Inispal ti Dios ti kararuak iti pannakatnagna iti abot; agtultuloy a makakita ti biagko iti lawag.'
Iye anapulumutsa moyo wanga kuti usapite ku manda, ndipo ndidzakhala ndi moyo ndi kuonanso kuwala kwa dzuwa.’
29 Kitaem, ar-aramiden ti Dios amin dagitoy a banbanag iti tao, mamindua, wen, mamitlo pay a daras,
“Mulungu amachita zonsezi kwa munthu kawirikawiri,
30 tapno maisubli ti kararuana manipud iti abot, tapno malawlawagan isuna babaen iti silaw ti biag.
kupulumutsa moyo wa munthuyo ku manda, kuti athe kuonanso kuwala kwa moyo.
31 Ipangagmo Job, ken denggennak; agulimekka ta agsaoak.
“Abambo Yobu, tcherani khutu ndipo mundimvere; khalani chete kuti ndiyankhule.
32 No adda ibagam, sungbatannak; agsaoka, ta kayatko a paneknekan nga addaka iti umno.
Ngati muli nʼchoti munene, ndiyankheni; yankhulani, pakuti ine ndikufuna mupezeke wolungama.
33 No saan, denggennak ngarud; agulimekka latta, ket isurok kenka ti kinasirib.”
Koma ngati sichoncho, mundimvere; khalani chete ndipo ine ndidzakuphunzitsani nzeru.”