< Job 26 >

1 Kalpasanna simmungbat ni Job ket kinunana,
Pamenepo Yobu anayankha kuti,
2 “Anian a panangtulongmo iti tao nga awan pannakabalinna! Anian a panangisalakanmo iti takkiag nga awanan pigsa!
“Wamuthandizadi munthu wopanda mphamvu! Walimbitsadi dzanja la munthu wofowoka!
3 Anian a panangbalakadmo iti tao a nakuneng ket imbagam kenkuana ti nagsayaat a pannakaamo!
Wapereka malangizo kwa munthu amene alibe nzeru! Ndipotu waonetsadi nzeru zochuluka!
4 Siasino ti akintulong nga imbagam dagitoy a sasao? Siasino ti akin-espiritu daytoy a rimuar kenka?
Kodi wakuthandiza ndani kuti uyankhule mawu awa? Ndipo ndi mzimu wa yani umene unayankhula pakamwa pako?
5 Simmungbat ni Bildad, “Agpigerger dagiti pimmusayen, dagiti linong, dagiti agnanaed iti uneg dagiti dandanum.
“Mizimu ya anthu akufa ikunjenjemera pansi pa madzi, ndi zonse zokhala mʼmadzimo.
6 Lamo-lamo ti sheol iti sangoanan ti Dios; ti pannakadadael ket awan pangabbongna a maibusor kenkuana. (Sheol h7585)
Dziko la anthu akufa ndi lapululu pamaso pa Mulungu; chiwonongeko ndi chosaphimbidwa. (Sheol h7585)
7 Binbinatenna ti amianan iti rabaw ti awan nagyanna a law-ang ken ibitbitinna ti lubong iti awan.
Mulungu anayala thambo la kumpoto pa phompho; Iye anakoloweka dziko lapansi mʼmalo mwake pamene panali popanda nʼkanthu komwe.
8 Bungbungonenna dagiti danum kadagiti napuskol nga ulepna, ngem saan a mapisang dagiti ulep iti babaen dagitoy.
Amasunga madzi ambiri mʼmitambo yake, koma mitamboyo siphulika chifukwa cha kulemera kwa madziwo.
9 Ab-abbonganna ti rupa ti bulan ken iwarwarasna dagiti ulepna iti daytoy.
Iye amaphimba mwezi wowala, amawuphimba ndi mitambo yake.
10 Nangikitikit isuna ti nagbukel a beddeng iti rabaw dagiti dandanum kas linya iti nagbaetan ti lawag ken ti sipnget.
Mulungu anawalembera madzi malire wonga uta, kukhala malire pakati pa kuwunika ndi mdima.
11 Agkintayeg dagiti adigi ti langit ken agsiddaawda iti panangtubngarna.
Mizati yochirikiza mitambo yakumwamba imanjenjemera, ndi kudabwa pa kudzudzula kwake.
12 Pinatalinaayna ti baybay babaen iti pannakabalinna; dinadaelna ni Rahab babaen iti pannakaawatna.
Ndi mphamvu zake anatontholetsa nyanja; ndi nzeru zake anakantha chirombo cha mʼmadzi chija chotchedwa Rahabe.
13 Babaen iti angesna, winaknitanna dagiti langit kadagiti bagyo; nawaknitan dagiti langit manipud kadagiti bagyo; sinalput dagiti imana ti agliblibas nga uleg.
Ndi mpweya wake anayeretsa zamumlengalenga, dzanja lake linapha chinjoka chothawa chija.
14 Adtoy, babassit laeng dagitoy a paset dagiti wagasna; anian a nagkapsut nga arasaas ti mangmangegtayo kenkuana! Siasino ti makaawat iti gurruod ti pannakabalinna?”
Zimenezi ndi pangʼono chabe mwa ntchito yake; tingomva pangʼono za Iye ngati kunongʼona! Kodi ndani angathe kudziwa kukula kwa mphamvu zake?”

< Job 26 >