< Jeremias 4 >

1 No agsublikayo, Israel—kastoy ti pakaammo ni Yahweh— siak ti rumbeng a pagsublianyo. No ikkatenyo dagiti makarimon a banbanagyo iti imatangko, ken saandak manen a tallikudan,
“Ngati mukufuna kubwerera, inu Aisraeli, bwererani kwa Ine,” akutero Yehova. “Chotsani mafano anu onyansa pamaso panga ndipo musasocherenso.
2 ken no isapatayo, ‘adda kenni Yahweh ti kinapudno, hustisia, ken kinalinteg,' kiddawento dagiti nasion ti bendisionko, ken idayawdakto.
Muzilumbira mokhulupirika ndiponso mwa chilungamo kuti, ‘Pali Yehova wamoyo.’ Mukatero anthu a mitundu ina yonse adzandipempha kuti ndiwadalitse ndipo adzanditamanda.”
3 Ta kastoy ti kuna ni Yahweh iti tunggal maysa a tattao iti Juda ken Jerusalem. ‘Aradwenyo ti bukodyo a daga, ken saankayo nga agmula kadagiti kasisiitan.
Zimene Yehova akunena kwa anthu a ku Yuda ndi a ku Yerusalemu ndi izi: “Limani masala anu musadzale pakati pa minga.
4 Makugitkayo koma kenni Yahweh ken ikkatenyo dagiti akin-rabaw a kudil dagiti pusoyo, lallaki ti Juda ken dakayo nga agnanaed iti Jerusalem, ta no saan, gumil-ayabto a kasla apuy ti rungsotko ken manguram nga awan ti uray siasino a makaiddep iti daytoy. Mapasamakto daytoy gapu iti kinadakes dagiti aramidyo.
Dziperekeni nokha kwa Ine kuti munditumikire ndi mtima wanu wonse, inu anthu a ku Yuda ndi ku Yerusalemu. Muzichita zimenezi kuopa kuti mkwiyo wanga ungabuke ngati moto ndi kukutenthani, chifukwa cha ntchito zanu zoyipazo popanda wina wowuzimitsa.
5 Ipakaammoyo idiay Juda ken ipangngegyo iti Jerusalem. Kunaenyo, “Pagunienyo ti tangguyob iti daga.” Iwaragawagyo, “Aguummongkayo.” Mapantayo kadagiti nasarikedkedan a siudad.”
“Lengeza ku Yuda ndi kulalikira mu Yerusalemu kuti, ‘Lizani lipenga mʼdziko lonse!’ Ndipo fuwulani kuti, ‘Sonkhanani! Tiyeni tithawire ku mizinda yotetezedwa!’
6 Itag-ayyo ti bandera a pagilasinan ket iturongyo idiay Sion, ken tumaraykayo tapno natalgedkayo! Saankayo nga agtalinaed, ta mangiyegak iti didigra manipud amianan ken dakkel a pannakarebba.
Kwezani mbendera kuyangʼana ku Ziyoni! Musachedwe, thawani kuti mupulumuke! Pakuti Ine ndikubweretsa chilango kuchokera kumpoto, kudzakhala chiwonongeko choopsa.”
7 Rummuarto iti maysa a leon manipud kasamekan, ken agsagsaganan ti maysa a mangdadaelto kadagiti nasion. Pumanaw isuna iti lugar nga ayanna tapno mangiyeg ti nakaal-alinggaget a pasamak iti dagayo, dadaelenna dagiti siudadyo, ket awanto ti agnaed.
Monga mkango umatulukira mʼngaka yake momwemonso wowononga mayiko wanyamuka ndi kutuluka ku mbuto yake. Watero kuti awononge dziko lanu. Mizinda yanu idzakhala mabwinja popanda wokhalamo.
8 Gapu iti daytoy, balkotenyo ti bagbagiyo iti nakersang a lupot, agdung-aw ken aganug-ogkayo. Ta saan a timmalikud kadatayo ti rungsot ti pungtot ni Yahweh.
Choncho valani ziguduli, lirani ndi kubuwula, pakuti mkwiyo waukulu wa Yehova sunatichokere.
9 Ket mapasamakto iti dayta nga aldaw, —kastoy ti pakaammo ni Yahweh— a matayto ti puso dagiti ari ken dagiti opisialna. Makigtotto dagiti padi, ken mapabutnganto dagiti profeta.
“Pa tsiku limenelo, mfumu ndi nduna zake adzataya mtima, ansembe adzachita mantha kwambiri, ndipo aneneri adzathedwa nzeru,” akutero Yehova.
10 Isu a kinunak, “O! Yahweh nga Apo. Pudno nga inallilawmo a naminpinsan dagitoy a tattao ken ti Jerusalem babaen iti panangibagam, ‘Maaddaankayonto iti kappia.' Idinto a silalayat ti kampilan a maibusor iti biagda.
Ndipo ine ndinati, “Haa, Ambuye Yehova, ndithu munawanyenga anthu awa pamodzi ndi Yerusalemu pamene munanena kuti, ‘Mudzakhala pa mtendere,’ chonsecho lupanga lili pakhosi pathu.”
11 Iti dayta a tiempo maibaganto ti kastoy kadagitoy a tattao ken iti Jerusalem “Ti nabara nga angin manipud kadagiti patad ti let-ang ket agturongto kadagiti annak a babbai dagiti tattaok. Saannanto ida a taepan wenno dalusan.
Nthawi imeneyo anthu awa ndi Yerusalemu adzawawuza kuti, “Mphepo yotentha yochokera ku magomo a mʼchipululu ikuwomba pa anthu anga, osati mphepo yopeta kapena yoyeretsa;
12 Addanto iti angin a napigpigsa nga adayo ngem iti dayta nga angin nga umay babaen ti bilinko, ket iyulogkon ti panangukomko kadakuada.
koma mphepo yamphamvu kwambiri yochokera kwa Ine. Tsono ndi Ineyo amene ndikuwaweruza.”
13 Kitaenyo, ruma-ut isuna a kasla ulep, ken kasla bagyo dagiti karwahena. Naparpartak dagiti kabaliona ngem kadagiti agila. Asitayo pay, ta madadaeltayonto!
Taonani, adani akubwera ngati mitambo, magaleta awo akubwera ngati kamvuluvulu, akavalo awo ndi aliwiro kupambana chiwombankhanga. Tsoka ilo! Tawonongeka!
14 O Jerusalem, dalusanyo dagiti pusoyo manipud iti kinadangkes, tapno maisalakankayo. Kaanonto pay ti panagsardengyo iti panangpanpanunotyo no kasano ti agbasol?
Iwe Yerusalemu, tsuka mtima wako kuchotsa zoyipa kuti upulumuke. Kodi maganizo ako oyipawo udzakhala nawo mpaka liti?
15 Ta addanto timek a mangiyeg iti damag manipud Dan, ken mangngeg ti um-umay a didigra manipud kadagiti kabanbantayan ti Efraim.
Pakuti amithenga akulalika mawu mʼdziko la Dani; akulengeza za masautso kuchokera ku mapiri a Efereimu.
16 Bay-am a panunoten dagiti nasion ti maipanggep iti daytoy: Denggem, ibagam iti Jerusalem nga um-umayen dagiti manglakub manipud iti adayu a daga a mangipukkaw iti gubat a maibusor kadagiti siudad ti Juda.
Iwo akuti, “Fotokozani zimenezi kwa anthu a mitundu ina, lengezani zimenezi mu Yerusalemu kuti, ‘Ankhondo akubwera kuchokera ku dziko lakutali, akufuwula ndi kudzazinga mizinda ya Yuda.
17 Maiyarigdanto kadagiti agwanwanawan iti naaradon a talon a nangpalawlaw iti daytoy, agsipud ta nagsukir daytoy kaniak—kastoy ti pakaammo ni Yahweh—
Azinga Yerusalemu ngati anthu olondera munda, chifukwa Yerusalemu wandiwukira,’” akutero Yehova.
18 ken ti kababalin ken ar-aramidmo ti makagapu a mapasamak dagitoy kenka. Kastoyto ti dusam. Anian a nakaam-amakto daytoy! Dangrannanto ti mismo a pusom.
“Makhalidwe anu ndi zochita zanu zakubweretserani zimenezi. Chimenechi ndiye chilango chanu. Nʼchowawa kwambiri! Nʼcholasa mpaka mu mtima!”
19 O pusok! O pusok! Agsansanaang daytoy pusok. Mariribukan daytoy pusok. Saanak a makatalna ta mangmangngegko ti uni ti tangguyob, ti pakdaar ti gubat.
Mayo, mayo, ndikumva kupweteka! Aa, mtima wanga ukupweteka, ukugunda kuti thi, thi, thi. Sindingathe kukhala chete. Pakuti ndamva kulira kwa lipenga; ndamva mfuwu wankhondo.
20 Pannakarebba ken pannakarebba ti maiwarwaragawag, ta kellaat a nadadael ti entero a daga. Naminpinsan a dinadaelda ti tabernakulok ken ti toldak.
Tsoka limatsata tsoka linzake; dziko lonse lasanduka bwinja. Mwadzidzidzi matenti athu awonongedwa, mwa kanthawi kochepa nsalu zake zotchinga zagwetsedwa.
21 Kasano pay ngata kabayag a kitkitaek ti bandera? Mangngegkonto kadi pay ti uni ti tangguyob?
Kodi ndikhale ndikuona mbendera ya nkhondo, ndi kumva kulira kwa lipenga mpaka liti?
22 Ta iti kinamaag dagiti tattaok—saandak nga am-ammo. Nakunengda a tattao ken awan pannakaawatda. Nalaingda no maipapan iti kinadakes, ngem awan ammoda nga agaramid iti kina-imbag.
Yehova akuti, “Anthu anga ndi zitsiru; iwo sandidziwa. Iwo ndi ana opanda nzeru; samvetsa chilichonse. Ali ndi luso lochita zoyipa, koma sadziwa kuchita zabwino.”
23 Nakitak ti daga, ket anian! Awan langlangana ken unga-ong daytoy. Ta awan silaw dagiti langit.
Ndinayangʼana dziko lapansi, ndipo linali lopanda anthu ndi lopanda kanthu; ndinayangʼana thambo, koma linalibe kuwala kulikonse.
24 Kimmitaak kadagiti kabanbantayan. Nakitak nga agkinkintayeg ken aggungungon dagiti turod.
Ndinayangʼana mapiri, ndipo ankagwedezeka; magomo onse ankangosunthira uku ndi uku.
25 Kimmitaak. Adtoy, awan uray maysa a tao, ken timmayab amin a billit ti langit.
Ndinayangʼana, ndipo sindinaone anthu; mbalame iliyonse ya mlengalenga inali itathawa.
26 Kimmitaak. Nakitak a nagbalin a let-ang ti minuyongan ken narba amin dagiti siudad iti sangoanan ni Yahweh, gapu iti rungsot ti pungtotna.”
Ndinayangʼana, dziko lachonde linali litasanduka chipululu; mizinda yake yonse inali itasanduka bwinja pamaso pa Yehova, chifukwa cha mkwiyo wake.
27 Kastoy ti kuna ni Yahweh, “Madadaelto ti daga, ngem saankonto a dadaelen a naan-anay daytoy.
Yehova akuti, “Dziko lonse lidzasanduka chipululu komabe sindidzaliwononga kotheratu.
28 Gapu iti daytoy, agladingitto ti daga, ken agsipngetto ti tangatang. Ta impakaammokon ti panggepko; ipatungpalko; Saanakto nga agsanud a mangipatungpal kadagitoy.
Chifukwa chake dziko lapansi lidzalira ndipo thambo lidzachita mdima, pakuti ndayankhula ndipo sindidzafewa mtima, ndatsimikiza ndipo sindidzabwerera mʼmbuyo.”
29 Itarayanto ti tunggal siudad ti arimpadek dagiti kumakabalio ken dagiti pumapana; tumaraydanto kadagiti kabakiran. Kumalay-atto ti tunggal siudad kadagiti kabatbattoan a luglugar. Mabaybay-anto dagiti siudad, ta awanto ti uray maysa nga agtaeng kadagitoy.
Pakumva phokoso la okwera pa akavalo ndi la anthu oponya mivi, anthu a mʼmizinda adzathawa. Ena adzabisala ku nkhalango; ena adzakwera mʼmatanthwe mizinda yonse nʼkuyisiya; popanda munthu wokhalamo.
30 Ita ta nadadaelkan, ania ti aramidem? Ta uray agkaweska iti nalabbaga a kawes, arkusam ti bagim iti alahas a balitok, ken padakkelem ti matam babaen iti pinta, saandakan a kayat ita dagiti lallaki a nagderrep kenka. Ngem ketdi, kayatda a pukawen ti biagmo.
Iwe Yerusalemu, ndiwe bwinja! Ukutanthauza chiyani kuvala zovala zofiira ndi kuvalanso zokometsera zagolide? Ngakhale udzikonze maso ako powapaka zokometsera, ukungodzivuta chabe. Zibwenzi zako zikukunyoza; zikufuna kuchotsa moyo wako.
31 Isu a mangngegko ti uni ti asug, tuok a kas iti agpasngay iti inauna nga anak, ti timek ti babai nga anak ti Sion. Agang-angsab isuna. Iyukradna dagiti imana, ' Asi-ak pay! Matallimudawak gapu kadagitoy a mammapatay.”'
Ndikumva kulira ngati kwa mayi pa nthawi yake yobereka, kubuwula ngati kwa mayi amene akubereka mwana wake woyamba. Kuliraku ndi kwa anthu a mu Ziyoni, wefuwefu. Atambalitsa manja awo nʼkumati, “Kalanga ife! Tikukomoka. Moyo wathu waperekedwa kwa anthu otipha.”

< Jeremias 4 >