< Jeremias 37 >

1 Ita, nagturay a kas ari ni Zedekias a putot ni Josias a saan ket a ni Jeconias a putot ni Jehoiakim. Insaad ni Nebucadnesar nga ari ti Babilonia ni Zedekias a kas ari iti entero a daga ti Juda.
Nebukadinezara mfumu ya Babuloni, inakhazika pa mpando waufumu Zedekiya mwana wa Yosiya kukhala mfumu ya Yuda. Iye analowa mʼmalo mwa Yehoyakini mwana wa Yehoyakimu.
2 Ngem saan a dimngeg ni Zedekias, dagiti adipenna ken dagiti tattao iti daga, kadagiti sasao ni Yahweh nga impakaammona babaen kadagiti ima ni Jeremias a profeta.
Koma Zedekiya kapena atumiki ake ngakhalenso anthu a mʼdzikomo sanasamalire mawu a Yehova amene anayankhula kudzera mwa mneneri Yeremiya.
3 Nangipatulod ngarud da ari Zedekias, Jehucal a putot ni Selemias, ken Sofonias a putot ni Maaseias a padi iti mensahe kenni Jeremias a profeta. Kinunada, “Ikararagandakami kenni Yahweh a Diostayo.”
Tsono Zedekiya anatuma Yehukali mwana wa Selemiya ndi wansembe Zefaniya mwana wa Maseya kwa mneneri Yeremiya ndi uthenga uwu: “Chonde tipempherereni kwa Yehova Mulungu wathu.”
4 Ita, nawaya pay laeng a makilangen-langen ni Jeremias kadagiti tattao, ta saan pay isuna a naibalud.
Nthawi imeneyinso nʼkuti Yeremiya ali ndi ufulu woyenda pakati pa anthu chifukwa anali asanaponyedwe mʼndende.
5 Rimmuar ti armada ni Faraon iti Egipto, ket nadamag dagiti Caldeo a manglaklakub iti Jerusalem ti maipanggep kadakuada ket pinanawanda ti Jerusalem.
Nthawi imeneyinso nʼkuti gulu lankhondo la Farao litatuluka mʼdziko la Igupto. Ndipo Ababuloni amene anali atazinga Yerusalemu atamva zimenezi, anachoka ku Yerusalemuko.
6 Ket immay ti sao ni Yahweh kenni Jeremias a profeta a kinunana,
Tsono Yehova anawuza mneneri Yeremiya kuti,
7 “Ni Yahweh a Dios ti Israel, kastoy ti kunana: Daytoy ti ibagamto iti ari ti Juda, gapu ta imbaonnaka a dumawat iti balakad manipud kaniak, “Kitaem, ti armada ni Faraon nga immay a tumulong kadakayo, ket pasublin idiay Egipto, a bukodda a daga.
“Uyiwuze mfumu ya Yuda imene inakutuma kuti udzapemphe nzeru kwa ine kuti Ine Yehova, Mulungu wa Israeli ndikuti, gulu lankhondo la Farao limene linatuluka kuti lidzakuthandize lidzabwerera kwawo ku Igupto.
8 Agsublinto dagiti Caldeo. Gubatendanto daytoy a siudad, sakupen, ken puorandanto daytoy.
Ndipo Ababuloni adzabwerera kudzathira nkhondo mzinda uno. Iwo adzawugonjetsa ndi kuwutentha.
9 Kastoy ti kuna ni Yahweh: Saanyo nga allilawen dagiti bagbagiyo babaen iti panangibagbagayo, 'Awan duadua a panawandatayo dagiti Caldeo,' ta saandanto a pumanaw.
“Yehova akuti: Musadzinyenge, nʼkumaganiza kuti, ‘Ndithu Ababuloni adzatisiya.’ Ndithudi sadzakusiyani!
10 Uray no maparmekyo ti entero nga armada dagiti Caldeo a makiranget kadakayo tapno dagitinto laeng nasugatan a lallaki ti mabati kadagiti toldada, bumangondanto ket puoranda daytoy a siudad.”
Ngakhale mutagonjetsa gulu lonse lankhondo la Ababuloni limene likukuthirani nkhondo ndipo mʼmatenti mwawo ndikutsala anthu ovulala okhaokha, amenewo adzabwera ndi kudzatentha mzinda uno.”
11 Isu nga idi pimmanawen ti armada dagiti Caldeo iti Jerusalem bayat nga um-umay ti armada ni Faraon,
Gulu lankhondo la Ababuloni litaleka kuthira nkhondo mzinda wa Yerusalemu chifukwa choopa gulu lankhondo la Farao,
12 ket rimmuar ni Jeremias iti Jerusalem tapno mapan idiay daga ti Benjamin. Kayatna ti mangtagikua iti paset ti daga sadiay, nga isu iti ayan dagiti tattaona.
Yeremiya ananyamuka kuchoka ku Yerusalemu ndi kumapita ku dziko la Benjamini kuti akalandire gawo lake la minda ya makolo ake.
13 Bayat iti kaaddana iti Ruangan ti Benjamin, maysa a panguloen dagiti agbanbantay ti adda sadiay. Ti naganna ket Jerias, ket putot isuna ni Selemias a putot ni Hananias. Ginammatanna ni Jeremias a profeta ket kinunana, “Mapanka tumipon kadagiti Caldeo, ania!”
Koma atafika pa Chipata cha Benjamini, mkulu wa alonda amene dzina lake linali Iriya mwana wa Selemiya, mwana wa Hananiya, anagwira mneneri Yeremiyayo ndipo anati, “Iwe ukuthawira kwa Ababuloni!”
14 Ngem kinuna ni Jeremias, “Saan a pudno dayta. Saanak a mapan tumipon kadagiti Caldeo.” Ngem saan a dimngeg ni Jerias kenkuana. Ingguyodna ni Jeremias ket impanna kadagiti opisial.
Yeremiya anati, “Zimenezo si zoona! Ine sindikuthawira kwa Ababuloni.” Koma Iriya sanamumvere. Mʼmalo mwake anagwira Yeremiya nʼkupita naye kwa akuluakulu.
15 Nakaunget dagiti opisial kenni Jeremias. Sinapsaplitda ken imbaludda isuna iti balay ni Jonatan nga eskriba, ta pinagbalinda daytoy a pagbaludan.
Akuluakuluwo anamupsera mtima Yeremiya ndipo anamukwapula ndi kumuyika mʼnyumba ya mlembi Yonatani, imene anayisandutsa ndende.
16 Naibalud ngarud ni Jeremias iti pagbaludan nga adda iti uneg ti daga, a nagtalinaedanna iti adu nga al-aldaw.
Yeremiya anayikidwa mʼndende ya pansi pa nthaka, kumene anakhalako nthawi yayitali.
17 Ket nangibaon ni Ari Zedekias iti maysa a tao a mangiyeg kenkuana iti palasio. Iti balayna, nalimed a sinaludsod kenkuana ti ari, “Adda kadi sao manipud kenni Yahweh?” Simmungbat ni Jeremias, “Adda iti sao: “Maiyawatkanto iti ima ti ari ti Babilonia.”
Kenaka Mfumu Zedekiya inatuma anthu kuti akayitane Yeremiya ndipo anabwera naye ku nyumba ya mfumu. Atafika mfumu inamufunsa mwamseri kuti, “Kodi pali mawu ena amene Yehova wakuwuza?” Yeremiya anayankha kuti, “Inde. Inu mfumu mudzaperekedwa kwa mfumu ya ku Babuloni.”
18 Ket kinuna ni Jeremias kenni Ari Zedekias, “Ania ti nakabasolak kenka, kadagiti adipenmo wenno kadagitoy a tattao tapno ibaluddak?
Pamenepo Yeremiya anafunsa Mfumu Zedekiya kuti, “Kodi ndakulakwirani chiyani inuyo kapena akuluakulu anu kapenanso anthu awa, kuti mundiyike mʼndende?
19 Sadino ti ayan dagiti profetam, dagidiay nagipadto para kenka ken nagkuna a saan nga umay ti ari ti Babilonia a maibusor kenka wenno maibusor iti daytoy a daga?
Kodi ali kuti aneneri anu amene anakuloserani kuti, ‘Mfumu ya ku Babuloni sidzakuthirani nkhondo pamodzi ndi dziko lino’?
20 Ngem ita dumngegka, apok nga ari! Patgam koma dagiti kiddawko iti sangoanam. Saannak koma nga isubli iti balay ni Jonatan nga eskriba, ta no isublinak sadiay, matayak.”
Koma tsopano, mbuye wanga mfumu, chonde tamverani. Loleni ndinene pempho langa pamaso panu: Musandibwezere ku nyumba ya mlembi Yonatani, kuopa kuti ndingakafere kumeneko.”
21 Nangted ngarud ni Zedekias iti bilin. Inkabil dagiti adipenna ni Jeremias iti paraangan nga ayan dagiti agbanbantay. Inaldaw a maik-ikkan isuna iti tinapay manipud iti kalsada dagiti panadero, agingga a naibus dagiti tinapay iti siudad. Nagtalinaed ngarud ni Jeremias iti paraangan nga ayan dagiti agbanbantay.
Tsono Mfumu Zedekiya analamula kuti Yeremiya asungidwe mʼbwalo la alonda. Ankamupatsa buledi tsiku ndi tsiku amene ankamugula kwa ophika buledi. Anapitiriza kutero mpaka buledi yense anatha mu mzindamo. Choncho Yeremiya anapitirira kukhala mʼbwalo la alonda.

< Jeremias 37 >