< Jeremias 3 >

1 “Kunada, 'Adda maysa a lalaki a mangpatpatalaw iti asawana, isu a pimmanaw ti babai ket nagbalin nga asawa ti sabali a lalaki. Rumbeng kadi a sublien ti lalaki ti babai? Saan kadi a naan-anayen a narugit ti babai?' Dayta a babai ket daytoy a daga! Nagtignayka a kas iti balangkantis nga addaan iti adu a kaayan-ayat, ket ita kayatmo ti agsubli kaniak? —kastoy ti pakaammo ni Yahweh.
“Ngati munthu asudzula mkazi wake ndipo mkaziyo nʼkuchoka nakakwatiwa ndi mwamuna wina, kodi mwamuna woyambayo angathe kumutenganso mkaziyo? Kodi atatero sindiye kuti dzikolo layipitsidwa kwambiri? Koma iwe Israeli wachita zadama ndi zibwenzi zambiri. Komabe bwerera kwa ine,” akutero Yehova.
2 Tumangadka ket kumitaka kadagiti tapaw dagiti turod! Sadino ti saanmo a nakikaiddaan? Nagtugawka kadagiti igid dagiti daldalan a mangur-uray kadagiti kaayan-ayatmo, a kasla ka la tulisan nga agpadpadaan idiay let-ang. Tinulawam ti daga iti kinabalangkantis ken kinadangkesmo.
“Tayangʼana ku zitunda zowuma. Kodi aliponso malo ena amene iwe sunachitepo zadama? Iwe unkakhala mʼmbali mwa njira kumadikira zibwenzi zako, ngati Mluya wobisalira anthu mʼchipululu. Inu mwayipitsa dziko ndi zadama zanu ndi ntchito zanu zoyipa.
3 Isu a nalapdan dagiti arbis ken saan a nagtinnag ti maudi a tudo. Ngem natangsit ta rupam a kas iti rupa ti balangkantis a babai. Saanmo ng ammo ti agbain.
Nʼchifukwa chake Yehova wayimitsa mvula, ndipo mvula ya nthawi ya masika sinagwe. Komabe uli ndi maonekedwe a mkazi wachiwerewere; ndipo sukuchita manyazi ndi pangʼono pomwe.
4 Manipud ita a tiempo, saankanto aya nga umawag kaniak a kunam, 'Amak! Sika ti kasingedan a gayyemko manipud pay kinaagtutubok.
Kodi iwe siposachedwa pomwepa pamene wanena kuti, ‘Abambo anga, Inu bwenzi langa la unyamata wanga,
5 Agnanayon kadi ti ungetmo? Pagtalinaedem kadi a kanayon ti ungetmo?' Dumngegka! Impakaammom nga agaramidka iti dakes, ket inaramidmo dayta. Itultuloymo ngarud nga aramiden dayta!”
kodi mudzandikwiyira nthawi zonse? Kodi ukali wanu udzakhalabe mpaka muyaya?’ Umu ndimo mmene umayankhulira, koma umapitirizabe kuchita zoyipa monga momwe umathera.”
6 Ket kinuna ni Yahweh kaniak kadagidi aldaw ni Josias nga ari, “Makitam kadi ti panangliput ti Israel kaniak? Mapan isuna iti tunggal nangato a bantay ken iti sirok ti tunggal nalangto a kayo, ket sadiay agtignay a kasla balangkantis a babai.
Pa nthawi ya Mfumu Yosiya Yehova anandiwuza kuti, “Kodi waona zomwe Israeli wosakhulupirika uja wachita? Anakwera pa phiri lililonse lalitali ndi kupita pa tsinde pa mtengo uliwonse wogudira kukapembedza. Choncho anachita za chiwerewere kumeneko.
7 Kinunak, 'Kalpasan a maaramidna amin dagitoy a banbanag, agsublinto isuna kaniak,' ngem saan nagsubli. Ket nakita ti nagulib a kabsatna a ni Juda ti inaramidna.
Ndinaganiza kuti atachita zonsezi, adzabwerera kwa Ine, koma sanabwerere, ndipo mlongo wake wosakhulupirika uja, Yuda, anaziona zimenezi.
8 Isu a nakitak a gapu kadagitoy amin a nakikamalala isuna. Managsukir nga Israel! Pinagtalawko isuna ket inikkak iti kasuratan ti panagsina. Ngem saan a nagbuteng ti nagulib a kabsatna a ni Juda, ket rimmuar ken nagtigtignay met a kas iti balangkantis a babai!
Anaona kuti ndinasudzula Israeli wosakhulupirikayo ndi kumupirikitsa chifukwa cha zigololo zake. Komabe Yuda mʼbale wake wosakhulupirika uja sanaope, nayenso anapita kukachita chigololo.
9 Awan aniamanna kenkuana a tinulawanna ti daga, isu a nagaramidda kadagiti bato ken kayo a didiosen.
Chiwerewere cha Israeli chinali chochititsa manyazi kotero kuti chinayipitsa dziko lonse. Anachita chigololo popembedza mafano a miyala ndi mitengo.
10 Ket kalpasan amin dagitoy, uray ti nagulib a kabsatna a ni Juda ket saan a nagsubli kaniak iti amin a pusona, no di ket naginsusubli! —kastoy ti pakaammo ni Yahweh.”
Israeli atachita zonsezi, Yuda mʼbale wake wosakhulupirika uja sanabwerere kwa Ine ndi mtima wake wonse, koma mwachiphamaso chabe,” akutero Yehova.
11 Ket kinuna ni Yahweh kaniak, “Nalinlinteg ti mangliliput nga Israel ngem iti nagulib a Juda!
Yehova anandiwuza kuti, “Kusakhulupirika kwa Israeli nʼkochepa kuyerekeza ndi kusakhulupirika kwa Yuda.
12 Mapanmo iwaragawag daytoy iti amianan. Kunaem, ''Agsublika, sika a mangliliput nga Israel! —kastoy ti pakaammo ni Yahweh—saanakto a kanayon a makaunget kenka. Agsipud ta napudnoak—kastoy ti pakaammo ni Yahweh—saanak nga agnanayon a makaunget.”
Pita ukalalikire kumpoto uthenga wakuti, “‘Israeli wosakhulupirikawe, bwerera,’ akutero Yehova. ‘Sindidzakukalipira mpaka kalekale, pakuti ndine wachifundo,’ akutero Yehova. ‘Sindidzakukwiyira mpaka kalekale.
13 Bigbigem ti basolmo, ta nagbasolka kenni Yahweh a Diosmo; nakinaigka kadagiti ganggannaet iti sirok dagiti nalalangto a kayo! Ta saanmo nga impangag ti timekko! —kastoy ti pakaammo ni Yahweh.
Ungovomera kulakwa kwako kuti unawukira Yehova Mulungu wako. Vomera kuti unayendayenda kukapembedza milungu yachilendo pansi pa mtengo uliwonse wogudira, ndiponso kuti sunandimvere,’” akutero Yehova.
14 Agsublikayo, dakayo a saan a napudno a tattao! —kastoy ti pakaammo ni Yahweh—ta inasawakayo! Mangalaak kadakayo iti maysa manipud iti tunggal siudad, dua manipud iti tunggal puli, ket ipankayo idiay Sion!
“Bwererani, ana osakhulupirika, pakuti ndine mbuye wanu,” akutero Yehova. “Ndinakusankhani, mmodzimmodzi kuchokera ku mudzi uliwonse ndiponso awiriawiri kuchokera ku banja lililonse.
15 Ikkankayto kadagiti agpaspastor nga iti pagayatanna ket ti pagayatak, ken idalandakayonto nga addaan iti pannakaammo ken kinasirib.
Ndipo ndidzakupatsani abusa a pamtima panga amene adzakutsogolerani mwanzeru ndi mwaluntha.
16 Ket mapasamakto, nga umadu ken maaddaankayonto iti adu a kaputotan iti daytoy a daga kadagidiay nga al-aldaw—kastoy ti pakaammo ni Yahweh. Saandanton nga ibaga, “Ti lakasa ti tulag ni Yahweh!” Saandanton a malagip daytoy, ta saandanto a panunoten ti maipanggep iti daytoy wenno ikaskaso daytoy. Daytoy a sao ket saanton a maibaga pay.'
Masiku amenewo mukadzachulukana kwambiri mʼdzikomo, anthu sadzanenanso za ‘Bokosi la Chipangano la Yehova’ kapena kuliganizira. Sadzalikumbukiranso kapena kulifuna, ndipo sadzapanganso lina,” akutero Yehova.
17 Iti dayta a tiempo, iwaragawagdanto maipanggep iti Jerusalem, 'Daytoy ti trono ni Yahweh,' ket aguummongto dagiti amin a nasion idiay Jerusalem iti nagan ni Yahweh. Saandanton nga aramiden dagiti dakes a tartarigagayanda.
Nthawi imeneyo adzatcha Yerusalemu Mpando Waufumu wa Yehova, ndipo mitundu yonse ya anthu idzasonkhana mu Yerusalemu pamaso pa Yehova. Sadzawumiriranso kutsata mitima yawo yoyipa.
18 Kadagidiay nga aldaw, makipagkaykaysanto ti balay ti Juda iti balay ti Israel. Agkuyogdanto nga umay manipud iti daga iti amianan ket mapanda iti daga nga intedko a kas tawid kadagiti kapuonanyo.
Masiku amenewo fuko la Yuda lidzaphatikizana ndi fuko la Israeli, onse pamodzi adzachokera ku dziko la kumpoto kupita ku dziko limene ndinapatsa makolo awo, kuti likhale cholowa.
19 No kaniak, kinunak, 'Kayatka a padayawan a kas anakko a lalaki ken ikkanka iti nasayaat a daga, maysa a tawid a napinpintas ngem iti adda iti sadinnoman a nasion!' Imbagak koma nga, 'Awagandak nga “amak”.' Imbagak koma a saankanto a sumina iti panangsurotmo kaniak.
“Ine mwini ndinati, “‘Ndikanakonda bwanji kukukhazikani pakati pa ana anga ndikukupatsani dziko labwino kwambiri, cholowa chokongola kwambiri kuposa cha mitundu ina ya anthu.’ Ndinaganiza kuti mudzanditcha Ine ‘Atate’ ndi kuti simudzaleka kunditsata.
20 Ngem kas iti babai a saan a napudno iti asawana, liniputannak, sika a balay ti Israel—kastoy ti pakaammo ni Yahweh.”
Koma monga mkazi wosakhulupirika amasiya mwamuna wake, momwemonso inu mwakhala osakhulupirika kwa Ine, inu fuko la Israeli,” akutero Yehova.
21 “Adda ariwawa a mangngeg kadagiti patad, ti panagsangit ken panagpakaasi dagiti tattao ti Israel! Ta binaliwanda dagiti wagasda; nalipatandak, Siak a ni Yahweh a Diosda.
Mawu akumveka pa magomo, Aisraeli akulira ndi kupempha chifundo chifukwa anatsata njira zoyipa ndi kuyiwala Yehova Mulungu wawo.
22 Agsublikayo, dakayo a tattao a nangtallikud iti Apo! Paimbagenkayo iti kinamanangallilawyo!” “Adtoy! Umaykami kenka, ta sika ni Yahweh a Diosmi!
Inu mukuti, “Bwererani, anthu osakhulupirika; ndidzachiritsa kubwerera mʼmbuyo kwanu.” “Inde, tidzabwerera kwa Inu pakuti ndinu Yehova Mulungu wathu.
23 Ulbod laeng ti agtaud kadagiti turod, manipud kadagiti adu a bantay. Pudno a ti pannakaisalakan ti Israel ket adda laeng kenni Yahweh a Diostayo.
Ndithu kupembedza pa magomo komanso kuchita maphwando pa mapiri zilibe phindu. Zoonadi chipulumutso cha Israeli chili mwa Yehova Mulungu wathu basi.
24 Ngem dagiti nakababain a didiosen ket inalun-onda dagiti nagbannogan dagiti kapuonantayo— dagiti arban iti karnero ken bakada, dagiti annakda a lallaki ken babbai!
Kuyambira pa ubwana wathu milungu yochititsa manyazi ija yakhala ikutiwonongetsa phindu la ntchito za makolo athu, nkhosa ndi ngʼombe zawo, ana awo aamuna ndi aakazi.
25 Agiddatayo a sibabain. Abbongannatayo koma ti pannakaibabaintayo, ta nagbasoltayo kenni Yahweh a Diostayo! Datayo a mismo ken dagiti kapuonantayo, manipud idi tiempo ti kinaagtutubotayo agingga kadagitoy nga agdama nga aldaw, saantayo a dimngeg iti timek ni Yahweh a Diostayo!”
Tilekeni tigone pansi mwa manyazi, ndipo kunyozeka kwathu kutiphimbe. Paja tachimwira Yehova Mulungu wathu, ife pamodzi ndi makolo athu kuyambira nthawi ya ubwana wathu mpaka lero lino sitinamvere Yehova Mulungu wathu.”

< Jeremias 3 >