< Isaias 42 >

1 Adtoy, ti adipenko, ti pabpabilegek; ti pinilik, isuna a pakaragsakak. Inkabilko ti Espirituk kenkuana; iyegnanto ti kinalinteg kadagiti nasion.
“Nayu mtumiki wanga, amene ndimamuchirikiza, amene ndamusankha, amenenso ndimakondwera naye. Ndayika Mzimu wanga mwa Iyeyo, ndipo adzaweruza anthu a mitundu yonse mwachilungamo.
2 Saanto isuna nga agikkis wenno agpukkaw, wenno ipangngeg ti timekna kadagiti kalkalsada.
Iye sadzafuwula, sadzamveka mawu, kapena mawu ake kumveka mʼmisewu.
3 Saanna a tukkolen ti naparpar a runo, ken ti nakudrep a pabilo ket saannanto nga iddepen; sipupudnonto nga ipatungpalna ti kinalinteg.
Bango lophwanyika sadzalithyola, ndipo moto wozilala sadzawuzimitsa. Motero adzaonetsa kuti chilungamo ndicho choonadi;
4 Saanto isuna a kumapsut wenno maupay agingga a naipasdeknan ti kinalinteg iti rabaw ti daga; ket aguray iti lintegna dagiti daga iti igid ti baybay.
sadzafowoka kapena kukhumudwa mpaka atakhazikitsa chilungamo pa dziko lapansi, ndi mpaka mayiko a mʼmbali mwa nyanja atafika poyembekezera malangizo ake.”
5 Daytoy ti ibagbaga ti Dios a ni Yahweh, isuna a namarsua kadagiti langit ken nangukrad kadagitoy; isuna a nangukrad iti lubong ken mangmangted iti biag iti daytoy; isuna a mangmangted iti anges kadagiti tattao iti daytoy, ken biag kadagiti agnanaed iti daytoy;
Yehova Mulungu amene analenga zamlengalenga ndi kuziyalika, amene analenga dziko lapansi ndi zonse zimene zimabereka, amenenso amapereka mpweya kwa anthu ake okhala mʼdzikomo, ndi moyo kwa onse oyendamo, akuti,
6 “Siak a ni Yahweh, inayabanka iti kinalinteg ket kibinenkanto. Aywanankanto ken isaadkanto a kas katulagan kadagiti tattao, a kas lawag kadagiti Hentil,
“Ine Yehova, ndakuyitana chifukwa Ine ndine wolungama; ndikugwira dzanja ndipo ndidzakuteteza. Ndakupereka kukhala pangano langa kwa anthu ndi kuwunika kwa anthu a mitundu ina.
7 tapno luktam dagiti mata dagiti bulag, tapno wayawayaam dagiti balud manipud iti nasipnget a pagbaludan, ken dagiti agtugtugaw iti nasipnget iti balay a pagbaludan.
Udzatsekula maso a anthu osaona, udzamasula anthu a mʼndende ndi kutulutsa mʼndende anthu okhala mu mdima.
8 Siak ni Yahweh, dayta ti naganko; ket saanko nga ibingay ti dayagko iti dadduma wenno ti dayawko kadagiti kinitikitan a didiosen.
“Ine ndine Yehova: dzina langa ndi limenelo! Sindidzapereka ulemerero wanga kwa wina aliyense kapena matamando anga kwa mafano.
9 Kitaenyo, napasamaken dagiti immuna a banbanag, ita, ipakaammokon dagiti baro a mapasamak. Sakbay a mangrugi a mapasamak dagitoy, ibagakon kadakayo ti maipapan kadagitoy.”
Taonani, zinthu zimene ndinalosera kale zachitikadi, ndipo ndikuwuzani zinthu zatsopano; zinthuzo zisanaonekere Ine ndakudziwitsani.”
10 Kantaanyo ni Yahweh iti baro a kanta, ken pagdayawna kenkuana manipud iti pungto ti daga; dakayo a sumalsalog iti baybay, ken amin nga adda iti daytoy, dagiti daga iti igid ti baybay ken dagiti agnanaed kadagitoy.
Imbirani Yehova nyimbo yatsopano, mutamandeni inu okhala mʼdziko lonse lapansi, inu amene mumayenda pa nyanja, nyanja ikokome ndi zonse zili mʼmenemo. Inu okhala pa zilumba tamandani Yehova.
11 Agikkis koma ti disierto ken dagiti siudad, agpukkaw koma gapu iti rag-o dagiti rehion iti Kedar! Agkanta koma dagiti agnanaed iti Sela; agpukkawda koma manipud kadagiti tapaw ti bantay.
Chipululu ndi mizinda yake zikweze mawu awo; midzi ya Akedara ikondwere. Anthu a ku Sela ayimbe mwachimwemwe; afuwule kuchokera pamwamba pa mapiri.
12 Idaydayawda koma ni Yahweh ken ipakaammoda ti dayawna kadagiti daga iti igid ti baybay.
Atamande Yehova ndipo alalike matamando ake kwa anthu apazilumba zonse.
13 Rummuarto ni Yahweh a kas maysa a mannakigubat; mapanto isuna a kas maysa a mannakigubat. Ipakitananto ti pungtotna. Agpukkawto isuna, wen, agpukkawto isuna iti pukkaw ti gubat; ipakitananto kadagiti kabusorna ti pannakabalinna.
Yehova adzapita ku nkhondo ngati munthu wamphamvu, adzawutsa ukali wake ngati munthu wankhondo; akukuwa ndiponso akufuwula mfuwu wankhondo ndipo adzagonjetsa adani ake.
14 Nabayag a panawen a nagulimekak; nagtatalnaak ken ginawidak ti bagik; ita, agikkisak a kas iti babai nga agpaspasikal; agangsabak ken agal-alak.
Yehova akuti, “Ndakhala ndili chete kwa nthawi yayitali, ndakhala ndili phee osachita kanthu. Koma tsopano, ngati mayi pa nthawi yochira, ndi kubuwula ndi kupuma modukizadukiza ndipo ndili wefuwefu.
15 Rebbaekto dagiti banbantay ken dagiti turturod ket pagangoekto dagiti mulmulada; pagbalinekto nga isla dagiti karayan ken pagmagaekto dagiti dan-aw.
Ndidzawononga mapiri ndi zitunda ndipo ndidzawumitsa zomera zawo zonse; ndidzasandutsa mitsinje kukhala zilumba ndipo ndidzawumitsa maiwe.
16 Iyegkonto dagiti bulsek babaen iti dalan a saanda nga ammo; idalankonto ida kadagiti dalan a saanda nga ammo. Pagbalinekto a lawag ti kinasipnget iti sangoananda, ken pagbalinekto a nalinteg dagiti nakillo a disso. Dagitoy dagiti banbanag nga aramidekto ket saankonto ida a panawan.
Ndidzatsogolera anthu osaona mʼmisewu imene sanayidziwe, ndidzawatsogolera mʼnjira zimene sanayendepo; ndidzasandutsa mdima wa kutsogolo kwawo kuti ukhale kuwala ndipo ndidzasalaza malo osalala. Zimenezi ndizo ndidzachite; sindidzawataya.
17 Mailaksiddanto, maibabaindanto a naan-anay, isuda nga agtaltalek kadagiti kinitikitan nga imahe, a mangibagbaga kadagiti nakitikatan nga imahe, “Dakayo dagiti diosmi.”
Koma onse amene amadalira mafano amene amanena kwa mafanowo kuti, ‘ndinu milungu yathu,’ ndidzawachititsa manyazi kotheratu.
18 Denggenyo, dakayo a tuleng; ken kitaenyo dakayo a bulag tapno makitayo.
“Imvani, agonthi inu; yangʼanani osaona inu, kuti muone!
19 Siasino ti bulag, no saan a ti adipenko? Wenno tuleng a kas iti mensahero nga imbaonko? Adda kadi bulag a kas iti nakitulagak, wenno bulag a kas iti adipen ni Yahweh?
Ali wosaona ndani, si mtumiki wanga kodi? Ndipo ndani ali wosamva ngati mthenga amene ndamutuma? Kodi ndani ali wosaona ngati uja ndinachita naye pangano, kapena wosaona ndani ngati mtumiki wa Yehova?
20 Adu dagiti banbanag a makitkitayo ngem saanyo a maawatan; nakalukat dagiti lapayag ngem awan ti dumdumngeg.
Iwe waona zinthu zambiri, koma sunazisamale; makutu ako ndi otsekuka koma sumva kanthu.”
21 Makaay-ayo kenni Yahweh a dayawen ti kinalintegna ken itan-ok ti lintegna.
Chinamukomera Yehova chifukwa cha chilungamo chake, kapena lamulo lake kukhala lalikulu ndi lopambana.
22 Ngem dagitoy a tattao ket natakawan ken nasamsaman; naipalab-ogda amin kadagiti ab-abut, naipupokda kadagiti pagbaludan; nasamsamda nga awan ti siasinoman a mangispal kadakuada, ken awan ti siasinoman a nagkuna, “Isubliyo ida!”
Koma awa ndi anthu amene afunkhidwa ndi kuwalanda zinthu zawo, onsewa anawakola mʼmaenje kapena akuwabisa mʼndende. Tsono asanduka chofunkha popanda wina wowapulumutsa kapena kunena kuti, “Abwezeni kwawo.”
23 Siasino kadakayo ti mangipangagto iti daytoy? Siasinonto ti mangipangag ken mangdengngeg iti masakbayan?
Kodi ndani wa inu amene adzamvetsera zimenezi kapena kutchera khutu ndi kumva za mʼtsogolomo?
24 Siasino ti nangiyawat kenni Jacob kadagiti mannanakaw, ken ti Israel kadagiti tulisan? Saan aya a ni Yahweh, a nagbasolantayo, nga akin-wagas iti nagkedkedanda nga aramiden, ken akin-linteg iti nagkedkedanda a pagtulnogan?
Ndani anapereka Yakobo kwa ofunkha, ndi Israeli kwa anthu akuba? Kodi si Yehova, amene ife tamuchimwirayu? Pakuti sanathe kutsatira njira zake; ndipo sanamvere malangizo ake.
25 Isu nga imparukpokna ti nakaro a pungtotna maibusor kadakuada, nga addaan iti pannakadadael babaen iti gubat. Simged daytoy iti aglawlawda ngem saanda a naamiris daytoy; inuramna ida ngem saanda a pinagan-ano.
Motero anawakwiyira kwambiri, nawavutitsa ndi nkhondo. Anayatsa moto ponseponse mowazungulira komabe iwo sanamvetse; motowo unawapsereza, koma iwo sanatengepo phunziro ayi.

< Isaias 42 >