< Genesis 42 >

1 Ita, naammoan ni Jacob nga adda bukel idiay Egipto. Kinunana kadagiti putotna a lallaki. “Apay ta agkikinnitakayo?”
Yakobo atamva kuti ku Igupto kuli tirigu, anati kwa ana ake, “Nʼchifukwa chiyani mukungoyangʼanana wina ndi mnzake?
2 Kinunana, “Dumngegkayo, nangngegko nga adda bukel idiay Egipto. Sumalogkayo sadiay ket gumatangkayo iti agpaay kadatayo manipud sadiay tapno agbiagtayo a saan ket a matay.”
Ine ndamva kuti ku Igupto kuli tirigu. Pitani kumeneko mukatigulireko kuti tisafe ndi njala.”
3 Simmalog ngarud dagiti sangapulo a kakabsat ni Jose tapno gumatang iti bukel manipud iti Egipto.
Choncho abale ake khumi a Yosefe anapita kukagula tirigu ku Igupto.
4 Ngem ni Benjamin a kabsat ni Jose ket saanna a pinasurot kadagiti kakabsatna, ta kinunana, “Amangan no adda dakes a mapasamak kenkuana.”
Koma Yakobo sanamulole Benjamini mngʼono wake wa Yosefe kuti apite nawo chifukwa anaopa kuti choyipa chingamuchitikire.
5 Immay met dagiti annak ni Israel tapno gumatang malaksid pay kadagiti immay, ta adda met panagbisin iti daga ti Canaan.
Choncho ana a Israeli aja anapita pamodzi ndi gulu la anzawo kukagula tirigu pakuti ku Kanaani kunalinso njala.
6 Ita, ni Jose ti gobernador iti entero a daga. Isuna ti aglaklako kadagiti amin a tattao ti daga. Immay dagiti kakabsat ni Jose ket nagpaklebda iti daga.
Pakuti Yosefe anali nduna yayikulu yolamulira dziko la Igupto, ndiye kuti analinso amene ankagulitsa tirigu kwa anthu onse. Choncho abale ake a Yosefe nawonso anabwera, ndipo anamugwadira pansi.
7 Nakita ni Jose dagiti kakabsatna ket nabigbigna ida, ngem nagpammarang isuna kadakuada ken nagsao isuna iti nagubsang kadakuada. Kinunana kadakuada, “Sadinno ti naggapuanyo?” Kinunada, “Naggapukkami iti daga ti Canaan tapno gumatang iti taraon.”
Yosefe atangowaona abale ake anawazindikira, koma ananamizira kukhala ngati mlendo nawayankhula mwaukali kuwafunsa kuti, “Mwachokera kuti?” Iwo anayankha, “Ku dziko la Kanaani, tikudzagula chakudya.”
8 Nabigbig ni Jose dagiti kakabsatna ngem saanda a nabigbig isuna.
Ngakhale Yosefe anawazindikira abale ake, koma iwo sanamuzindikire.
9 Nalagip ni Jose dagiti tagtagainepna maipapan kadakuada. Kinunana kadakuada, “Espiakayo. Immaykayo tapno kitaenyo ti saan a naguardia-an a paset ti daga.”
Pamenepo anakumbukira maloto aja amene analota za iwo ndipo anati, “Inu ndinu akazitape! Mwabwera kudzazonda dziko lathu kuti muone pamene palibe chitetezo.”
10 Kinunada kenkuana, “Saan, apo. Immay dagitoy nga adipenmo a gumatang ti taraon.
Iwo anayankha, “Ayi mbuye wathu, antchito anufe tabwera kudzagula chakudya.
11 Putotnakami amin ti maymaysa a tao. Mapagtalkankami a lallaki. Saan nga espia dagitoy adipenmo.”
Tonse ndife ana a munthu mmodzi. Ndife antchito anu okhulupirika osati akazitape.”
12 Kinunana kadakuada, “Saan, ngem immaykayo tapno kitaenyo ti saan a naguardia-an a paset ti daga.”
Iye anawawuza kuti, “Ayi! Inu mwabwera kudzaona pamene palibe chitetezo mʼdziko muno.”
13 Kinunada, “Sangapulo ket dua nga agkakabsat dagitoy adipenmo, putotnakami ti maysa a tao idiay daga ti Canaan. Kitaem, kadua ita ti amami ti inaudi a kabsatmi, ket awanen iti daytoy a biag ti maysa pay a kabsatmi.”
Koma iwo anayankha, “Tinalipo ana aamuna khumi ndi awiri. Abambo athu ndi mmodzi, ndipo kwathu ndi ku Kanaani. Panopo wotsiriza ali ndi abambo athu ndipo wina anamwalira.”
14 Kinuna ni Jose kadakuada, “Kas nakunakon; espiakayo.
Yosefe anawawuza kuti, “Ndi momwe ndaneneramo: Inu ndinu akazitape.
15 Babaen iti daytoy masubokkayo. Isapatak iti nagan ti Faraon a saankayo a pumanaw ditoy, malaksid no umay ditoy ti inaudi a kabsatyo.
Ndiye ndikuyesani motere: Ine ndikulumbira pali Farao ndithu, inuyo simudzachoka malo ano mpaka wotsirizayo atabwera kuno.
16 Mangibaonkayo iti maysa kadakayo ket mapanna alaen ti kabsatyo. Maibaludkayo tapno masubok dagiti imbagayo, no adda met laeng kinapudno kadakayo, ta no saan, isapatak iti nagan ti Faraon, awan duadua nga espiakayo.”
Tumizani mmodzi wa inu akamutenge mʼbale wanuyo ndipo ena nonsenu musungidwa mʼndende, kuti titsimikize ngati zimene mukunenazi ndi zoona. Apo ayi, pali Farao ndithu, inu ndinu akazitape!”
17 Ket imbaludna amin ida iti tallo nga aldaw.
Ndipo onse anawayika mʼndende kwa masiku atatu.
18 Iti maikatlo nga aldaw, kinuna ni Jose kadakuada, “Aramidenyo daytoy ket agbiagkayo, ta adda panagbutengko iti Dios.
Pa tsiku lachitatu Yosefe anawawuza kuti, “Popeza ine ndimaopa Mulungu, ndipo inuyo ngati mukufuna kukhala ndi moyo muchite izi:
19 No mapagtalkankayo a lallaki, mabati ngarud ti maysa kadakayo iti daytoy a pagbaludan, ngem mapankayo, mangawitkayo kadagiti bukel para iti panagbisin kadagiti balbalayyo.
Ngati muli anthu achilungamo, mmodzi wa inu atsale mʼndende, pamene ena nonse mupite kwanu kuti muwatengere chakudya anthu akwanu kuli njalako.
20 Iyegyo ti inaudi a kabsatyo kaniak iti kasta ket mapaneknekan dagiti imbagayo ket saankayo a matay.” Kasta ngarud ti inaramidda.
Mukabwere naye kuno mngʼono wanu wotsirizayo kuti titsimikizire zimene munanena kuti musafe.” Ndipo anachita zomwezo.
21 Kinunada iti tunggal maysa, “Pudno a nagbidduttayo maipapan iti inaramidtayo iti kabsattayo ta nakitatayo ti ladingit ti kararuana idi nagpakaasi kadatayo ngem saantayo a dimngeg. Ngarud naisubli kadatayo daytoy a ladingit.
Iwo anati kwa wina ndi mnzake, “Ndithu ife tinalakwira mʼbale wathu uja popeza kuti ngakhale tinaona kuvutika kwake ndi kumva kulira kwake pamene ankatidandaulira kuti timuchitire chifundo, koma ife sitinamvere. Nʼchifukwa chake masautso awa atigwera.”
22 Simmungbat ni Ruben kadakuada, “Saan kadi nga imbagak kadakayo, 'Saankayo nga agaramid iti basol maibusor iti ubing,' ngem saankayonto met gamin a dimngeg? Ita kitaenyo, maisidsidirenkadatayo ti darana.”
Rubeni anayankha, “Kodi sindinakuwuzeni kuti musamuchite kanthu mnyamata uja? Koma inu simunamvere! Tsopano tikulandira malipiro a magazi ake.”
23 Saanda nga ammo a naawatan ida ni Jose, ta adda mangipatpatarus iti nagbabaetanda.
Koma sanadziwe kuti Yosefe ankawamva popeza kuti ankagwiritsa ntchito wotanthauzira poyankhula naye.
24 Pinanawanna ida ket nagsangit. Kalpsanna, nagsubli isuna iti ayanda ket nagsao kadakuada. Innalana ni Simeon kadakuada ket pinaibaludna iti imatangda.
Yosefe anapita pambali payekha kukalira. Kenaka anabweranso nadzayankhula nawo. Iye anatenga Simeoni namumanga iwo akuona.
25 Ket binilin ni Jose dagiti adipenna a punoenda iti bukbukel dagiti sako dagiti kakabsatna, ken isublida ti kuarta ti tunggal maysa a lalaki iti sakona, ken ipaayanda ida iti kasapulanda iti panagdaliasatda. Kasta ngarud ti naaramid para kadakuada.
Yosefe analamula kuti awadzazire matumba awo ndi tirigu, awayikiremo ndalama zawo momwemo ndiponso awapatse chakudya cha panjira. Izi anawachitiradi.
26 Inkarga dagiti agkakabsat dagiti awitda a bukel kadagiti asnoda ket pimmanawda manipud sadiay.
Abale a Yosefe aja anasenzetsa abulu awo tirigu amene anagula uja ndipo ananyamuka ulendo wawo.
27 Iti lugar a naginanaanda, maysa kadakuada ti nanglukat iti sakona tapno pakanenna ti asnona ket nakitana ti kuartana. Adda daytoy iti ngarab ti sakona.
Atafika pamalo pena poti agone, mmodzi mwa iwo anatsekula thumba lake kuti atapemo chakudya cha bulu wake. Atangomasula anaona kuti ndalama zake zili pakamwa pa thumba.
28 Kinunana kadagiti kakabsatna, “Naisubli ti kuartak. Kitaenyo daytoy; adda daytoy iti sakok.” Ket uray la agkibbakibbayo ti pusoda ken agpigpigergerda a nagkikinnita. Kinunada, “Ania daytoy nga inaramid ti Dios kadatayo?”
Iye anati kwa abale akewo, “Ndalama zanga andibwezera, izi zili mʼthumba mwangamu.” Mitima yawo inachita ngati yachokamo ndipo anali ndi mantha ambiri, nati, “Ndi chiyani chimene Mulungu watichitira?”
29 Napanda kenni Jacob nga amada nga adda iti daga ti Canaan ket imbagada kenkuana ti amin a napasamak kadakuada. Kinunada,
Atafika kwa abambo awo Yakobo mʼdziko la Kanaani anafotokoza zonse zimene zinawachitikira nati,
30 “Ti lalaki, nga apo ti daga ket sigugubsang a nakisarita kadakami ken impagarupna nga espiakami iti daga.
“Nduna yayikulu ya mʼdzikomo inatiyankhula mwa ukali kwambiri ndipo inkatiyesa kuti ndife akazitape.
31 Imbagami kenkuana, 'Mapagtalkankami a lallaki. saankami nga espia.
Koma tinamuwuza kuti, ‘Ndife anthu woona mtima osati akazitape.
32 Sangapulo ket dua kami nga agkakabsat, putotnakami ti amami. Natayen ti maysa kadakami ken ti inaudi a kabsatmi ket adda ita iti ayan ti amami idiay daga ti Canaan.'
Ife tonse tinalipo ana aamuna khumi ndi awiri, abambo mmodzi. Mmodzi anamwalira, ndipo wamngʼono ali ndi abambo athu ku Kanaani.’”
33 Ti lalaki nga apo ti daga, kinunana kadakami, 'Babaen iti daytoy ket maammoak no mapagtalkankayo a lallaki. Ibatiyo ti maysa a kabsatyo kaniak, mangalakayo iti bukel para iti panagbisin kadagiti balayyo, ket mapankayo.
Ndipo nduna ija inati kwa ife, “Kuti ndidziwedi kuti ndinu anthu owona mtima muchite izi: Mmodzi mwa inu atsale ndi ine kuno, ndipo enanu mutenge chakudya ndi kubwerera kwanu kumene kuli njalako.
34 Iyegyo ti inaudi a kabsatyo kaniak. Iti kasta ket mapaneknekak a saankayo nga espia, ngem ketdi, mapagtalkankayo a lallaki. Ket wayawayaakto ti kabsatyo ket mabalinkayo a gumatang ken aglako iti daytoy a daga.”'
Koma mundibweretsere wotsirizayo kuti ndidziwedi kuti sindinu akazitape koma anthu achilungamo. Kenaka ndidzakubwezerani mʼbale wanuyu ndipo mukhoza kuchita malonda mʼdzikoli.”
35 Napasamak nga idi imbukbokda dagiti sakoda ket adtoy, adda iti sako ti tunggal maysa ti nakasupot a kuartada. Idi nakitada ken ti amada dagiti nakasupot a kuartada, nagbutengda.
Pamene amakhuthula matumba awo a tirigu aliyense anapeza kuti kathumba kake ka ndalama kali momwemo. Ataona zimenezi, iwo pamodzi ndi abambo awo anachita mantha kwambiri.
36 Kinuna ti amada a ni Jacob, kadakuada, “Pinagladingitdak kadagiti putotko. Natayen ni Jose, awanen ni Simeon ken iyadayoyo ni Benjamin. Maibusor kaniak amin dagitoy a banbanag.”
Abambo awo Yakobo anawawuza kuti, “Mwandilanda ana anga ine. Yosefe anamwalira ndipo Simeoni palibenso, ndiye tsopano mukufuna mutengenso Benjamini. Zonsezi zandigwera ine!”
37 Nagsao ni Ruben iti amana, a kunana, “Uray patayemto dagiti dua a putotko a lallaki no saanko a maisubli ni Benjamin kenka. Italekmo isuna kaniak ket isublikto isuna kenka.”
Koma Rubeni anati kwa abambo ake, “Ngati sindidzabwera naye kwa inu, mudzaphe ana anga aamuna awiri. Muperekeni mʼmanja mwangamu ndipo ndidzamusamala ndi kubwera naye kwa inu.”
38 Kinuna ni Jacob, “Saan a sumurot a sumalog kadakayo ti anakko. Ta natayen ti kabsatna ket isuna laengen ti nabati. No adda dakes a mapasamak kenkuana iti dalanyo, ipandakto, siak a purawen ti buokna, iti sheol gapu iti ladingit.” (Sheol h7585)
Koma Yakobo anati, “Mwana wanga sapita nanu kumeneko; mkulu wake anamwalira ndipo watsala yekha. Ngati choyipa chitamuchitikira pa ulendo mukupitawu, ndiye kuti ndi mmene ndakalambiramu inu mudzandipha ndi chisoni chotere.” (Sheol h7585)

< Genesis 42 >