< Ezra 2 >
1 Dagitoy dagiti tattao iti probinsia a nakaruk-at iti pannakaibalud kadakuada ni Ari Nebucadnesar a nangipan kadakuada a kas balud idiay Babilonia, dagiti tattao a nagsubli kadagiti tunggal siudadda iti Jerusalem ken iti Judea.
Awa ndi anthu a mʼchigawo cha Yuda amene anabwerako ku ukapolo, amene Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni anawagwira ukapolo ndi kupita nawo ku Babuloni (iwo anabwerera ku Yerusalemu ndi ku Yuda, aliyense ku mzinda wake.
2 Kaduada a nagsubli da Zerubbabel, Jesua, Nehemias, Seraias, Reelaias, Mardokeo, Bilsan, Mispar, Bigvai, Rehum ken Baana. Daytoy ti listaan dagiti lallaki manipud kadagiti tattao ti Israel.
Iwo anabwerera pamodzi ndi Zerubabeli, Yesuwa, Nehemiya, Seruya, Reelaya, Mordekai, Bilisani, Misipara, Bigivai, Rehumu ndi Baana). Chiwerengero cha anthu aamuna a Israeli chinali chotere:
3 Dagiti kaputotan ni Paros: 2, 172.
Zidzukulu za Parosi 2,172
4 Dagiti kaputotan ni Safatias: 372.
zidzukulu za Sefatiya 372
5 Dagiti kaputotan ni Aras: 775.
zidzukulu za Ara 775
6 Dagiti kaputotan ni Pahat Moab, babaen kenni Jesua ken Joab: 2, 812.
zidzukulu za Pahati-Mowabu (zochokera kwa Yesuwa ndi Yowabu) 2,812
7 Dagiti kaputotan ni Elam: 1, 254.
zidzukulu za Elamu 1,254
8 Dagiti kaputotan ni Zattu: 945.
zidzukulu za Zatu 945
9 Dagiti kaputotan ni Zaccai: 760.
zidzukulu za Zakai 760
10 Dagiti kaputotan ni Bani: 642.
zidzukulu za Bani 642
11 Dagiti kaputotan ni Bebai: 623.
zidzukulu za Bebai 623
12 Dagiti kaputotan ni Azgad: 1, 222.
zidzukulu za Azigadi 1,222
13 Dagiti kaputotan ni Adonikam: 666.
zidzukulu za Adonikamu 666
14 Dagiti kaputotan ni Bigvai: 2, 056.
zidzukulu za Bigivai 2,056
15 Dagiti kaputotan ni Adin: 454.
zidzukulu za Adini 454
16 Dagiti tattao ni Ater babaen kenni Hezekias: siam a pulo ket walo.
zidzukulu za Ateri (kudzera mwa Hezekiya) 98
17 Dagiti kaputotan ni Bezai: 323.
zidzukulu za Bezayi 323
18 Dagiti kaputotan ni Jora: 112.
zidzukulu za Yora 112
19 Dagiti tattao ni Hasum: 223.
zidzukulu za Hasumu 223
20 Dagiti tattao ni Gibbar: siam a pulo ket lima.
zidzukulu za Gibari 95.
21 Dagiti tattao ti Betlehem: 123.
Anthu a ku Betelehemu 123
22 Dagiti tattao ti Netofa: lima pulo ket innem.
Anthu aamuna a ku Netofa 56
23 Dagiti tattao ti Anatot: 128.
Anthu aamuna a ku Anatoti 128
24 Dagiti tattao ti Asmavet: uppat a pulo ket dua.
Anthu aamuna a ku Azimaveti 42
25 Dagiti tattao ti Kiriat Jearim, Kefira ken Beerot: 743.
Anthu aamuna a ku Kiriati Yearimu, Kefira ndi Beeroti 743
26 Dagiti tattao ti Rama ken Geba: 621.
Anthu aamuna a ku Rama ndi Geba 621
27 Dagiti tattao ti Micmas: 122.
Anthu aamuna a ku Mikimasi 122
28 Dagiti tattao ti Betel ken Ai: 223.
Anthu aamuna a ku Beteli ndi Ai 223
29 Dagiti tattao ti Nebo: lima pulo ket dua.
Anthu aamuna a ku Nebo 52
30 Dagiti tattao ti Magbis: 156.
Anthu aamuna a ku Magaibisi 156
31 Dagiti tattao ti sabali nga Elam: 1, 254.
Anthu aamuna a ku Elamu wina 1,254
32 Dagiti tattao ti Harim: 320.
Anthu aamuna a ku Harimu 320
33 Dagiti tattao ti Lod, Hadid, ken Ono: 725.
Anthu aamuna a ku Lodi, Hadidi ndi Ono 725
34 Dagiti tattao ti Jerico: 345.
Anthu aamuna a ku Yeriko 345
35 Dagiti tattao ti Senaa: 3, 630.
Anthu aamuna a ku Sena 3,630.
36 Dagiti papadi: Dagiti kaputotan ni Jedaias iti balay ni Jesua: 973.
Ansembe anali awa: Zidzukulu za Yedaya (kudzera mu banja la Yesuwa) 973
37 Dagiti kaputotan ni Immer: 1, 052.
Zidzukulu za Imeri 1,052
38 Dagiti kaputotan ni Pasur: 1, 247.
Zidzukulu za Pasuri 1,247
39 Dagiti kaputotan ni Harim: 1, 017.
Zidzukulu za Harimu 1,017.
40 Dagiti Levita: Dagiti kaputotan da Jesua ken Kadmiel, a kaputotan ni Hodavias: pitopulo ket uppat.
Alevi anali awa: Zidzukulu za Yesuwa ndi Kadimieli (kudzera mwa ana a Hodaviya) 74.
41 Dagiti kumakanta iti templo: Dagiti kaputotan ni Asaf: 128.
Anthu oyimba nyimbo anali awa: Zidzukulu za Asafu 128.
42 Dagiti kaputotan dagiti agbanbantay iti ruangan: Dagiti kaputotan da Salum, Ater, Talmon, Akkub, Hatita, ken Sobai: 139 amin.
Alonda a ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Salumu, zidzukulu za Ateri, zidzukulu za Talimoni, zidzukulu za Akubu, zidzukulu za Hatita ndi zidzukulu za Sobai 139.
43 Dagidiay naisaad nga agserbi iti templo: Dagiti kaputotan da Siha, Hasufa, Tabaot,
Otumikira ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Ziha, zidzukulu za Hasufa, zidzukulu za Tabaoti,
zidzukulu za Kerosi, zidzukulu za Siyaha, Padoni,
45 Lebana, Hagaba, Akkub,
zidzukulu za Lebana, zidzukulu za Hagaba, zidzukulu za Akubu,
46 Hagab, Samlai ken Hanan;
zidzukulu za Hagabu, zidzukulu za Salimayi, zidzukulu za Hanani,
47 dagiti kaputotan da Giddel, Gahar, Reayas,
zidzukulu za Gideli, zidzukulu za Gahari, zidzukulu za Reaya,
48 Resin, Necoda, Gazzam,
zidzukulu za Rezini, zidzukulu za Nekoda, zidzukulu za Gazamu,
zidzukulu za Uza, zidzukulu za Peseya, zidzukulu za Besai,
50 Asna, Meumin ken Nefisim;
zidzukulu za Asina, zidzukulu za Meunimu, Nefusimu,
51 dagiti kaputotan da Bakbuk, Hakufa, Harhur,
zidzukulu za Bakibuku, zidzukulu za Hakufa, zidzukulu za Harihuri,
52 Baslut, Mehida, Harsa,
zidzukulu za Baziruti, zidzukulu za Mehida, zidzukulu za Harisa,
zidzukulu za Barikosi, zidzukulu za Sisera, zidzukulu za Tema,
zidzukulu za Neziya ndi zidzukulu za Hatifa.
55 Dagiti kaputotan dagiti adipen ni Solomon: Dagiti kaputotan da Sotai, Hasoferet, Peruda,
Zidzukulu za antchito a Solomoni zinali izi: Zidzukulu za Sotai, zidzukulu za Hasofereti, zidzukulu za Peruda,
56 Jaala, Darkon, Giddel,
zidzukulu za Yaala, zidzukulu za Darikoni, zidzukulu za Gideli,
57 Sefatias, Hattil, Pokeret Hazzebaim, ken Ami.
zidzukulu za Sefatiya, zidzukulu za Hatilu, zidzukulu za Pokereti, Hazebayimu ndi Ami.
58 Agdagup iti 392 amin a kaputotan dagiti naisaad nga agserbi iti templo ken dagiti kaputotan dagiti adipen ni Solomon.
Chiwerengero cha onse otumikira ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi zidzukulu za Solomoni chinali 392.
59 Dagidiay pimmanaw manipud Tel Mela, Tel Harsa, Kerub, Addan ken Immer—ngem saanda a mapaneknekan a nagtaud iti Israel ti kapuonanda—agraman
Anthu ali mʼmunsiwa anabwera kuchokera ku mizinda ya Teli-Mela, Teli-Harisa, Kerubi, Adoni ndi Imeri, ngakhale samatha kutsimikiza kuti mafuko awo analidi Aisraeli enieni kapena ayi:
60 dagiti 652 a kaputotan da Delaias, Tobias ken Necoda.
Zidzukulu za Delaya, zidzukulu za Tobiya, ndi zidzukulu za Nekoda. Onse pamodzi anali 652.
61 Ket kadagiti kaputotan dagiti papadi: Dagiti kaputotan da Habaias, Hakkoz, ken Barzillai (a nakiasawa kadagiti babbai a kaputotan ni Barzillai a Galaadita ket naawagan babaen kadagiti naganda)
Ndi ena pakati pa ansembe anali awa: Zidzukulu za Hobiya, Hakozi, ndi Barizilai (Zidzukulu za Hobiya, zidzukulu za Hakozi ndi zidzukulu za Barizilai. Barizilai ameneyu ndi uja anakwatira mmodzi mwa ana aakazi a Barizilai Mgiliyadi ndipo ankadziwika ndi dzina la bambo wawoyo.)
62 Pinadasda a biruken ti listaan ti nagtaudanda a kapuonan, ngem saanda a nabirukan gapu ta rinugitanda ti kinapadida.
Amenewa anafufuza mayina awo mʼbuku lofotokoza mbiri ya mafuko awo, koma mayinawo sanawapezemo, choncho anawachotsa pa unsembe ngati anthu odetsedwa pa zachipembedzo.
63 Isu a kinuna ti gobernador kadakuada a saanda a mangan kadagiti aniaman a nasantoan a daton agingga a palubosan ida ti maysa a padi nga addaan iti Urim ken Tummim.
Bwanamkubwa anawawuza anthuwo kuti asamadye nawo mpaka atapezeka wansembe wodziwa kuwombeza ndi Urimu ndi Tumimu.
64 Agdagup iti 42, 360 ti bilang ti entero a bunggoy,
Chiwerengero cha anthu onse pamodzi chinali 42,360,
65 saan a karaman dagiti adipenda ken dagiti adipenda a babbai (agdagup dagitoy iti 7, 337) ken dagiti lallaki ken babbai a kumakanta iti templo (dua gasut).
kuwonjezera pamenepo, panalinso antchito awo aamuna ndi aakazi okwanira 7,337. Analinso ndi amuna ndi akazi oyimba nyimbo okwanira 200.
66 Dagiti kabalioda: 736. Dagiti muloda: 245.
Anali ndi akavalo 736, nyulu 245,
67 Dagiti kamelioda: 435. Dagiti asnoda: 6, 720.
ngamira 435 ndi abulu 6,720.
68 Idi napanda iti balay ni Yahweh idiay Jerusalem, nangted dagiti papanguloen ti pamilia iti nagtaud iti kaunggan a sagsagut tapno mausar iti pannakaibangon ti balay.
Atafika ku Nyumba ya Yehova mu Yerusalemu, ena mwa atsogoleri a mabanja anapereka zopereka zaufulu zothandizira kumanganso Nyumba ya Mulungu pamalo pake pakale.
69 Nangtedda segun iti kabaelanda nga ited a mausar iti trabaho: 61, 000 a daric ti balitok, lima ribo a minas ti pirak, ken sangagasut a pagan-anay para kadagiti padi.
Anapereka kwa msungichuma wa ntchitoyo molingana ndi mmene aliyense chuma chake chinalili: golide wa makilogalamu 500, siliva makilogalamu 2,800 ndi zovala za ansembe zokwanira 100.
70 Isu a dagiti papadi ken dagiti Levita, dagiti tattao, dagiti kumakanta iti templo ken dagiti mangbanbantay kadagiti ruangan, ken dagiti nadutokan nga agserbi iti templo ket nagnaedda kadagiti siudadda. Dagiti amin a tattao iti Israel ket adda kadagiti siudadda.
Ansembe, Alevi, oyimba nyimbo, alonda ndi antchito a ku Nyumba ya Yehova pamodzi ndi Aisraeli ena onse ankakhala mʼmidzi ya makolo awo.