< Ezekiel 33 >

1 Kalpasanna, dimteng kaniak ti sao ni Yahweh a kunana,
Yehova anandiyankhula nati:
2 “Anak ti tao, ipakaammom daytoy kadagiti tattaom; ibagam kadakuada, 'Inton mangiyegak iti kampilan a maibusor iti aniaman a daga, ket mangdutok dagiti tattao iti dayta a daga iti maysa a tao manipud kadakuada nga agbalin a para-wanawanda.
“Iwe mwana wa munthu awuze anthu a mtundu wako kuti, ‘Paja zimati ndikatumiza nkhondo mʼdziko anthu a mʼdzikomo amasankha munthu mmodzi pakati pawo kuti akhale mlonda.
3 Siputanna ti kampilan nga um-umay iti daga ket puyotanna ti tangguyobna tapno ballaaganna dagiti tattao!
Tsono iyeyo amati akaona nkhondo ikubwera amaliza lipenga kuti achenjeze anthuwo.
4 No mangngeg dagiti tattao ti uni ti tangguyob ket saanda nga ipangag, ken no umay ti kampilan ket patayenna ida, ti dara ti tunggal maysa ket adda iti bukodda nga ulo.
Wina aliyense akamva lipenga koma osasamala, mdani uja akabwera nʼkumupha, ndiye kuti wadziphetsa yekha.
5 Ket no adda makangngeg iti uni ti tangguyob ket saanna nga ipangag, ti darana ket adda kenkuana; ngem no ipangagna, maisalakannanto ti bukodna a biag.
Iye anamva kulira kwa lipenga koma sanalabadire. Ndiye kuti wadziphetsa yekha. Akanasamala kuchenjeza kwa mlonda akanapulumuka.
6 Nupay kasta, no makita ti para-wanawan ti kampilan nga um-umay, ngem no saanna a pinuyutan ti tangguyob, a ti nagbanaganna ket saan a naballaagan dagiti tattao, ket no umay ti kampilan ket patayenna ti siasinoman, napapatay dayta a tao iti bukodna a basol ngem sapulekto ti darana iti para-wanawan.'
Koma ngati mlondayo aona lupanga likubwera ndipo osawomba lipengalo kuchenjeza anthu, ndipo lupanga libwera ndi kuchotsa moyo wa mmodzi mwa iwo, munthu ameneyo adzafa chifukwa cha tchimo lake, koma ndidzamuyimba mlandu mlondayo chifukwa cha imfa ya mnzakeyo.’
7 Ita, sika a mismo, anak ti tao! Pinagbalinka a para-wanawan para iti balay ti Israel; mangngegmonto dagiti sasaok manipud iti ngiwatko ket ballaagamto ida para kaniak.
“Tsono iwe mwana wa munthu, ndakuyika kuti ukhale mlonda wa Aisraeli. Choncho imva mawu amene ndikuyankhula ndipo uwachenjeze.
8 No ibagak iti maysa a nadangkes a tao, 'Nadangkes a tao, sigurado a matayka!' ngem no saanmo nga iwaragawag daytoy tapno maballaagan ti nadangkes maipapan iti aramidna, ket matayto dayta a nadangkes iti basolna, ngem sapulekto kadagiti imam ti darana!
Ndikawuza munthu woyipa kuti, ‘Iwe munthu woyipa, udzafa ndithu,’ ndipo iwe osayankhula kumuchenjeza kuti aleke njira zake, munthu wochimwayo adzafa chifukwa cha tchimo lake, koma Ine ndidzakuyimba mlandu chifukwa cha imfa yake.
9 Ngem sika, no ballaagam ti nadangkes maipapan iti aramidna, tapno matallikodanna daytoy, ket no saan isuna a timmallikod manipud iti aramidna, matayto isuna iti basolna, ngem sika a mismo ket maisalakanmonto ti bukodmo a biag.
Koma ngati uchenjeza munthu woyipa kuti aleke njira zake, ndipo iye osatero, adzafa chifukwa cha tchimo lake, koma iwe udzapulumutsa moyo wako.
10 Isu a sika, anak ti tao, ibagam iti balay ti Israel, 'Kastoy ti ibagbagayo: Adda kadakami dagiti panagsalungasingmi ken basolmi, ket madaddadaelkamin kadagitoy! Kasano nga agbiagkami?
“Iwe mwana wa munthu, akumbutse Aisraeli mawu awo akuti, ‘Ife talemedwa ndi zolakwa zathu ndi machimo athu, ndipo tikuwonda chifukwa cha zimene tachita. Kodi tingakhale ndi moyo bwanji?’”
11 Ibagam kadakuada, 'Iti naganko nga adda iti agnanayon—kastoy ti pakaammo ti Apo a ni Yahweh—saanko a pakaragsakan ti ipapatay ti nadangkes a tao, ngem no agbabawi ti nadangkes a tao manipud iti aramidna, agbiagto ngarud isuna! Agbabawikayo! Agbabawikayo manipud kadagiti nadangkes a aramidyo! Ta apay koma a mataykayo, balay ti Israel?'
Uwawuze kuti, Ine Ambuye Yehova ndikuti: “Pali Ine wamoyo, sindikondwera ndi imfa ya munthu woyipa. Ndimakondwera ndikamaona munthu woyipa akuleka zoyipa zake kuti akhale ndi moyo. Tembenukani! Tembenukani, siyani makhalidwe anu oyipa! Muferanji, Inu Aisraeli?
12 Ket sika, anak ti tao, ibagam kadagiti tattaom, 'Ti kinalinteg ti maysa a nalinteg a tao ket saanto a makaisalakan kenkuana no agbasol! Ken ti kinadangkes ti maysa a nadangkes a tao ket saanto a daytoy ti gapu a mapukaw isuna no agbabawi manipud iti basolna. Ta saanto nga agbiag ti nalinteg a tao gapu iti kinalintegna no agbasol isuna.
“Tsono iwe mwana wa munthu, awuze anthu a mtundu wako kuti, ‘Ngati munthu wolungama achimwa, ndiye kuti ntchito zake zabwino zija sizidzamupulutsa. Koma wochimwa akaleka ntchito zake zoyipazo, sadzalangidwa konse. Ndithu ngati munthu wolungama ayamba kuchimwa sadzatha kukhala ndi moyo chifukwa cha ntchito zake zabwino zija.’
13 No ibagak iti maysa a nalinteg, “Sigurado nga agbiagto isuna!” ket no agtalek isuna iti bukodna a kinalinteg ket kalpasanna, agaramid iti saan a nainkalintegan, saankonto a lagipen ti aniaman a kinalintegna; matayto isuna iti kinadangkes nga inaramidna.
Ngati ndiwuza munthu wolungama kuti adzafa ndithu, koma iyeyo nʼkumadalira ntchito zake zabwino zimene anachita kale ndi kuyamba kuchimwa, ndiye kuti ntchito zake zabwinozo zidzayiwalika. Iye adzafa chifukwa cha machimo ake.
14 Ket no ibagak iti nadangkes, “Sigurado a matayka!” ngem no agbabawi isuna kadagiti basolna ket aramidenna ti nainkalintegan ken umno—
Ndipo ngati ndiwuza munthu woyipa kuti, ‘Udzafa ndithu,’ tsono iye nʼkutembenuka kuleka machimo ake ndi kuyamba kuchita zimene Yehova afuna,
15 no isublina ti naisalda kenkuana a kiniddawna a sidadangkes, wenno isublina ti tinakawna, ket no surotenna dagiti bilbilin a mangipaay iti biag ket saanen nga agramid iti basol— sigurado nga agbiagto ngarud isuna; saanto isuna a matay.
monga kubweza chimene anatenga ngati chikole cha ngongole, kubweza chimene anaba, kutsatira malamulo omwe amapereka moyo ndi kuleka kuchita zoyipa, iye adzakhala ndithu ndi moyo; sadzafa.
16 Awanto a pulos ti malagip kadagiti basol nga inaramidna, nagtignay isuna a sililinteg; sigurado nga agbiagto isuna!
Ndidzakhululuka machimo ake onse anachita. Iye wachita zimene ndi zolungama ndi zoyenera ndipo iye adzakhala ndi moyo ndithu.
17 Ngem kinuna dagiti tattaom, '“Saan a nalinteg ti wagas ti Apo!” ngem dagiti wagasyo ti saan a nalinteg!
“Komabe anthu a mtundu wako akunena kuti, ‘Zimene Ambuye amachita ndi zopanda chilungamo.’ Ayi, koma makhalidwe awo ndiwo ali osalungama.
18 No tallikodan ti maysa a nalinteg a tao ti kinalintegna ket agaramid iti basol, daytoyto ngarud ti pakatayanna!
Ngati munthu wolungama atembenuka ndi kuleka ntchito zake zolungama ndi kuyamba kuchita zoyipa, adzafa nazo.
19 Ket no tallikodan ti maysa a nadangkes a tao ti kinadangkesna ket aramidenna ti nainkalintegan ken rumbeng, agbiagto isuna gapu kadagidiay a banbanag!
Ndipo ngati munthu woyipa atembenuka ndi kuleka ntchito zake zoyipa ndi kuyamba kuchita zolungama ndi zoyenera, iye adzakhala ndi moyo pochita zimenezo.
20 Ngem kinunayo dakayo a tattao, “Saan a nalinteg ti wagas ti Apo!” Ukomekto ti tunggal maysa kadakayo segun iti wagasna, balay ti Israel!'”
Koma Inu Aisraeli, mukunena kuti, ‘Zimene Ambuye amachita ndi zopanda chilungamo.’ Ayi, inu Aisraeli, Ine ndidzaweruza aliyense wa inu potsata ntchito zake.”
21 Napasamak daytoy iti maikasangapulo ket dua a tawen, iti maikalima nga aldaw ti maikasangapulo a bulan ti pannakaibaludtayo, nga adda immay kaniak a maysa a nakalibas manipud Jerusalem ket kinunana,
Pa tsiku lachisanu la mwezi wakhumi, chaka chakhumi ndi chiwiri cha ukapolo wathu, munthu wina amene anapulumuka ku Yerusalemu anabwera kudzandiwuza kuti, “Mzinda wagwa!”
22 “Nasakupen ti siudad!” Adda kaniak ti ima ni Yahweh iti rabii sakbay a dimteng ti nakalibas, ket naglukat ti ngiwatko idi dimteng isuna iti parbangon. Isu a nalukatan ti ngiwatko; saanakon nga umel!
Tsono madzulo ake munthuyo asanafike, dzanja la Yehova linali pa ine. Koma mmawa mwake munthuyo atabwera Yehova anatsekula pakamwa panga, motero kuti sindinakhalenso wosayankhula.
23 Ket dimteng kaniak ti sao ni Yahweh a kunana,
Ndipo Yehova anandiyankhula kuti:
24 “Anak ti tao, ibagbaga dagiti agnanaed kadagidiay a nadadael iti daga ti Israel, 'Maymaysa laeng a tao ni Abraham ket tinawidna ti daga, ngem adutayo! Naited kadatayo ti daga a kas sanikua.'
“Iwe mwana wa munthu, anthu amene akukhala mʼmizinda ya mabwinja ya dziko la Israeli akunena kuti, ‘Abrahamu anali munthu mmodzi yekha, ndipo anamupatsa dziko lonse. Koma ife tilipo ambiri, motero tsono dzikolo ndi lathu.’
25 Ngarud ibagam kadakuada, 'Kastoy ti ibagbaga ti Apo a Yahweh: Mangmangankayo iti dara ken tumangtangadkayo kadagiti didiosenyo, ket iparparukpokyo ti dara dagiti tattao. Rumbeng kadi a tagikuaenyo ti daga?
Choncho iwe uwawuze kuti Ine Ambuye Yehova ndikuti, ‘Inu mumadya nyama ili ndi magazi ake, ndipo mumapembedza mafano ndi kukhetsa magazi, kodi tsono inu nʼkulandira dzikoli?
26 Nagtalekkayo kadagiti kampilanyo ken nangaramidkayo kadagiti makarimon a banbanag; daddadaelen ti tunggal lalaki ti dayaw ti asawa ti kaarrubana. Rumbeng kadi a tagikuaenyo ti daga?'
Mumadalira lupanga lanu, mumachita zinthu zonyansa, ndipo aliyense wa inu amachita chigololo ndi mkazi wa mnzake. Kodi inu nʼkulandira dzikoli?’
27 Kastoyto ti ibagam kadakuada, 'Kastoy ti kuna ti Apo a Yahweh: Iti naganko nga adda iti agnanayon, sigurado a mapasagto dagiti adda kadagiti nadadael babaen iti kampilan, ket itedkonto dagiti adda kadagiti taltalon kadagiti sibibiag a parsua a kas taraonda, ket matayto babaen kadagiti didigra dagiti adda kadagiti nasarikedkedan ken kueba.
“Uwawuze kuti Ine Ambuye Yehova ndikuti, ‘Ndithu pali Ine wamoyo, anthu amene anatsala mʼmizinda ya mabwinja adzaphedwa ndi lupanga, amene ali ku midzi ndidzawapereka kuti adzadyedwe ndi zirombo zakuthengo, ndipo amene ali mʼmalinga ndi mʼmapanga adzafa ndi mliri.
28 Ket pagbalinekto a langalang ken nakabutbuteng ti daga, ket agpatingganto ti kinapalangguad ti bileg daytoy, ta mabaybay-anto dagiti bantay ti Israel ken awanto ti lumabas kadagitoy.'
Ndidzalisandutsa chipululu dzikolo, ndipo mphamvu zake zimene amanyadira zidzatheratu, ndipo mapiri a Yerusalemu adzasanduka chipululu, kotero kuti palibe amene adzatha kudutsako.
29 Isu a maammoandanto a siak ni Yahweh, inton pagbalinek a langalang ken nakabutbuteng ti daga gapu kadagiti amin a makarimon a banbanag nga inaramidda.
Ndikadzasandutsa dzikolo chipululu chifukwa cha zonyansa zimene ankachita, pamenepo ndiye adzadziwa kuti ndine Yehova.’
30 Ket sika, anak ti tao— adda ibagbaga dagiti tattaom maipapan kenka iti abay dagiti pader ken kadagiti ruangan dagiti balbalay, ket ibagbaga ti tunggal maysa kadagiti dadduma— tunggal maysa iti kabsatna a lalaki, 'Mapantayo dumngeg iti sao ti profeta a nagtaud kenni Yahweh!'
“Koma kunena za iwe, mwana wa munthu, anthu a mtundu wako akumayankhula za iwe akakhala pa makoma a mzinda ndi pa makomo a nyumba zawo. Akumawuzana kuti, ‘Tiyeni tikamve uthenga umene wachokera kwa Yehova.’
31 Isu a mapanto kenka dagiti tattaok, kas iti masansan nga ar-aramidenda, ket agtugawdanto iti sangoanam ket dumngegda kadagiti sasaom, ngem saandanto a tungpalen dagitoy. Adda kadagiti ngiwatda dagiti umno a sasao, ngem dagiti pusoda ket adda kadagiti saan a nainkalintegan a pakagunggonaanda.
Anthu anga amabwera kwa iwe, monga momwe amachitira nthawi zonse anthu anga, ndipo amakhala pansi pamaso pako kumvetsera mawu ako. Koma zimene akumvazo sazichita. Zokamba zawo zimaonetsa chikondi, koma mitima yawo imakhala pa phindu lawo.
32 Ta kaslaka makay-ayo a kanta kadakuada, maysa a napintas a samiweng a natukaran a nasayaat iti adda kuerdasna nga instrumento, isu a dumngegdanto kadagiti sasaom ngem awanto a pulos kadakuada ti agtulnog kadagitoy.
Kunena zoona, kwa iwowo sindiwe kanthu konse, ndiwe munthu wamba chabe womangoyimba nyimbo zachikondi ndi liwu lokoma poyimba zeze. Kumva amamva mawu ako koma sawagwiritsa ntchito.
33 Isu nga inton mapasamak amin dagitoy— kitaem! mapasamakto daytoy! — ket maammoandanto a kaduada idi ti profeta.”
“Koma zonsezi zikadzachitika, ndipo zidzachitika ndithu, pamenepo adzadziwa kuti mneneri anali pakati pawo.”

< Ezekiel 33 >