< Ezekiel 32 >
1 Ket napasamak nga iti maika-sangapulo ket dua a bulan iti maika-sangapulo ket dua a tawen, iti umuna nga aldaw ti bulan, immay kaniak ti sao ni Yahweh a kunana,
Pa tsiku loyamba la mwezi wa khumi ndi chiwiri, chaka chakhumi ndi chiwiri, Yehova anandiyankhula kuti:
2 “Anak ti tao, dung-awam ni Faraon, nga ari ti Egipto; ibagam kenkuana, 'Arigmo ti urbon a leon kadagiti nasion, kaskala nakabutbuteng nga ayup iti baybay; kibkiburem ti danum, liblibegem dagiti danum babaen kadagiti sakam ken rugrugitam dagiti danumda!
“Iwe mwana wa munthu imba nyimbo ya maliro a Farao mfumu ya Igupto ndipo uyiwuze kuti, “Iwe umadziyesa ngati mkango pakati pa mitundu ya anthu. Koma iwe uli ngati ngʼona mʼnyanja. Umakhuvula mʼmitsinje yako, kuvundula madzi ndi mapazi ako ndi kudetsa madzi mʼmitsinje.
3 Kastoy ti kuna ti Apo a ni Yahweh, “Isarwagko ngarud kenka ti iketko iti taripnong dagiti adu a puli dagiti tattao, ket ingatodakanto iti iketko!
“Tsono Ine Ambuye Yehova ndikuti, “‘Pogwiritsa ntchito gulu la anthu a mitundu yambiri, ndidzakuponyera khoka langa ndi kukugwira mu ukonde wanga.
4 Baybay-ankanto iti daga! Ibellengkanto iti away ket pagbatayekto kenka dagiti billit iti tangatang; mapnekto dagiti amin a mabisin nga ayup iti daga babaen kenka.
Ndidzakuponya ku mtunda ndi kukutayira pansi. Ndidzabweretsa mbalame zamumlengalenga kuti zidzatere pa iwe, ndipo zirombo zonse za dziko lapansi zidzakudya.
5 Ta ikabilkonto ti lasagmo kadagiti bantay, ken punnoekto dagiti tanap iti agruprupsa a bangkaymo!
Ndidzayanika mnofu wako pa mapiri ndipo zigwa zidzadzaza ndi zotsalira zako.
6 Kalpasanna, iparukpokkonto ti daram kadagiti bantay, ket mapnonto dagiti waig iti daram!
Ndidzanyowetsa dziko ndi magazi ako, mpaka kumapiri komwe, ndipo mitsinje idzadzaza ndi mnofu wako.
7 Ket inton iddepek ti silawmo, lengdakto dagiti langit ken pagsipngetek dagiti bituen daytoy; lengdakto ti init babaen kadagiti ulep, ket saanto nga agraniag ti bulan!
Ndikadzakuwononga, ndidzaphimba miyamba ndikudetsa nyenyezi zake. Ndidzaphimba dzuwa ndi mtambo, ndipo mwezi sudzawala.
8 Pagsipngetekto dagiti amin nga agranraniag a silaw kadagiti langit iti ngatoem, ket pagsipngetekto ti dagam! —kastoy ti pakaammo ti Apo a ni Yahweh.
Zowala zonse zamumlengalenga ndidzazizimitsa; ndidzachititsa mdima pa dziko lako, akutero Ambuye Yehova.
9 Ket butbutngekto ti puso dagiti adu a puli dagiti tattao kadagiti daga a saanmo nga ammo, inton ipadamagko kadagiti nasion ti pannakarebbam.
Ndidzasautsa mitima ya anthu a mitundu yambiri pamene ndidzakupititsa ku ukapolo pakati pa mitundu ya anthu, ku mayiko amene iwe sunawadziwe.
10 Kellaatekto dagiti adu a puli dagiti tattao iti maipapan kenka; agpigergerto iti buteng dagiti arida maipapan kenka inton iwasiwasko ti kampilanko iti sangoananda. Iti tunggal kanito, agpigergerto ti tunggal maysa gapu kenka, iti aldaw ti pannakarebbam.
Ine ndidzachititsa kuti anthu a mitundu yambiri adabwe nawe, ndipo mafumu awo adzanjenjemera ndi mantha aakulu chifukwa cha iwe pamene ndidzaonetsa lupanga langa pamaso pawo. Pa nthawi ya kugwa kwako, aliyense wa iwo adzanjenjemera moyo wake wonse.
11 Ta kastoy ti kuna ti Apo a ni Yahweh: Umayto a maibusor kenka ti kampilan ti ari ti Babilonia!
“‘Pakuti ndikunena Ine Ambuye Yehova kuti, “‘Lupanga la mfumu ya ku Babuloni lidzabwera kudzalimbana nawe.
12 Ipaluboskonto a mapasag dagiti adipenmo babaen kadagiti kampilan dagiti mannakigubat—pagbutngento ti tunggal mannakigubat dagiti nasion! Dadaelento dagitoy a mannakigubat ti dayag ti Egipto ken papatayendanto amin dagiti adu a tattao nga agnanaed iti daytoy!
Ndidzachititsa gulu lako lankhondo kuti ligwe ndi lupanga la anthu amphamvu, anthu ankhanza kwambiri pakati pa mitundu yonse ya anthu. Adzathetsa kunyada kwa Igupto, ndipo gulu lake lonse la nkhondo lidzagonjetsedwa.
13 Ta papatayekto dagiti amin a taraken manipud iti igid dagiti adu a danum; saanen a kiburen dagiti saka ti tao dagiti danum, wenno kiburen ti saka ti baka dagitoy!
Ndidzawononga ziweto zake zonse zokhala mʼmbali mwa madzi ambiri. Ku madziko sikudzaonekanso phazi la munthu kapena kudetsedwa ndi phazi la ziweto.
14 Ket pagtalnaekto dagiti danumda ken pagayusekto dagiti karayanda a kas iti panagayus ti lana—kastoy ti pakaammo ti Apo a ni Yahweh!
Pambuyo pake ndidzayeretsa madzi ake ndipo mitsinje yake idzayenda mokometsera ngati mafuta, akutero Ambuye Yehova.
15 Inton ti daga ti Egipto—daga a napunpunno—ket pagbalinek a nadadael a lugar, nabaybay-an a lugar; inton darupek dagiti amin nga agnanaed kenkuana, ket maammoandanto a siak ni Yahweh!
Ndikadzasandutsa dziko la Igupto kukhala bwinja; ndikadzawononga dziko lonse ndi kukantha onse okhala kumeneko, adzadziwa kuti ndine Yehova.’
16 Addanto panagdung-aw! Ta dung-awanto isuna dagiti annak a babbai dagiti nasion; dung-awandanto ti Egipto. Dung-awandanto dagiti amin nga adipenna! —kastoy ti pakaammo ti Apo a ni Yahweh!'''
“Mawu angawa adzakhala nyimbo ya maliro. Ana a akazi amitundu ya anthu adzayimba, kuyimbira Igupto ndi gulu lake lonse la nkhondo, akutero Ambuye Yehova.”
17 Ket napasamak nga iti maika-sangapulo ket dua a tawen, iti maika-sangapulo ket lima nga aldaw ti bulan, immay kaniak ti sao ni Yahweh a kunana,
Pa tsiku la 15 la mwezi woyamba, chaka cha khumi ndi chiwiri, Yehova anayankhula kuti:
18 “Anak ti tao, sangitam dagiti adipen ti Egipto ket ibellengmo ida—isuna ken dagiti annak a babbai dagiti nabileg a nasion—iti kababaan a paset ti daga a kadua dagiti napan iti abut!
“Iwe mwana wa munthu, lirira gulu lankhondo la Igupto ndipo uwalowetse pamodzi ndi anthu ena amphamvu a mayiko ena ku dziko la anthu akufa.
19 Saludsudem kadakuada, 'Napinpintaskayo kadi ngem iti siasinoman? Bumabakayo ket agiddakayo a kaduayo dagiti saan a nakugit!'
Ufunse kuti, ‘Ndani amene akukuposa kukongola? Tsikirani ku manda ndi kukhala pamodzi ndi anthu osachita mdulidwe.’
20 Mapasagda ket maitiponda kadagiti napapatay babaen iti kampilan! Naited ti Egipto iti kampilan; tiliwento isuna dagiti kabusorna ken dagiti adipenna!
Aigupto adzagwa pakati pa amene akuphedwa ndi lupanga. Lupanga ndi losololedwa kale. Iye adzaphedwa pamodzi ndi gulu lake lankhondo.
21 Iwaragawagto dagiti kapipigsaan kadagiti mannakigubat iti sheol ti maipapan iti Egipto ken dagiti kakaduana, 'Bimmabadan ditoy! Agiddada a kaduada dagiti saan a nakugit a napapatay babaen iti kampilan!' (Sheol )
Mʼkati mwa manda atsogoleri amphamvu pamodzi ndi ogwirizana nawo azidzakambirana za Igupto nʼkumati, ‘Afika kuno anthu osachita mdulidwe aja! Ndi awa agona apawa, ophedwa pa nkhondo.’ (Sheol )
22 Adda sadiay ti Asiria agraman ti amin a taripnongna! Pinalikmutan isuna dagiti tanemna; aminda ket napapatay babaen iti kampilan.
“Asiriya ali komweko ndipo ankhondo ake onse ali mʼmanda omuzungulira. Onsewo anaphedwa pa nkhondo.
23 Adda sadiay dagiti makin tanem iti adda iti kaunggan a paset ti abut, agraman ti taripnongna. Pinalikmutan dagiti tanemna dagiti amin a napapatay, a napasag babaen iti kampilan, dagiti nangyeg iti pammutbuteng iti daga dagiti sibibiag!
Manda awo ali kumalo ozama a dzenje, ndipo ankhondo ake azungulira manda ake. Onse amene anaopseza dziko la anthu amoyo aphedwa, agwa ndi lupanga.
24 Adda sadiay ti Elam agraman dagiti adipenna! Pinalikmutan isuna dagiti tanemna; napapatayda amin! Dagidiay napasag babaen iti kampilan, a saan a nakugit a bimmaba kadagiti kaadalman a paset ti daga, a nangiyeg kadagiti pammutbutbutengda iti daga dagiti sibibiag ken kaduada a mangaw-awit ita iti bainda, bumabbabadan iti abut!
“Elamu ali komweko ndipo ankhondo ake ali mʼmanda omuzungulira. Onsewa anaphedwa pa nkhondo, natsikira ku manda ali osachita mdulidwe. Iwowa kale ankaopseza anthu pa dziko lapansi. Tsopano akuchita manyazi pamodzi ndi amene ali mʼmanda.
25 Nangisaganada iti pagiddaan para iti Elam ken para kadagiti amin nga adipenna iti nagtetengngaan dagiti napapatay; pinalikmutan isuna dagiti tanemna! Aminda ket saan a nakugit, dagidiay napapatay babaen iti kampilan, dagidiay nangiyeg iti pammutbutengda iti daga dagiti sibibiag! Isu nga awit-awitda ti bukkodda a bain, agraman dagiti bumabbaba iti abut a karaman kadagiti napapatay, dagidiay bumabbaba iti abut. Karaman ti Elam kadagiti napapatay.
Amukonzera pogona pakati pa anthu ophedwa, pamodzi ndi gulu lake lonse la nkhondo litazungulira manda ake. Onsewo ndi anthu osachita mdulidwe ophedwa ndi lupanga. Paja anthuwa ankaopsa mʼdziko la anthu a moyo. Koma tsopano akuchita manyazi pamodzi ndi amene ali mʼmanda. Iwo ayikidwa pakati pa anthu ophedwa.
26 Adda sadiay ti Mesack, Tubal ken dagiti amin nga adipenda! Pinalikmutan ida dagiti tanemda! Aminda ket saan a nakugit, napapatay babaen iti kampilan, gapu ta inyegda dagiti pammutbutbutegda iti daga dagiti sibibiag!
“Mesaki ndi Tubala ali komweko, pamodzi ndi gulu lonse la nkhondo litazungulira manda awo. Onsewo ndi anthu osachita mdulidwe, ophedwa ndi lupanga. Paja ankaopsa mʼdziko la anthu amoyo.
27 Saan kadi a nagiddada a kaduada dagiti napasag a mannakigubat dagiti saan a nakugit a bimmaba iti lubong dagiti natay (Sheol) agraman dagiti amin nga igamda a pakigubat, ken agraman dagiti kampilanda nga impunganda? Naiparabaw dagiti kalasagda kadagiti tulangda. Ta isuda dagiti mangbutbuteng a mannakigubat iti daga dagiti sibibiag! (Sheol )
Iwo sanayikidwe mwaulemu ngati ankhondo amphamvu amakedzana, amene anatsikira ku dziko la anthu akufa ndi zida zawo zomwe za nkhondo. Malupanga awo anawayika ku mitu yawo, ndipo zishango zawo anaphimba mafupa awo. Kale anthu amphamvu amenewa ankaopsa dziko la anthu amoyo. (Sheol )
28 Isu a sika nga Egipto, ket madadaelto iti nagtetengngaan dagiti saan a nakugit! Ken agiddakanto a kaduam dagiti napapatay babaen iti kampilan!
“Iwenso Farao, udzaphwanyidwa ndi kuyikidwa pakati pa anthu osachita mdulidwe, amene anaphedwa ndi lupanga.
29 Adda sadiay ti Edom agraman dagiti arina ken dagiti amin a pangulona. Nabilegda idi, ngem itan ket nakaiddada a kaduada dagiti napapatay babaen iti kampilan, kaduada dagiti saan a nakugit ken dagiti bimmaba iti abut.
“Edomu ali kumeneko pamodzi ndi mafumu ake ndi akalonga ake onse. Ngakhale anali amphamvu, koma anayikidwa. Ayikidwa pamodzi ndi anthu osachita mdulidwe, pamodzi ndi iwo amene akutsikira ku dzenje.
30 Adda sadiay dagiti prinsipe iti amianan—aminda ken amin a taga-Sidon a bimmaba a kadua dagiti natay! Nabilegda ken pinagbutengda dagiti dadduma, ngem itan ket nakaiddada sadiay a mababain, saan a nakugit a kaduada dagiti napapatay babaen iti kampilan. Awit-awitda ti bukodda a bain, kaduada dagiti dadduma a bumabbaba iti abut.
“Akalonga onse akumpoto pamodzi ndi anthu onse a ku Sidoni ali kumeneko. Anatsikira ku dziko la anthu akufa mwamanyazi ngakhale anali owopsa ndi mphamvu zawo. Iwo akugona osachita mdulidwe pamodzi ndi amene anaphedwa ndi lupanga ndipo akuchita manyazi pamodzi ndi iwo amene anatsikira kale ku manda.
31 Kumitanto ni Faraon ken maliwliwanto maipapan kadagiti amin nga adipenna a napapatay babaen iti kampilan—kastoy ti pakaammo ti Apo a ni Yahweh.
“Farao ndi gulu lake lankhondo akadzawaona iwowa adzathunza mtima pokumbukira kuchuluka kwa gulu lake lankhondo limene linaphedwa pa nkhondo. Ndikutero Ine Ambuye Yehova.
32 Intulokko a mangbutbuteng isuna iti daga dagiti sibibiag, ngem agiddanto isuna iti nagtetengngaan dagiti saan a nakugit, a kaduana dagiti napapatay babaen iti kampilan—kastoy ti pakaammo ti Apo a ni Yahweh!”
Paja ankaopsa mʼdziko la anthu amoyo. Koma Faraoyo pamodzi ndi ankhondo ake onse adzayikidwa pamodzi ndi anthu osachita mdulidwe, pamodzi ndi amene anaphedwa pa nkhondo. Ndikutero Ine Ambuye Yehova.”