< Ezekiel 30 >

1 Immay kaniak ti sao ni Yahweh a kunana,
Yehova anandiyankhula kuti:
2 “Anak ti tao, agipadtoka ket ibagam, 'kastoy ti kuna ti Apo a ni Yahweh: Idung-awmo, “Asi pay ti dumteng nga aldaw!”
“Iwe mwana wa munthu, nenera ndipo ulengeze zimene Ine Ambuye Yehova ndikunena. “‘Ufuwule mawu awa akuti, ‘Kalanga, tsiku lafika!’
3 Asidegen ti aldaw! Asidegen ti aldaw para kenni Yahweh! Aldawto daytoy dagiti ulep, tiempo a mapasamakto dagiti nakabutbuteng a banbanag kadagiti nasion!
Pakuti tsiku layandikira, tsiku la Yehova lili pafupi, tsiku la mitambo yakuda, tsiku lachiwonongeko cha mitundu ya anthu.
4 Kalpasanna, umayto ti kampilan a maibusor iti Egipto, ket addanto panagladingit idiay Cus inton maidasay idiay Egipto dagiti napapatay a tattao—inton alaenda ti kinabaknangna, ken inton madadael dagiti pundasionna!
Lupanga lidzabwera kudzalimbana ndi Igupto ndipo mavuto adzafika pa Kusi. Pamene anthu ambiri adzaphedwa mu Igupto, chuma chake chidzatengedwa ndipo maziko ake adzagumuka.
5 Ti Cus, Libya, ken Lydia ken dagiti amin a ganggannaet, agraman dagiti tattao a maibilang iti katulagan—mapasagdanto amin babaen iti kampilan!
Kusi, Puti, Ludi ndi Arabiya yense, Libiya ndiponso anthu a mʼdziko logwirizana naye adzaphedwa ndi lupanga pamodzi ndi Igupto.
6 Kastoy ti kuna ni Yahweh: Mapasagto ngarud dagiti mangtultulong iti Egipto, ken mapukawto ti kinatangsit ti pigsana. Mapasagto dagiti soldadoda manipud Migdol agingga iti Siene babaen iti kampilan! —Kastoy ti pakaammo ti Apo a ni Yahweh!
“‘Ine Ambuye Yehova ndikuti: “‘Onse othandiza Igupto adzaphedwa ndipo kunyadira mphamvu zake kudzatheratu. Adzaphedwa ndi lupanga kuyambira ku Migidoli mpaka ku mzinda wa Asiwani,’” ndikutero Ine Ambuye Yehova.
7 Maupaydanto iti nagtetengngaan dagiti nabaybay-an a daga, ken maibilangto dagiti siudadda kadagiti nadadael a siudad!
“‘Dziko la Igupto lidzasanduka bwinja kupambana mabwinja ena onse opasuka, ndipo mizinda yake idzakhala yopasuka kupambana mizinda ina yonse.
8 Ket maammoandanto a Siak ni Yahweh, inton mangpasgedak iti apuy iti Egipto, ken inton madadael dagiti amin a mangtultulong kenkuana!
Nditatha kutentha Igupto ndi kupha onse omuthandiza, pamenepo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.
9 Iti dayta nga aldaw, manipud iti sangoanak, rummuarto dagiti mensahero a nakabarko tapno butbutngenda ti natalged a Cus, ket addanto panagladingit kadakuada iti aldaw a mapasamak iti Egipto dagiti nakabutbuteng a banbanag. Ta adtoy! Umadanin daytoy!
“‘Nthawi imeneyo ikadzafika, amithenga adzapita mofulumira kuchokera kwa Ine kukaopseza Kusi, iwowo osadziwako kanthu. Ndipo adzada nkhawa pa tsiku limene Igupto adzawonongedwa, chifukwa tsikulo lidzafika ndithu.
10 Kastoy ti kuna ti Apo a ni Yahweh: Gibusakto dagiti adu a tattao ti Egipto babaen iti ima ni Nebucadnesar nga ari ti Babilonia.
“‘Ine Ambuye Yehova ndikuti, “‘Ndidzagwiritsa ntchito Nebukadinezara, mfumu ya ku Babuloni kuti ndithetse gulu lankhondo la Igupto.
11 Isuna ken dagiti armadana, dagiti mangbutbuteng kadagiti nasion ket maiyegto a mangdadael iti daga; asutendanto dagiti kampilanda maibusor iti Egipto ken punnoenda ti daga kadagiti natay a tattao!
Iye ndi gulu lake lankhondo, mtundu wa anthu ankhanza kwambiri aja adzabwera kudzawononga dzikolo. Adzasolola malupanga awo kulimbana ndi Igupto ndipo dziko lidzadzaza ndi mitembo.
12 Pagbalinekto a namaga a daga dagiti karayan, ket ilakokto ti daga kadagiti nadangkes a tattao. Pagbalinekto a langalang ti daga ken ti amin nga adda iti daytoy babaen iti ima dagiti ganggannaet! Siak a ni Yahweh, ti nangipakaammo iti daytoy!
Ndidzawumitsa mtsinje wa Nailo ndi kugulitsa dziko la Igupto kwa anthu oyipa. Ndidzagwiritsa ntchito anthu achilendo kuti ndiwononge dzikolo pamodzi ndi zonse zili mʼmenemo. Ine Yehova ndayankhula.
13 Kastoy ti kuna ti Apo a ni Yahweh: Dadaelekto dagiti didiosen, ken gibusakto dagiti awan serserbina a didiosen ti Memfis. Awanto iti prinsipe iti daga ti Egipto, ket butbutngekto ti daga ti Egipto!
“‘Ine Ambuye Yehova ndikuti, “‘Ndidzawononga mafano ndi kuthetsa milungu yosema ya ku Mefisi. Simudzakhalanso mfumu mu Igupto, ndipo ndidzaopseza dziko lonse.
14 Ket pagbalinekto a langalang ti Patros ken mangpasgedak iti apuy idiay Zoan, ken ukomekto ti Tebes.
Ndidzasandutsa chipululu mzinda wa Patirosi, ndi kutentha mzinda wa Zowani. Ndidzalanga mzinda wa Thebesi.
15 Ta ibukbukkonto ti pungtotko iti Pelusium, ti sarikedked ti Egipto, ken gibusakto dagiti adu a tattao ti Tebes.
Ndidzakhuthulira ukali wanga pa mzinda wa Peluziumu, linga lolimba la Igupto, ndi kuwononga gulu lankhondo la Thebesi.
16 Kalpasanna, mangpasgedakto iti apuy idiay Egipto. Agladingitto iti nakaro ti Pelusium, ken madadaelto ti Tebes. Inaldawto nga adda kabusor ti Memfis.
Ndidzatentha ndi moto dziko la Igupto; Peluziumu adzazunzika ndi ululu. Malinga a Thebesi adzagumuka, ndipo mzindawo udzasefukira ndi madzi.
17 Mapasagto dagiti agtutubo a lallaki ti Heliopolis ken Bubastis babaen iti kampilan, ken masakupto dagiti siudadda.
Anyamata a ku Oni ndi ku Pibeseti adzaphedwa ndi lupanga ndipo okhala mʼmizinda yake adzatengedwa ukapolo.
18 Idiay Tafnes, iyimutto ti aldaw ti lawagna inton dadaelek sadiay ti sangol ti Egipto, ken agpatingganto ti kinatangsit ti pigsana. Addanto ulep a manglinged kenkuana, ken matiliwto a kas balud dagiti annakna a babbai.
Ku Tehafinehezi kudzakhala mdima pamene ndidzathyola goli la Igupto; motero kunyada kwake kudzatha. Iye adzaphimbidwa ndi mitambo yakuda, ndipo okhala mʼmizinda yake adzapita ku ukapolo.
19 Ipatungpalkonto ti panangukomko idiay Egipto tapno maammoanda a siak ni Yahweh.'''
Kotero ndidzalanga dziko la Igupto, ndipo iwo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.’”
20 Ket napasamak nga iti maika-sangapulo ket maysa a tawen iti maika-pito nga aldaw iti umuna a bulan, immay kaniak ti sao ni Yahweh a kunana,
Pa tsiku lachisanu ndi chiwiri la mwezi woyamba wa chaka chakhumi ndi chimodzi, Yehova anandiyankhula kuti:
21 “Anak ti tao, tinukkolko ti takkiag ni Faraon nga ari ti Egipto. Kitaem! Saan daytoy a nabedbedan ken saan a makaawat iti agas; awan ti makabael a mangbedbed iti daytoy, isu a saan a napigsa a mangiggem iti kampilan.
“Iwe mwana wa munthu, ndathyola dzanja la Farao mfumu ya Igupto. Taona, silinamangidwe kuti lipole, ngakhale kulilimbitsa ndi nsalu kuti lithe kugwiranso lupanga.
22 Ngarud, kastoy ti kuna ti Apo a ni Yahweh, 'Kitaem, ni Faraon nga ari ti Egipto! Ta tukkolekto ti takkiagna, ti napigsa ken ti natukkol, ken tinnagekto ti kampilan manipud iti imana.
Nʼchifukwa chake Ine Ambuye Yehova ndikuti, Ine ndikudana ndi Farao mfumu ya Igupto. Ndidzathyola manja ake onse; dzanja labwino pamodzi ndi lothyokalo, ndipo lupanga lidzagwa mʼmanja mwake.
23 Ket iwarawarakto ti Egipto kadagiti nasion ken iwaraskonto ida kadagiti daga.
Ndidzamwaza Aigupto pakati pa mitundu ya anthu ndikuwabalalitsira ku mayiko ambiri.
24 Papigsaekto dagiti takkiag ti ari ti Babilonia ken ipaiggemko ti kampilanko iti imana tapno madangrak ti takkiag ni Faraon. Agasugto isuna iti sangoanan ti ari ti Babilonia a kas iti panagasug ti matmatay a tao.
Ndidzalimbitsa manja a mfumu ya ku Babuloni, ndipo mʼmanja mwake ndidzayikamo lupanga langa. Koma ndidzathyola manja a Farao, ndipo adzabuwula ngati wolasidwa koopsa pamaso pa mfumu ya ku Babuloniyo.
25 Ta papigsaekto dagiti takkiag ti ari ti Babilonia, bayat a kumapkapuy dagiti ima ni Faraon. Ket maammoandanto a siak ni Yahweh, inton ipaiggemko ti kampilanko iti ima ti ari ti Babilonia; ta rautennanto ti daga ti Egipto babaen iti daytoy.
Ndidzalimbitsa manja a mfumu ya ku Babuloni, koma manja a Farao adzafowoka. Motero anthu adzadziwa kuti Ine ndine Yehova, ndikadzayika lupanga langa mʼmanja mwa mfumu ya ku Babuloni. Ndipo adzaligwiritsa ntchito pothira nkhondo dziko la Igupto.
26 Isu nga iwarawarakto ti Egipto kadagiti nasion ken iwarasko ida kadagiti daga. Ket maammoandanto a siak ni Yahweh!'''
Ndidzamwaza Aigupto pakati pa mitundu ya anthu, ndikuwabalalitsira ku mayiko ambiri. Motero adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.”

< Ezekiel 30 >