< Ezekiel 27 >

1 Immay manen kaniak ti sao ni Yahweh a kunana,
Yehova anandiyankhula kuti:
2 “Ita, sika nga anak ti tao, irugim ti agdung-aw maipapan iti Tiro,
“Iwe mwana wa munthu, imba nyimbo yodandaulira Turo.
3 ken ibagam iti Tiro, 'Sika nga agnanaed kadagiti pagserkan ti baybay, agtagtagilako iti ayan dagiti tattao kadagiti adu nga isla, kastoy ti kuna ti Apo a ni Yahweh: Tiro! Imbagam, “Nakapimpintasak unay!”
Uza Turo, mzinda wokhala pa dooko la nyanja, wochita malonda ndi anthu ambiri a mʼmbali mwa nyanja kuti: Ambuye Yehova akuti, “Iwe Turo, umanena kuti, ‘Ndine wokongola kwambiri.’
4 Dagiti beddengmo ket adda iti tengnga iti baybay; pinapintasdaka iti kasta unay dagiti nangaramid kenka.
Malire ako anali mʼkati mwenimweni mwa nyanja; amisiri ako anakukongoletsa kwambiri.
5 Ti inaramatda a tarikayom ket saleng a naggapu iti Bantay Hermon; nangalada iti kayo a sedro manipud Libano tapno aramidenda a palom.
Anakupanga ndi matabwa a payini ochokera ku Seniri; anatenga mikungudza ya ku Lebanoni kupangira mlongoti wako.
6 Ti inaramidda a gaudmo ket lugo a naggapu idiay Basan; ti inaramidda a kamarotem ket alamo a naggapu idiay Cyprus, ken kinalupkopanda daytoy iti marfil.
Ndi mitengo ya thundu ya ku Basani anapanga zopalasira zako; ndi matabwa a mitengo ya payini yochokera ku zilumba za Kitimu. Pakuti anapanga thandala lako pakati pa matabwawo panali minyanga ya njovu.
7 Dagiti layagmo ket nabordaan iti linen a naggapu idiay Egipto nga agserbi met laeng a banderam!
Nsalu yabafuta yopeta yochokera ku Igupto inali thanga yako, ndipo inakhala ngati mbendera. Nsalu zophimba matenti ako zinali za mtundu wamtambo ndi pepo zochokera ku zilumba za Elisa.
8 Dagiti agnanaed iti Sidon ken Arvad dagiti para-gaudmo, adda kenka dagiti agkakalaing a tattao ti Tiro; isuda ti marinerom.
Anthu a ku Sidoni ndi Arivadi ndi amene anali opalasa ako. Anthu aluso ako, iwe Turo, anali mwa iwe ndiwo amene ankakuyendetsa.
9 Nasanay a lallaki a kumikitikit manipud Biblos ti nangtarimaan kadagiti birrim; dagiti tagilakom ket aw-awiten dagiti amin a barko iti baybay ken dagiti lumalayagda para iti pannakisinnukat!
Akuluakulu ndi eni luso a ku Gebala anali mʼkati mwako, ngati okonza zibowo zako. Sitima za pa nyanja zonse, ndi oyendetsa ake ankabwera pamodzi ndi katundu kudzachita nawe malonda.
10 Ti Persia, Lydia, ken Libya ket adda iti armadam, dagiti tattaom a mannakigubat! Nangibitbitinda kenka kadagiti kalasag ken helmet; impakitada ti dayagmo!
“Anthu a ku Perisiya, a ku Ludi ndi Puti anali asilikali mʼgulu lako la nkhondo. Iwo ankapachika zishango ndi zipewa zawo zankhondo pa makoma ako, kubweretsa kwa iwe ulemerero.
11 Dagiti lallaki a taga- Arvad ken Helek a kameng ti armadam ket adda kadagiti padermo a nakapalikmut kenka, ken dagiti tattao ti Gamad ket adda kadagiti torrem! Imbitinda dagiti kalasagda kadagiti bakud iti aglawlawmo! Isuda ti nangan-anay iti pintasmo!
Anthu a ku Arivadi ndi Heleki ankalondera mbali zonse za mpanda wako; anthu a ku Gamadi anali mu nsanja zako, Iwo ankapachika zishango zawo pa makoma ako onse. Amenewo ndiwo anakukongoletsa kwambiri.
12 Ti Tarsus ti kinatinagilakom gapu iti kinaadu ti amin a kita ti kinabaknang; pirak, landok, lata ken buli. Gatangenda ken ilakoda dagiti tagilakom!
“Dziko la Tarisisi linachita nawe malonda chifukwa cha kuchuluka kwa katundu wako wamtundumtundu. Iwo ankapereka siliva, chitsulo, chitini ndi mtovu mosinthanitsa ndi katundu wako.
13 Ti Javan, Tubal ken Mesec—isuksukatda dagiti tagabu ken alikamen a naaramid iti bronse. Makisinsinnukatda kadagiti tagilakom.
“Yavani, Tubala ndi Mesaki ankachita nawe malonda; iwo ankapereka akapolo ndi ziwiya za mtovu mosinthanitsa ndi katundu wako.
14 Ti Bet Togarma ket mangipapaay kadagiti kabalio a pagtrabaho ken kabalio a pakigubat ken mulo a kas sukat dagiti tagilakom.
“Anthu a ku Beti Togarima ankapereka akavalo antchito, akavalo ankhondo ndi abulu mosinthanitsa ndi katundu wako.
15 Dagiti tattao iti Rodes ket makinegnegosio kenka kadagiti adu nga igid ti baybay. Adu ti tagilakom; mangyegda iti sara, marfil, ken ballatinaw a kas sukat dagiti tagilakom!
“Anthu a ku Dedani ankachita nawe malonda, ndipo anthu ambiri a mʼmbali mwa nyanja anali ogula malonda ako. Ankakupatsa minyanga ya njovu ndi phingo.
16 Ti Aram ket nakinegnegosio kenka kadagiti adu a tagilakom; mangisabsabetda iti esmeralda, purpura, adda marisna a lupot, perlas, ken kadagiti rubi a kas sukat dagiti tagilakom.
“Anthu a ku Aramu ankachita nawe malonda chifukwa cha kuchuluka kwa zinthu zako. Iwo ankapereka miyala ya emeradi, nsalu zapepo, nsalu zopetapeta, nsalu zabafuta, korali ndi miyala ya rubi mosinthanitsa ndi katundu wako.
17 Nakinegnegosio kenka ti Juda ken ti daga ti Israel. Nangisabsabetda iti trigo manipud iti Minith, bungbunga ti igos, diro, lana ken bangbanglo a kas sukat dagiti tagilakom.
“Yuda ndi Israeli ankachita nawe malonda. Iwo ankapereka tirigu ochokera ku Miniti ndi zokometsera zakudya, uchi, mafuta ndi mankhwala mosinthanitsa ndi katundu wako.
18 Ti Damasco ket nakisinsinnukat kenka kadagiti amin a tagilakom; kadagiti amin a kinabaknangmo, ken iti arak ti Helbon ken iti puraw nga inabel a dutdot ti karnero a naggapu iti Sahar.
“Anthu a ku Damasiko, chifukwa cha zinthu zako za malonda zambiri ndi katundu wako wosiyanasiyana, ankachita nawe malonda a vinyo wochokera ku Heliboni ndi ubweya wankhosa ochokera ku Zahari.
19 Ti Dan ken Javan ket mangisabsabet kenka kadagiti tagilako a napanday a landok, cinnamon, ken calamus a naggapu iti Uzal. Dagitoy ti insukatda kadagiti tagilakom.
Adani ndi Agriki ochokera ku Uzala ankagula katundu wako. Iwo ankapereka chitsulo chosalala, kasiya ndi bango lonunkhira mosinthanitsa ndi katundu wako.
20 Ti Dedan ket mangmangyeg kenka kadagiti lupot a pagap-ap iti pagsakayan.
“Anthu a ku Dedani ankakugulitsa nsalu zoyika pa zishalo za akavalo.
21 Nakinegosio kenka ti Arabia ken dagiti amin a pangulo ti Kedar; mangmangyegda kenka kadagiti urbon a karnero, kalakian a karnero ken kalding.
“Arabiya ndi mafumu onse a ku Kedara anali ogula malonda ako. Iwo ankachita nawe malonda a ana ankhosa onenepa, nkhosa zazimuna ndi mbuzi.
22 Dagiti agtagtagilako manipud iti Seba ken Raama ket immay tapno agilakoda kenka kadagiti kasasayaatan a kita ti amin a bangbanglo ken iti amin a kita ti napapateg a batbato; balitok ti isuksukatda kadagiti tagilakom.
“Anthu amalonda a ku Seba ndi Raama ankachita nawe malonda. Iwo ankapereka zonunkhira zosiyanasiyana zabwino kwambiri, miyala yokongola ndi golide mosinthanitsa ndi katundu wako.
23 Makinegnegosio kenka ti Haran, Canne, ken Eden, agraman ti Seba, Assur ken Kilmad.
“Amalonda a ku Harani, Kane, Edeni, Seba, Asuri ndi Kilimadi ankachita nawe malonda.
24 Dagitoy dagiti agilaklako kadagiti pagtagtagilakoam kadagiti agkakangina a kagay a maris ube ken naburdaan kadagiti kolor, ken kadagiti ules nga adu kolorna, naburdaan, ken nasayaat ti pannakaabelna a lupot.
Iwowa ankasinthanitsana nawe zovala zokongola, nsalu zopetapeta, zoyala pansi za mawangamawanga, atazimanga bwino ndi zingwe zolimba.
25 Dagiti barko ti Tarshish ti mangkarkarga kadagiti tagilakom! Isu a napnoka, napnoka kadagiti tagilako iti tengnga dagiti baybay!
“Sitima za pa madzi za ku Tarisisi zinali zonyamula malonda ako. Motero iwe uli ngati sitima yapamadzi yodzaza ndi katundu wolemera.
26 Impandaka dagiti para-gaudmo kadagiti nalawa a baybay; dinadaelnaka ti angin-daya iti tengnga dagitoy.
Anthu opalasa ako amakupititsa pa nyanja yozama. Koma mphepo yakummawa idzakuthyolathyola pakati pa nyanja.
27 Ti kinabaknangmo, dagiti tagilakom, ken dagiti banbanag a negosiom; dagiti marinerom, dagiti para—layagmo, ken dagiti para-aramid kadagiti barko; dagiti agtagtagilakom ken amin dagiti lallaki a mannakigubatmo nga adda kenka, ken amin a kakaduam—matnagdanto iti kaadalman ti baybay iti aldaw ti pannakadadaelmo.
Chuma chako, katundu wako, malonda ako, okuyendetsa ako, okuwongolera ako ndi opanga sitima za pa madzi, anthu ako amalonda ndi asilikali ako onse ndiponso aliyense amene ali mʼmenemo adzamira mʼnyanja tsiku limene udzawonongeka.
28 Agpigerger dagiti siudad iti baybay iti uni dagiti sangsangit dagiti pilotom;
Madera a mʼmbali mwa nyanja adzagwedezeka chifukwa cha kufuwula kwa oyendetsa sitimawo.
29 Bumabanto amin dagiti para-gaudmo manipud kadagiti barkoda; agtakderto iti daga dagiti marinero, ken tunggal aglaylayag iti baybay.
Onse amene amapalasa sitima zapamadzi, adzatuluka mʼsitima zawo; oyendetsa ndi onse owongolera sitima zapamadzi adzayimirira mʼmbali mwa nyanja.
30 Ket ipangngegdanto kenka ti timekda ken agdung-awda iti nasaem; mangipurruakda iti tapok kadagiti uloda. Agtulidtulidda kadagiti dapu.
Iwo akufuwula, kukulira iwe kwambiri; akudzithira fumbi kumutu, ndi kudzigubuduza pa phulusa.
31 Kuskosanda dagiti uloda ken agkawesda iti nakersang a lupot, ken sangitandakanto iti nasaem, ken umasugda.
Akumeta mpala mitu yawo chifukwa cha iwe ndipo akuvala ziguduli. Akukulira iweyo ndi mitima yowawa kwambiri.
32 Dung-awandaka ken ikantaandaka kadagiti pangnatay a kanta, a kas iti Tiro, a napaulimek ita iti tengnga ti baybay?
Akuyimba nyimbo yokudandaulira nʼkumati: ‘Ndani anawonongedwapo ngati Turo pakati pa nyanja?’
33 Idi napan dagiti tagilakom kadagiti igid ti baybay, pinennek daytoy dagiti adu a tattao; pinabaknangmo dagiti ar-ari ti daga babaen iti kasta unay a kinabaknangmo ken tagtagilakom!
Pamene malonda ako ankawoloka nyanja unakhutitsa mitundu yambiri ya anthu. Mafumu a dziko lapansi analemera ndi chuma chako komanso ndi malonda ako.
34 Ngem idi dinadaelnaka dagiti baybay, babaen kadagiti nauuneg a danum, limned dagiti amin a tagilakom ken amin dagiti aglaylayagmo!
Koma tsopano wathyokera mʼnyanja, pansi penipeni pa nyanja. Katundu wako ndi onse amene anali nawe amira pamodzi nawe.
35 Naupay kenka dagiti amin nga agnanaed kadagiti igid ti baybay, ken nagbuteng dagiti arida gapu iti napasamak kenka!
Onse amene amakhala mʼmbali mwa nyanja aopsedwa ndi zimene zakuchitikira. Mafumu awo akuchita mantha ndipo nkhope zangoti khululu.
36 Nagpigergerda! Nagsakuntip dagiti agtagtagilako gapu kenka; nagbalinka a pagbutbutngan, ken mapukawkan iti agnanayon.”'
Anthu amalonda a mitundu ina akukunyogodola. Watha mochititsa mantha ndipo sudzakhalaponso mpaka muyaya.”

< Ezekiel 27 >