< Ezekiel 12 >

1 Immay kaniak ti sao ni Yahweh a kunana,
Yehova anayankhula nane kuti,
2 “Anak ti tao, makipagnanaedka iti nagtetengngaan dagiti nasukir a tattao, addaanda iti mata ngem saanda a makakita; addaanda iti lapayag ngem saanda a makangngeg, gapu ta nasukirda a tattao.
“Iwe mwana wa munthu, ukukhala pakati pa anthu owukira, iwowo maso openyera ali nawo, koma sakuona ndipo makutu omvera ali nawo, koma sakumva chifukwa choti ndi anthu owukira.
3 Isu a no maipapan kenka, anak ti tao, isaganam dagiti gargaretmo para iti ipapanawmo, ket iti aldaw, agrubbuatka bayat a siiimatangda, ta papanawenkanto bayat a siiimatangda ket ipanka iti sabali a lugar. Nalabit a mangrugida a makakita, uray nasukirda a tattao.
“Choncho, iwe mwana wa munthu, longedza katundu wako wopita naye ku ukapolo. Unyamuke nthawi yamasana iwo akuona. Uchite ngati wanyamuka kuchoka kumene ukukhala kupita ku dziko lachilendo iwowo akuona. Mwina adzamvetsetsa, paja ndi anthu aupandu.
4 Ket iti aldaw bayat a kitkitaendaka, irubbuatmo dagiti gargaretmo para iti ipapanawmo; iti rabii bayat a kitkitaenda, agrubbuatka a kas iti wagas nga ar-aramiden ti siasinoman a matiliw a maipan iti sabali a pagilian.
Utulutse katundu wako wopita naye ku ukapolo nthawi ya masana iwo akuona. Ndipo nthawi ya madzulo, iwo akuona, uchoke monga ngati ukupita ku ukapolo.
5 Abutam ti diding bayat a kitkitaenda, ket idiay ti pagnaam a rummuar.
Iwo akuona, ubowole pa khoma ndipo utulutsirepo katundu wako.
6 Iti imatangda, ibaklaymo dagiti gargaretmo, ket irruarmo dagitoy iti kasipngetan. Abbongam ti rupam, ta masapul a saanmo a makita ti daga, agsipud ta insaadka a kas pagilasinan iti balay ti Israel.”
Usenze katundu wako pa phewa iwo akuona, ndipo upite kunja ku mdima. Uphimbe nkhope yako kuti usaone pansi, pakuti ndakusandutsa iwe chizindikiro chochenjeza Aisraeli.”
7 Inaramidko ngarud daytoy, a kas naibilin kaniak. Iti aldaw, inrubbuatko dagiti gargaret nga itugotko iti ipapanawko, ket iti rabii, inabutak ti diding. Idi nasipngeten, inruarko dagiti gargaretko ket imbaklayko dagitoy iti imatangda.
Choncho ine ndinachita monga momwe anandilamulira. Nthawi yamasana ndinatulutsa zinthu zanga nditazimanga ngati ndikupita ku ukapolo. Ndipo nthawi yamadzulo ndinabowola khoma ndi manja anga. Pamene chisisira chinkayamba, ndinasenza katundu wanga pa phewa kutuluka naye iwo akuona.
8 Kalpasanna, iti parbangon, immay ti sao ni Yahweh kaniak a kunana,
Mmawa mwake Yehova anandiyankhula nati:
9 “Anak ti tao, saan kadi a nagdamdamag ti balay ti Israel, dagita a managsukir a tattao, a kunada, 'Ania ti ar-aramidem?'
“Iwe mwana wa munthu, kodi anthu aupandu a Israeli sanakufunse kuti ukuchita chiyani?
10 Ibagam kadakuada, ‘Kastoy ti kuna ni Yahweh nga Apo: Daytoy a padto nga ipakpakitak kadakayo ket maipapan iti prinsipe ti Jerusalem, ken iti amin a balay ti Israel nga adda iti nagbabaetanda.'
“Uwawuze kuti, ‘zimene ndikunena Ine Ambuye Wamphamvuzonse ndi izi: Uthengawu ndi wonena za kalonga wa ku Yerusalemu pamodzi ndi banja lonse la Israeli amene akukhala kumeneko.’
11 Ibagam, 'Siak ti pagilasinanyo. Kas iti inaramidko, kastanto met ti maaramid kadakuada; matiliw ken maipanawdanto ket maipanda iti sabali a pagilian.
Uwawuze kuti, ‘Ndiwe chizindikiro chowachenjeza.’ “Zidzakuchitikirani monga momwe zakuchitikira iwemu. Iwo adzatengedwa kupita ku ukapolo.”
12 Ti prinsipe nga adda kadakuada, ibaklaynanto dagiti gargaretna iti kasipngetan, magnanto iti naabutan a pader. Abutandanto ti pader ket irruardanto dagiti gargaretda sadiay. Abbongannanto ti rupana, tapno saanna a makita ti daga.'
“Kalonga wawo adzatenga katundu wake nʼchisisira nʼkunyamuka. Adzatulukira pa bowo limene anthu anabowola pa khoma. Adzaphimba nkhope yake kuti asaone kumene akupita.
13 Isarwagkonto ti iketko kenkuana ket matiliwto isuna iti palab-ogko; ket ipankonto isuna idiay Babilonia, ti daga dagiti Caldeo, ngem saannanto a makita daytoy. Matayto isuna sadiay.
Ndidzayala ukonde wanga pa iye ndi kumukola mu msampha wanga. Ndidzabwera naye ku Babuloni, dziko la Akaldeya, koma sadzaliona dzikolo, ndipo adzafera kumeneko.
14 Iwarawarakto met iti amin a paset, dagiti amin nga adda iti aglalawna a mangtultulong kenkuana ken dagiti amin a soldadona, ket mangibaonakto iti kampilan a mangkamat kadakuada.
Ine ndidzabalalitsa kumbali zonse zinayi onse okhala naye pafupi, ndiwo omuthandiza ake pamodzi ndi ankhondo ake. Ndidzawalondola ndi lupanga losolola.
15 Ket maammoandanto a siak ni Yahweh, inton iwarawarak ida kadagiti nasion ken iwarasko ida iti entero a daga.
“Iwo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova, ndikadzawamwaza pakati pa anthu a mitundu ina ndi kuwabalalitsira ku mayiko ena.
16 Ngem ispalekto ti sumagmamano a lallaki kadakuada manipud iti kampilan, iti nakaro a panagbisin, ken iti angol, tapno maisuratda amin dagiti nakarimrimon nga aramidda iti daga a pangipanak kadakuada, isu a maammoandanto a siak ni Yahweh!”
Koma ndidzasiyako ena pangʼono amene adzapulumuke ku lupanga, njala ndi mliri, kuti akafotokoze ntchito zawo zonse zonyansa pakati pa anthu achilendo kumene akupitako. Pamenepo adzadziwa kuti ndine Yehova.”
17 Immay ti sao ni Yahweh kaniak a kunana,
Pambuyo pake Yehova anandiyankhulanso nati,
18 “Anak ti tao, agtigergerka a mangan iti tinapaymo ken agpigerger ken agdanagka nga uminum iti danummo.
“Iwe mwana wa munthu, uzinjenjemera ukamadya chakudya chako, ndipo uzinthunthumira ndi mantha ukamamwa madzi ako.
19 Kalpasanna, ibagam kadagiti tattao iti daga, 'Kastoy ti kuna ni Yahweh nga Apo maipapan kadagiti agnanaed iti Jerusalem ken iti daga ti Israel: Agtigtigergerdanto a mangan iti taraonda ken agpigpigergerdanto bayat nga in-inumenda ti danumda, agsipud ta masamsamto dagiti adu unay nga adda iti daga gapu iti kinaranggas dagiti amin nga agnanaed sadiay.
Uwawuze anthu a mʼdzikomo kuti izi ndi zimene Ambuye Wamphamvuzonse akunena za anthu okhala mu Yerusalemu ndi dziko la Israeli: Iwo adzadya chakudya chawo ndi mantha ndi kumwa madzi awo ndi nkhawa. Zonse za mʼdziko lawo zidzalandidwa chifukwa cha ziwawa za anthu onse okhala mʼmenemo.
20 Isu a dagiti siudad nga adda agnanaed, agbalinto a langalang, agbalinto a let-ang ti daga; isu a maammoanyonto a siak ni Yahweh!”
Mizinda imene ili ndi anthu idzasakazika ndipo dziko lidzasanduka chipululu. Pamenepo inu mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova.”
21 Immay manen kaniak ti sao ni Yahweh a kunana,
Yehova anayankhulanso nane kuti,
22 “Anak ti tao, ania daytoy a pagsasao nga ibagbagada iti daga ti Israel, a kunana, 'Naglabasen dagiti aldaw, ngem saan met a napasamak ti sirmata?’
“Iwe mwana wa munthu, kodi mwambi umene ukunenedwa mu Israeli ndi wotani: ‘Masiku akupita koma masomphenya onse sakukwaniritsidwa?’
23 Isu nga ibagam kadakuada, 'Kastoy ti kuna ni Yahweh nga Apo: Pagpatinggaek daytoy nga ibagbagada tapno saanen nga ibaga dagiti tattao daytoy.' Kalpasanna, ipakaammom kadakuada, 'Umadanin dagiti aldaw, ket tunggal sirmata, pumaysonto!'
Choncho uwawuze anthuwo kuti, ‘Ine Ambuye Yehova ndidzawuthetsa mwambi umenewu ndipo sadzawunenanso mu Israeli.’ Uwawuze kuti, ‘masiku ayandikira oti zonse zimene ndinanena mʼmasomphenya zichitikedi.
24 Ta awanton dagiti saan a pudno a sirmata ken dagiti makaallilaw a panagipadto iti uneg ti balay ti Israel.
Pakuti masiku amenewo sikudzakhalanso masomphenya abodza kapena kuwombeza kwa chinyengo pakati pa anthu a Israeli.
25 Ta siak ni Yahweh! Agsaoak ken tungpalek dagiti sasao nga ibagak. Saanton a maitantan daytoy a banag. Ta ibagbagak daytoy a sao bayat a sibibiagkayo, dakayo a nasusukir a tattao, ket ipatungpalko daytoy! —Kastoy ti pakaammo ni Yahweh nga Apo.”
Koma Ine Ambuye ndidzayankhula chimene ndikufuna, ndipo chidzachitikadi, osachedwa ayi. Pakuti mʼmasiku anu omwe ano, inu anthu opanduka, ndidzakwaniritsa chilichonse chimene ndidzanena. Ndikutero Ine Yehova.’”
26 Immay manen kaniak ti sao ni Yahweh a kunana,
Yehova anandiyankhula nati:
27 “Anak ti tao, denggem! Kinuna ti balay ti Israel, 'Ti sirmata a makitkitana ket mapasamakto iti adu nga al-aldaw manipud ita, ket agipadpadto isuna iti mabayag pay a mapasamak.'
“Iwe mwana wa munthu, Aisraeli akunena kuti, ‘masomphenya amene ukuona sadzachitika kwa zaka zambiri. Iwo akuti ukulosa za zinthu zimene zidzachitika ku tsogolo kwambiri.’
28 Isu nga ibagam kadakuada, 'Kastoy ti kuna ni Yahweh nga Apo: Saanen a maitantan dagiti sasaok, ngem ti sao a naibagakon ket maaramidto—kastoy ti pakaammo ni Yahweh nga Apo!'”
“Choncho uwawuze kuti, ‘zimene Ine Ambuye Yehova ndikunena ndi izi: Zonena zanga sizidzachedwanso; chilichonse chimene ndikunena chidzachitikadi. Ndikutero Ine Yehova.’”

< Ezekiel 12 >