< 2 Tesalonica 3 >

1 Ket ita, kakabsat, ikararagandakami, tapno napardas iti pannaka-iwaragawag iti sao iti Apo ken maitan-ok, a kas met maaramid kadakayo.
Potsiriza, abale, mutipempherere kuti uthenga wa Ambuye ufalikire msanga ndi kulemekezedwa monga momwe munachitira inu.
2 Ikararagyo a maiyadayokami manipud kadagiti nadangkes ken dakes a tattao, gapu ta saan nga amin ket addaan ti pammati.
Ndipo pempherani kuti tilanditsidwe mʼmanja mwa anthu ovuta ndi oyipa, pakuti si onse amene ali nacho chikhulupiriro.
3 Ngem napudno ti Apo, a mangpatibker ken mangaywan kadakayo manipud iti dakes.
Koma Ambuye ndi wokhulupirika, ndipo adzakulimbikitsani ndi kukutetezani kwa woyipayo.
4 Adda panagtalekmi iti Apo maipapan kadakayo, nga itultuloyyo nga aramiden dagiti banbanag nga ibilinmi.
Tili ndi chikhulupiriro mwa Ambuye kuti mukuchita zonse ndipo mudzapitirira kuchita zimene tinakulamulirani.
5 Iturong koma iti Apo dagiti puspusoyo iti ayat iti Dios ken iti kinaibtur ni Cristo.
Ambuye atsogolere mitima yanu kuti mudziwe chikondi cha Mulungu ndiponso kupirira kumene Khristu amapereka.
6 Ita bilinendakayo, kakabsat, iti nagan ni Jesu-Cristo nga Apotayo, a liklikanyo iti tunggal kabsat nga agbibiag iti kinasadut ken saan a segun kadagiti kaugalian a naawatyo kadakami.
Abale, tikukulamulani mʼdzina la Ambuye Yesu Khristu, kuti mupewe mʼbale aliyense amene ndi waulesi ndi wachisokonezo, wosafuna kutsata zimene tinakuphunzitsani.
7 Ta ammoyo mismo nga umno para kadakayo a tuladendakami. Saankami a nakipagbiag kadakayo a kas kadagiti awanan iti disiplina.
Pakuti inu mukudziwa zimene muyenera kuchita pofuna kutitsatira. Ife sitinali alesi pamene tinali nanu
8 Ken saankami a nangan iti taraon iti siasinoman a saanmi a binayadan daytoy. Ngem ketdi, nagtrabaho ken nagbannogkami iti rabii ken aldaw iti narigat a panagtrabaho, tapno saankami nga agbalin a padagsen iti siasinoman kadakayo.
ndipo sitinadye chakudya cha aliyense osalipira. Komatu tinkagwira ntchito mwamphamvu usiku ndi usana kuti tisakhale cholemetsa kwa aliyense.
9 Inaramidmi daytoy a saan a gapu ta awan iti turaymi. Ngem ketdi, inaramidmi daytoy tapno agbalinkami a pagulidanan kadakayo, tapno tuladendakami koma.
Sitinachite zimenezi chifukwa choti tinalibe mphamvu zolamula kuti mutithandize koma kuti tikhale chitsanzo choti mutsatire.
10 Idi addakami kadakayo, imbilinmi kadakayo, “No adda iti saan a mangayat nga agtrabaho, rumbeng a saan a mangan.”
Pakuti ngakhale pamene tinali nanu, tinakupatsani lamulo lakuti, “Munthu wosafuna kugwira ntchito, asadye.”
11 Ta nangngegmi nga adda kadakayo ti agbibiag iti kinasadut. Saanda nga agtrabaho ngem ketdi mannakibiangda.
Ife tikumva kuti pakati panu pali ena amene ndi alesi. Iwo safuna kugwira ntchito, koma amangolowerera pa za eni.
12 Ita, dagiti bilinenmi ken bagbagaanmi iti nagan ni Apo Jesu-Cristo, a rumbeng nga agtrabahoda iti kinatalna ken kanenda iti bukodda a taraon.
Mʼdzina la Ambuye Yesu Khristu, tikuwalamula ndi kuwakakamiza kuti azigwira ntchito mwabata ndi kumadya chakudya chodzigwirira ntchito okha.
13 Ngem dakayo, kakabsat, saankayo a maupay iti panagar-aramid iti umno.
Koma inu abale, musatope nʼkuchita zabwino.
14 No addaman iti saan nga agtulnog iti saomi iti daytoy a surat, tandaananyo isuna ken saankayo a makikadua kenkuana, tapno mabainan isuna.
Ngati wina aliyense akana kumvera malangizo athu a mʼkalatayi, mumuonetsetse ameneyo ndipo musayanjane naye kuti achite manyazi.
15 Saanyo nga ibilang isuna a kas maysa a kabusor ngem ballaaganyo isuna a kas maysa a kabsat.
Komatu musamutenge kukhala mdani, koma muchenjezeni ngati mʼbale.
16 Ited koma ti Apo ti kapia kadakayo iti talna iti amin a tiempo iti amin a wagas. Adda koma kadakayo amin iti Apo.
Tsopano Ambuye mwini mtendere akupatseni mtendere nthawi zonse mwa njira iliyonse. Ambuye akhale ndi inu nonse.
17 Siak ni Pablo, daytoy iti kablaawko iti bukodko nga ima, nga isu iti pagilasinan iti tunggal isuratko. Daytoy ti isuratko
Ine Paulo, ndikulemba malonje awa ndi dzanja langa, chimene ndi chizindikiro chodziwika mʼmakalata anga onse. Umo ndi mmene ndimalembera.
18 Adda koma kadakayo ti parabur ni Jesu- Cristo nga Apotayo.
Chisomo cha Ambuye athu Yesu Khristu chikhale ndi inu nonse.

< 2 Tesalonica 3 >