< II Samuel 12 >

1 Kalpasanna, imbaon ni Yahweh ni Natan a mapan kenni David. Napan isuna kenkuana ket kinunana, “Adda iti dua a lallaki iti maysa a siudad. Ti maysa a lalaki ket nabaknang ken nakurapay ti maysa.
Tsono Yehova anatumiza Natani kwa Davide. Atafika kwa Davide anati, “Panali anthu awiri mʼmizinda ina, wina wolemera ndi wina wosauka.
2 Ti nabaknang ket addaan iti adu a bilang ti arbanna ken tarakenna,
Munthu wolemerayo anali ndi nkhosa ndi ngʼombe zambiri,
3 ngem ti nakurapay ket awanan malaksid iti maysa nga urbon a kabaian a karnero a ginatangna, pinakanna ken pinadakkelna. Dimmakkel daytoy a kaduana ken dagiti annakna. Makipangan pay ti urbon a karnero kenkuana ken makiinom iti bukodna a baso, maturog kadagiti takkiagna ken daytoy ket kasla iti maysa nga putot a babae kenkuana.
koma wosaukayo analibe chilichonse kupatula kankhosa kamodzi kakakazi kamene anakagula. Iye anakasunga ndipo kanakula naye pamodzi ndi ana ake. Kamadya chakudya chake, kamamwera chikho chake ndipo kamagona mʼmanja mwake. Kanali ngati mwana wamkazi kwa iyeyo.
4 Maysa nga aldaw, adda maysa a sangaili ti napan iti nabaknang ngem saan a kayat ti nabaknang a lalaki ti mangala iti ayup manipud iti bukodna nga arban ken taraken tapno itedna a taraon para iti sangalina. Ngem ketdi, innalana ti urbon a kabaian a karnero ti nakurapay sana linuto maipaay iti sangailina.”
“Ndipo mlendo anafika kwa munthu wolemera uja, koma munthu wolemerayo sanafune kutenga imodzi mwa nkhosa kapena ngʼombe zake kuti akonzere chakudya mlendo amene anafika kwa iye. Mʼmalo mwake anatenga mwana wankhosa wamkazi wa munthu wosauka uja nakonzera chakudya mlendo uja amene anabwera kwa iye.”
5 Simged ti unget ni David maibusor iti nabaknang ket nakaluksaw isuna kenni Natan, “Iti nagan ni Yahweh nga adda iti agnanayon, maikari a mapapatay ti lalaki a nangaramid iti daytoy.
Davide anapsa mtima kwambiri chifukwa cha munthuyo ndipo anati kwa Natani, “Pali Yehova, munthu amene anachita zimenezi ayenera kufa basi!
6 Nasken a bayadanna ti urbon a karnero iti maminpat a daras gapu iti kasta nga inaramidna, ken gapu ta awan ti asina iti nakurapay.”
Iye ayenera kulipira mwana wankhosa wamkaziyo kanayi, chifukwa anachita chinthu chimenechi ndipo analibe chifundo.”
7 Kinuna ni Natan kenni David, “Sika dayta a lalaki! Kinuna ni Yahweh a Dios ti Israel, 'Pinulotanka nga ari iti entero nga Israel, ken inispalka manipud iti ima ni Saul.
Kenaka Natani anati kwa Davide, “Munthuyo ndinu! Yehova, Mulungu wa Israeli akuti, ‘Ine ndinakudzoza kukhala mfumu ya Israeli, ndipo ndinakupulumutsa mʼdzanja la Sauli.
8 Intedko kenka ti balay ti amom, ken dagiti assawana kadagiti takkiagmo. Intedko pay ti balay ti Israel ken Juda. Ket no bassit unay dayta, itedko pay kenka dagiti adu a banbanag a nayonna.
Ndinakupatsanso banja la mbuye wako ndiponso akazi a mbuye wako mʼmanja mwako. Ine ndinakupatsanso banja la Israeli ndi Yuda. Ndipo ngati zinthu zonse izi zinali zochepa, Ine ndikanakupatsa zambiri.
9 Apay ngarud a sinalungasingmo dagiti bilbilin ni Yahweh tapno naaramidmo ti dakes iti imatangna? Pinapataymo ni Urias a Heteo babaen iti kampilan ken innalam ti asawana tapno agbalin nga asawam. Pinapataymo isuna babaen ti kampilan ti armada ti Ammon.
Nʼchifukwa chiyani unanyoza mawu a Yehova pochita chimene chili choyipa pamaso pake? Iwe unakantha Uriya Mhiti ndi lupanga ndipo unatenga mkazi wake kukhala wako. Uriyayo unamupha ndi lupanga la Aamoni.
10 Isu nga ita, saanen a pumanaw ti kampilan iti balaymo, gapu ta sinalungasingnak ken innalam a kas asawa ti asawa ni Urias a Heteo.'
Ndipo tsopano lupanga silidzachoka pa nyumba yako, chifukwa unandinyoza ine ndi kutenga mkazi wa Uriya Mhiti kukhala wako.’
11 Kinuna ni Yahweh, 'Kitaem, mangpataudak iti didigra a maibusor kenka manipud iti bukodmo a balay. Iti mismo a sangoanam, alaek dagiti assawam ket itedko ida iti kaarubam, kaiddaennanto dagiti assawam iti tengnga ti aldaw.
“Yehova akuti, ‘Ine ndidzabweretsa tsoka pa iwe lochokera mʼbanja lako. Ndidzatenga akazi ako iwe ukuona ndi kuwapereka kwa wina amene ali pafupi nawe, ndipo iye adzagona ndi akazi ako masanasana Aisraeli onse akuona.
12 Gapu ta nagbasolka a sililimed, ngem aramidek daytoy a banag iti imatang ti entero nga Israel, iti lawag ti init.'”
Iwe unachita zimenezi mwamseri koma Ine ndidzachita izi masanasana Aisraeli onse akuona.’”
13 Kalpasanna, kinuna ni David kenni Natan, “Nagbasolak kenni Yahweh.” Simmungbat ni Natan kenni David, “Pinalabasen ni Yahweh ti basolmo. Saanka ngarud a mapapatay.
Kenaka Davide anati kwa Natani, “Ine ndachimwira Yehova.” Natani anayankha kuti, “Yehova wachotsa tchimo lanu. Simufa ayi.
14 Nupay kasta, gapu iti daytoy nga aramidmo sinalungasingmo ni Yahweh, awan duadua a matay ti ubing a maipasngay nga anakmo.”
Komabe, popeza pochita zimenezi mwachititsa kuti adani a Yehova amunyoze, mwana amene akubalireniyo adzafa.”
15 Kalpasanna, pimmanaw ni Natan ket nagawid. Dinusa ni Yahweh ti anak ti asawa ni Urias nga inyanakna para kenni David, ket nagsakit isuna iti nakaro.
Natani atapita kwawo, Yehova anakantha mwana amene mkazi wa Uriya anabereka ndipo anayamba kudwala.
16 Nagpakaasi ngarud ni David iti Dios agpaay iti ubing. Nagayunar isuna, simrek iti uneg ket nagpatnag a nagidda iti suelo.
Davide anapempherera mwanayo kwa Mulungu. Iye anasala chakudya ndipo analowa mʼnyumba mwake nagona pansi usiku wonse.
17 Timmakder dagiti panglakayen iti balayna ket timmakderda iti abayna a mangibangon kenkuana ngem saan isuna a bimmangon, ken saan a nakipangan kadakuada.
Akuluakulu a banja lake anayima pambali pake kuti amudzutse, koma iye anakana, ndipo sanadye chakudya chilichonse pamodzi ndi iwo.
18 Ket dimteng iti maikapito nga aldaw, natay ti ubing. Mabuteng dagiti adipen ni David a mangibaga a natayen ti ubing, ta kinunada, “Kitaenyo, idi sibibiag pay ti ubing kinatungtungtayo isuna, ket saanna nga impangag ti timektayo. Ania ngata ti aramidenna iti bagina no ibagatayo kenkuana a natayen ti ubing?!”
Mwana anamwalira pa tsiku lachisanu ndi chiwiri. Antchito a Davide anaopa kumuwuza kuti mwanayo wamwalira, popeza ankaganiza kuti, “Pamene mwanayu anali ndi moyo, ife tinayankhula Davide koma sanatimvere. Nanga tingamuwuze bwanji kuti mwana wamwalira? Mwina atha kudzipweteka.”
19 Ngem idi nakita ni David nga agiinnarasaas dagiti adipenna, naamiris ni David a natayen ti ubing. Kinunana kadagiti adipenna, “Natay kadin ti ubing?” Insungbatda, “Wen apo, natayen isuna.”
Davide anaona kuti antchito ake amanongʼonezana pakati pawo ndipo anazindikira kuti mwanayo wamwalira. Iye anafunsa kuti, “Kodi mwanayo wamwalira?” Iwo anayankha kuti, “Inde wamwalira.”
20 Timmakder ngarud ni David manipud iti datar sa nagdigos, sinapsappoanna ti lana ti bagina, ket nagsukat iti badona. Napan isuna iti tabernakulo ni Yahweh ket nagdayaw sadiay, sa nagsubli iti bukodna a palasio. Idi nagdawat isuna iti makan, nagidasarda para kenkuana, ket nangan isuna.
Ndipo Davide anayimirira. Anakasamba nadzola mafuta ndi kusintha zovala zake. Pambuyo pake anapita ku nyumba ya Yehova kukapembedza. Kenaka anapita ku nyumba kwake ndipo atapempha chakudya anamupatsa nadya.
21 Ket kinuna dagiti adipenna kenkuana, “Apo, apay a kastoy ti inaramidmo? Nagayunar ken nagdung-awka para iti ubing idi sibibiag pay isuna, ngem idi natayen ti ubing, bimmangonka ket nanganka.”
Antchito ake anamufunsa kuti, “Chifukwa chiyani mukuchita zinthu motere? Pamene mwana anali ndi moyo, munkasala chakudya ndi kulira, koma tsopano pamene mwana wamwalira inu mukudzuka ndi kudya!”
22 Simmungbat ni David, “Idi sibibiag pay iti ubing, nagayunar ken nagdung-awak. Kinunak, 'Siasino ti makaammo no paraburannak ni Yahweh wenno saan, tapno agbiag ti ubing?'
Iye anayankha kuti, “Pamene mwana anali ndi moyo ine ndinkasala zakudya ndi kulira. Ine ndinkaganiza kuti, ‘Akudziwa ndani? Yehova atha kundikomera mtima kuti mwanayo akhale ndi moyo.’
23 Ngem ita, natayen isuna isu nga apay pay nga agayunarak? Maisublik pay kadi isuna? Mapanakto kenkuana ngem saanen isuna nga agsubli kaniak.”
Koma tsopano wamwalira ndisaliranji chakudya? Kodi ndingathe kumubwezanso? Ine ndidzapita kumene kuli iyeko, koma iye sadzabwerera kwa ine.”
24 Liniwliwa ni David ni Batseba nga asawana, napan kenkuana, ket nakikaidda isuna kenkuana. Isu a naganak ni Batseba iti maysa a lalaki, ket pinanagananna ti ubing iti Solomon. Inay-ayat ni Yahweh ti ubing,
Ndipo Davide anatonthoza mkazi wake Batiseba, napita kwa iye ndi kugona naye. Iye anabereka mwana wamwamuna, ndipo anamutcha dzina lake Solomoni. Yehova ankamukonda iye.
25 isu a nangipatulod isuna iti sao babaen kenni Natan a propeta tapno panagananna isuna ti Jedidia, gapu ta inay-ayat ni Yahweh ti ubing.
Ndipo chifukwa chakuti Yehova ankamukonda iyeyo, Yehovayo anatumiza mawu kwa mneneri Natani kuti akamutchule Yedidiya.
26 Ita, ginubat ni Joab ti Rabba, ti kangrunaan a siudad dagiti tattao ti Ammon, ket nasakupna dagiti sarikedkedna.
Pa nthawi imeneyi Yowabu anamenyana ndi Raba ku Amoni ndipo analanda nsanja yaufumu.
27 Isu a nangibaon ni Joab kadagiti mensahero kenni David ket kinunana, “Ginubatko ti Rabba ket naalak ti pagtataudan ti danum ti siudad.
Ndipo Yowabu anatumiza amithenga kwa Davide kukanena kuti, “Ine ndamenyana ndi Raba ndipo ndatenga zitsime zake za madzi.
28 Isu nga ita, ummongem dagiti nabatbati iti armada, pagkampoem maibusor iti siudad ket alaem daytoy gapu ta no maalak ti siudad, maipanaganto daytoy kaniak.”
Ndipo tsopano sonkhanitsani asilikali onse ndipo muzungulire mzindawo ndi kuwulanda.”
29 Isu nga inummong ni David amin nga armada ket napanda idiay Rabba; nakigubat isuna maibusor iti siudad ket nasakupna daytoy.
Kotero Davide anasonkhanitsa ankhondo onse ndipo anapita ku Raba kukawuthira nkhondo ndi kuwulanda.
30 Innala ni David ti korona ni Molec manipud iti ulona-maysa a talento a balitok ti dagsenna, ken adda napateg a bato iti daytoy. Naiparabaw ti korona iti ulo ni David. Kalpasanna, innalana nga inruar iti siudad ti dakkel a kantidad ti nasamsamda.
Davide anachotsa chipewa chaufumu pamutu pa mfumu yawo ndipo Davide anavala chipewacho. Chipewacho chinkalemera makilogalamu asanu agolide, ndiponso chinali ndi miyala yokongola. Iye anatenga katundu wambiri kuchokera mu mzindawo,
31 Pinaruarna dagiti tattao iti siudad ken pinilitna ida nga agragadi, aggabyon, ken agbalsig; pinagtrabadona pay ida iti pagaramidan ti ladrilio. Pinilit ni David dagiti amin a siudad dagiti tattao a taga-Amnon a trabahoen daytoy. Kalpasanna, nagsubli ni David ken ti amin nga armada iti Jerusalem.
ndipo anatulutsa anthu amene anali mʼmenemo, nawayika kuti azigwira ntchito ya macheka, yosula makasu ndi nkhwangwa, ndiponso yowomba njerwa. Davide anachita izi ndi mizinda yonse ya Aamoni. Kenaka iye pamodzi ndi gulu lake lonse lankhondo anabwerera ku Yerusalemu.

< II Samuel 12 >