< 2 Ar-ari 6 >

1 Kinuna dagiti annak dagiti profeta kenni Eliseo, “Ti lugar a pagnanaedantayo ket nailet unay para kadatayo amin.
Ana a aneneri anati kwa Elisa, “Taonani malo amene timakhala ndi inu atichepera kwambiri.
2 Pangngaasim ta palubosannakami a mapan idiay Karayan Jordan, ket palubosam ti tunggal lalaki a mangpukan iti kayo, ket mangbangontayo ti lugar sadiay a mabalin a pagnaedantayo.” Simmungbat ni Eliseo, “Mabalinyon ti mapan.”
Tiloleni tipite ku Yorodani kumene aliyense wa ife akadule mtengo umodzi, kuti timange malo woti tizikhalamo.” Ndipo Elisa anati, “Pitani.”
3 Kinuna ti maysa kadakuada, “Pangngaasim ta kumuyogka kadagiti adipenmo.” Simmungbat ni Eliseo, “Mapanak.”
Mmodzi wa iwo anati, “Chonde mulole kutsagana nawo atumiki anu.” Elisa anayankha kuti, “Ndipita nanu.”
4 Isu a kimmuyog ni Eliseo kadakuada, idi nakadanondan idiay Karayan Jordan, rinugianda ti nagpukan kadagiti kayo.
Ndipo anapita nawo. Anapita ku Yorodani nayamba kudula mitengo.
5 Ngem kabayatan nga agpukpukan ti maysa, natinnag ti ulo ti wasay iti danum; nagpukkaw isuna ket kinunana, “Ayna, apok, daytoy ket bulod!”
Pamene wina ankadula mtengo, nkhwangwa yake inaguluka nigwera mʼmadzi. Iye anafuwula kuti, “Mayo! Mbuye wanga! Popeza ndi yobwereka!”
6 Isu a kinuna ti tao ti Dios, “Sadino ti nakatnaganna?” Intudo ti lalaki kenni Eliseo ti disso a nakatnaganna. Nangputed ngarud ni Eliseo iti ruting, impuruakna daytoy iti danum, ket pinagtapawna ti landok.
Ndipo munthu wa Mulungu uja anafunsa, “Yagwera pati?” Pamene anamuonetsa malowo, Elisa anadula kamtengo nakaponya pamenepo, ndipo nkhwangwayo inayandama.
7 Kinuna ni Eliseo, “Pidutem.” Isu a ginaw-at ti lalaki daytoy.
Elisa anati, “Itenge.” Ndipo munthuyo anatambalitsa dzanja lake nayitenga.
8 Ita, ti ari ti Aram ket mangirugrugi idi iti gubat maibusor iti Israel. Nakiuman isuna kadagiti adipenna, a kunana, “Agkampoakto iti kastoy ken kastoy a lugar.”
Tsono mfumu ya ku Aramu inali pa nkhondo ndi Israeli. Itakambirana ndi atsogoleri ake ankhondo inati, “Ndidzamanga misasa yanga pamalo akutiakuti.”
9 Isu a nangibaon ti tao ti Dios iti ari ti Israel, a kunana, “Agannadkayo a saan a magna iti dayta a lugar, ta sumalsalog sadiay dagiti Arameo.”
Munthu wa Mulungu anatumiza mawu kwa mfumu ya ku Israeli kuti “Musamale podutsa malo akuti, chifukwa Aaramu akupita kumeneko.”
10 Kalpasanna, nangibaon ti ari ti Israel kadagiti lalaki iti lugar nga impakdaar ti tao ti Dios kenkuana. Namin-anon a daras nga insalakan isuna dayta a pakdaar sadiay.
Choncho mfumu ya ku Israeli inatuma anthu kumalo kumene munthu wa Mulunguyo ananena. Nthawi ndi nthawi Elisa ankachenjeza mfumu, kotero kuti ankakhala tcheru ku malo amenewo.
11 Nariribukan unay ti panunot ti ari ti Aram maipapan iti daytoy a pakdaar, ket inayabanna dagiti adipenna ket kinunana kadakuada, “Saanyo kadi nga ibaga kaniak no siasino kadatayo ti umay-ayon iti ari ti Israel?
Zimenezi zinakwiyitsa kwambiri mfumu ya ku Aramu. Mfumuyo inayitanitsa atsogoleri ake ankhondo ndipo inawafunsa kuti, “Kodi simungandiwuze munthu amene pakati pathu pano ali mbali ya mfumu ya ku Israeli?”
12 Kinuna ngarud ti maysa kadagiti adipenna, “Saan, apok nga ari, ta ni Eliseo a profeta iti Israel ti mangibagbaga iti ari ti Israel kadagiti sasao nga ibagbagam iti siledmo!”
Mmodzi mwa atsogoleri a ankhondowo anati, “Palibe ndi mmodzi yemwe pakati pathu, inu mbuye wanga, koma Elisa mneneri amene ali ku Israeli amawuza mfumu ya ku Israeli mawu enieni amene inu mumayankhula ku chipinda kwanu.”
13 Simmungbat ti ari, “Inkayo kitaen no sadino ti ayan ni Eliseo tapno makaibaonak kadagiti lallaki a mangtiliw kenkuana.” Naibaga kenkuana, “Kitaem, adda isuna idiay Dotan.”
Choncho mfumu inalamula kuti, “Pitani, kafufuzeni kumene akukhala kuti ine nditume anthu kukamugwira.” Anthuwo anabweretsa mawu oti, “Taonani, Elisa ali ku Dotani.”
14 Isu a nangipatulod ti ari idiay Dotan kadagiti kabalio, karwahe ken nangibaon iti dakkel a bunggoy dagiti armada. Dimtengda sadiay iti rabii ket pinalikmutanda ti siudad.
Ndipo mfumu inatumizako magaleta ndi akavalo ndiponso gulu lankhondo lamphamvu. Anapita usiku nakawuzungulira mzindawo.
15 Idi nakariing a nasapa ket rimmuar ti adipen ti tao ti Dios, adda met sadiay iti dakkel nga armada agraman dagiti kabalio ken karwahe a nakapalikmot iti siudad. Ket kinuna ti adipen kenni Eliseo, “O, apok! Ania ti aramidentayo?”
Mtumiki wa munthu wa Mulungu atadzuka mmamawa ndi kutuluka panja, gulu la ankhondo pamodzi ndi akavalo ndi magaleta anali atazungulira mzindawo. Mtumikiyo anafunsa kuti, “Kalanga mbuye wanga, tidzachita chiyani?”
16 Simmungbat ni Eliseo, “Saanka nga agbuteng, ta ad-adu dagiti kaduatayo ngem dagidiay a kakaduada.”
Mneneri anamuyankha kuti, “Usachite mantha. Amene ali mbali yathu ndi ambiri kupambana amene ali mbali yawo.”
17 Nagkararag ni Eliseo ket kinunana, Yahweh, agpakpakaasiak a lukatam dagiti matana tapno makitana.” Kalpasanna, linuktan ni Yahweh dagiti mata ti adipen, ket nakitana. Adtoy, napno ti bantay kadagiti kabalio ken karwahe nga umap-apuy iti likmot ni Eliseo!
Ndipo Elisa anapemphera kuti, “Inu Yehova tsekulani maso ake kuti aone.” Pamenepo Yehova anatsekula maso a mtumikiyo, ndipo anayangʼana naona kuti phiri lonse linali lodzaza ndi akavalo ndi magaleta a moto atazungulira Elisa.
18 Idi simmalog dagiti Arameo a napan kenkuana, nagkararag ni Eliseo kenni Yahweh a kinunana, “Dawatek kenka a pagbulsekem dagitoy a tattao.” Isu a pinagbulsek ida ni Yahweh, kas dinawat ni Eliseo.
Pamene adaniwo ankabwera kudzalimbana naye, Elisa anapemphera kwa Yehova kuti, “Achititseni khungu anthu awa.” Kotero Yehova anawachititsa khungu monga anapemphera Elisa.
19 Kalpasanna, imbaga ni Eliseo kadagiti Arameo, “Saan a daytoy ti dalan, wenno ti siudad. Surutendak, ket ipankayo iti tao a birbirukenyo.” Ket inturongna ida idiay Samaria.
Elisa anawawuza ankhondowo kuti, “Njira si imeneyi ndipo mzinda sumenewunso. Tsateni, ndipo ndidzakutengerani kwa munthu amene mukumufunayo.” Ndipo anawatengera ku Samariya.
20 Napasamak nga idi nakadanonda idiay Samaria, imbaga ni Eliseo, “Yahweh, luktam dagiti mata dagitoy a tattao tapno makakitada.” Linukatan ni Yahweh dagiti matada ket nakitada, ket adtoy, addada iti tengnga ti siudad ti Samaria.
Atalowa mu mzinda wa Samariya, Elisa anati, “Yehova tsekulani maso a anthu awa kuti aone.” Choncho Yehova anatsekula maso awo ndipo anangoona kuti ali mʼkati mwenimweni mwa Samariya.
21 Kinuna ti ari ti Israel kenni Eliseo, idi nakitana ida, “Amak, rumbeng kadi a papatayek ida? Rumbeng kadi a patayek ida?
Mfumu ya ku Israeli itawaona, inafunsa Elisa kuti, “Abambo anga, kodi ndiwaphe? Kodi ndiwaphe?”
22 Simmungbat ni Eliseo, “Saan a rumbeng a papatayem ida. Papatayem kadi dagiti natiliwmo a balud babaen kadagiti kampilan ken panam. Mangikabilka iti tinapay ken danum iti sangoananda, tapno mangan ken uminumda, ket mapanda iti apoda.”
Elisa anayankha kuti, “Musawaphe. Kodi mungaphe anthu amene munawagwira pogwiritsa ntchito lupanga ndi uta? Apatseni chakudya ndi madzi kuti adye ndi kumwa kenaka apite kwa mbuye wawo.”
23 Isu a nangisagana ti ari iti adu a taraon para kadakuada, ket idi nakapangan ken nakainomdan, pinapanawna ida, ket nagsublida iti apoda. Nabayag a panawen a saanen a nagsubli dagidiay a bunggoy dagiti soldado ti Aram iti daga ti Israel.
Choncho anawakonzera mphwando lalikulu, ndipo atatsiriza kudya ndi kumwa, anawatumiza kwawo ndipo anabwerera kwa mbuye wawo. Kotero magulu a ankhondo a ku Aramu analeka kuthira nkhondo dziko la Israeli.
24 Iti saan a nabayag kalpasan daytoy, inummong ni Ben Hadad nga ari ti Aram iti amin nga armada ti Aram ket rinautda ti Samaria ket linakubda daytoy.
Patapita nthawi, Beni-Hadadi mfumu ya Aramu anasonkhanitsa gulu lake lonse la ankhondo, napita kukazungulira mzinda wa Samariya.
25 Isu nga adda idi ti nakaro a panagbisin idiay Samaria. Adtoy, linakubda daytoy agingga a nailako ti ulo ti asno iti walo pulo a pidaso a pirak, ken ti kakapat a kab ti lugit ti kalapati iti lima a pidaso a pirak.
Mu mzinda wa Samariya munali njala yoopsa. Ndipo taonani, Aaramu anazungulira mzindawu kwa nthawi yayitali kotero kuti mutu wa bulu ankawugulitsa ndalama za siliva 80, ndipo magalamu 200 a zitosi za nkhunda ankawagulitsa pa mtengo wa masekeli asanu.
26 Kabayatan a magmagna ti ari ti Israel iti rabaw ti pader, nagpukkaw kenkuana ti maysa a babai, kinunana, “Tulong, apok nga ari.”
Pamene mfumu inkayenda pa khoma la mzindawo, mayi wina anafuwulira mfumuyo kuti, “Thandizeni mbuye wanga mfumu!”
27 Kinunana, “No saannaka a tulungan ni Yahweh, kasanoka a matulungan? Adda kadi aniaman nga agtataud iti pagirikan wenno pagpespesan ti arak?”
Mfumu inayankha kuti, “Ngati Yehova sakuthandiza iwe, ine thandizo lako ndingalipeze kuti? Kuchokera ku malo opunthira tirigu kodi? Kuchokera kumalo opsinyira mphesa kodi?”
28 Intultuloy ti ari, “Ania ti pakarirriribukam? Simmungbat ti babai, “Kinuna daytoy a babai kaniak, 'Itedmo ti anakmo a lalaki tapno kanenta isuna ita nga aldaw, ket kanenta ti anakko inton bigat.”
Pamenepo mfumuyo inafunsa mayiyo kuti, “Kodi chakuvuta nʼchiyani?” Iye anayankha kuti, “Mayi uyu anandiwuza kuti, ‘Bweretsa mwana wako kuti timudye lero, ndipo mawa tidzadya mwana wangayu.’
29 Inangermi ngarud ti anakko ket kinnanmi isuna, ket imbagak kenkuana iti sumaruno nga aldaw, “Itedmo ti anakmo ta kanenta isuna, ngem inlemmengna ti anakna.”
Choncho tinaphika mwana wanga ndi kumudya. Tsiku lotsatira lakelo ine ndinati, ‘Bweretsa mwana wako kuti timudye,’ koma iye anabisa mwana wakeyo.”
30 Idi nangngeg ti ari dagiti sao ti babai, rinay-abna dagiti kawesna (ita, magmagna ti ari iti rabaw ti pader), ket kimmita dagiti tattao ket nakitada a nakersang a lupot iti pang-uneg a kawesna.
Mfumu itamva mawu a mayiyo, inangʼamba mkanjo wake. Pamene inkayenda pa khoma, anthu anayangʼana, ndipo anaona zovala zamʼkati, pakuti anavala chiguduli.
31 Ket kinunana, “Kastoy koma met ti aramiden ti Dios kaniak, ken ad-adda pay koma, no ti ulo ni Eliseo nga anak ni Safat ket agtalinaed pay kenkuana ita nga aldaw.”
Mfumuyo inati, “Mulungu andilange, andilange kwambiri ndikapanda kudula mutu wa Elisa mwana wa Safati lero!”
32 Ngem agtugtugaw idi ni Eliseo iti uneg ti balayna, ket kaduana nga agtugtugaw dagiti panglakayen. Nangibaon ti ari iti tao manipud iti sangoananna, ngem idi napan ti mensahero kenni Eliseo, kinunana kadagiti panglakayen, “Kitaenyo no kasano a nangibaon daytoy nga anak ti mammapatay iti umay mangputed iti ulok? Kastoy, inton umay ti mensahero, irekepyo ti ridaw, ket saanyo nga ilukatan isuna. Saan kadi a ti uni dagiti saka ti amona iti sumarsaruno kenkuana?”
Tsono Elisa nʼkuti atakhala mʼnyumba mwake, ndipo akuluakulu anali naye limodzi. Mfumu inatuma munthu wina kuti imutsogolere, koma asanafike, Elisa anawuza akuluakuluwo kuti, “Kodi simukuona momwe wopha munthu uja watumizira munthu wina kuti adzadule mutu wanga? Taonani mthengayo akafika, mutseke chitseko ndipo muchigwiritsitse kuti asalowe. Kodi ndikumvawo pambuyo pake si mgugu wa mbuye wake?”
33 Kabayatan a makisarsarita pay laeng ni Eliseo kadakuada, adtoy, ti mensahero ket napan kenkuana. Kinuna ti ari, “Adtoy, daytoy a rigat ket naggapu kenni Yahweh. Apay koma nga agurayak pay laeng kenni Yahweh?”
Elisa akuyankhulabe ndi anthuwo, taonani, wamthengayo anafika kwa iye. Ndipo mfumu inati, “Mavuto amenewa ndi ochokera kwa Yehova. Kodi nʼchifukwa chiyani ine ndiyenera kudikira thandizo lochokera kwa Yehova?”

< 2 Ar-ari 6 >