< 2 Cronicas 22 >

1 Insaad dagiti agnanaed iti Jerusalem ni Ahazias a kaubingan a putot a lalaki ni Jehoram nga ari a kas kasukatna; ta dagiti lallaki nga immay a rimmaut iti kampo agraman dagiti taga-Arab a kakaduada ket pinapatayda dagiti amin nga inauna a putotna a lallaki. Isu a ni Ahazias a putot ni Jehoram nga ari ti Juda ti naisaad a kas ari.
Anthu a mu Yerusalemu anayika Ahaziya mwana wamngʼono kwambiri wa Yehoramu kukhala mfumu mʼmalo mwake, popeza gulu lankhondo limene linabwera ndi Aarabu ku misasa, linapha ana onse aakulu. Motero Ahaziya mwana wa Yehoramu mfumu ya Yuda anayamba kulamulira.
2 Uppat a pulo ket dua ti tawen ni Ahazias idi nangrugi isuna nga agturay; nagturay isuna idiay Jerusalem iti maysa a tawen. Atalia ti nagan ti inana a putot a babai ni Omri.
Ahaziya anali wa zaka 22 pamene anakhala mfumu ndipo analamulira mu Yerusalemu chaka chimodzi. Dzina la amayi ake linali Ataliya, chidzukulu cha Omuri.
3 Sinurotna met dagiti wagas ti balay ni Ahab ta ti inana ti mammagbaga kenkuana nga agaramid kadagiti dakes a banbanag.
Nayenso anayenda mʼnjira ya banja la Ahabu, pakuti amayi ake anamulimbikitsa kuchita zolakwika.
4 Inaramid ni Ahazias ti dakes iti imatang ni Yahweh, a kas iti ar-aramiden ti balay ni Ahab, ta kalpasan ti ipapatay ti amana ket isuda dagiti mammagbaga kenkuana nga isu ti nakaigapuan ti pannakadadaelna.
Iye anachita zoyipa pamaso pa Yehova monga momwe banja la Ahabu linachitira, pakuti atamwalira abambo ake, iwo anakhala alangizi ake, kumene kunali kudziwononga kwake.
5 Sinurotna met dagiti balakadda; nakikadua kenni Joram a putot a lalaki ni Ahab nga ari ti Israel tapno makiranget kenni Hazael nga ari ti Aram idiay Ramot Galaad. Sinugatan dagiti taga-Aram ni Joram.
Iyeyo anatsatiranso uphungu wawo pamene anapita ndi Yehoramu, mwana wa Ahabu, mfumu ya Israeli kukachita nkhondo ndi Hazaeli mfumu ya Aramu ku Ramoti Giliyadi. Aaramu anavulaza Yehoramu,
6 Nagsubli ni Joram idiay Jezreel tapno agpaimbag kadagiti sugatna, idi nakiranget isuna kenni Hazael nga ari ti Aram idiay Rama. Isu a simmalog ni Ahazias a putot a lalaki ni Jehoram, nga ari ti Juda idiay Jezreel tapno sarungkaranna ni Joram a putot a lalaki ni Ahab, gapu ta nasugatan ni Joram.
kotero iye anabwerera ku Yezireeli kuti akachire mabala amene anamuvulaza ku Ramoti pa nkhondo ndi Hazaeli mfumu ya Aaramu. Ndipo Ahaziya, mwana wa Yehoramu mfumu ya Yuda anapita ku Yezireeli kukaona Yehoramu mwana wa Ahabu chifukwa anavulazidwa.
7 Ita, ti pannakadadael ni Ahazias ket inyeg ti Dios babaen iti panangsarungkar ni Ahazias kenni Joram. Idi nakasangpet isuna, nakikadua kenni Joram a mangdarup kenni Jehu a putot a lalaki ni Nimsi a pinili ni Yahweh a mangdadael iti balay ni Ahab.
Mulungu anakonza kuti Ahaziya akaphedwe pa ulendo wake wokacheza. Ahaziya atafika, iye ndi Yoramu anapita kukakumana ndi Yehu mwana wa Nimisi, amene Yehova anamudzoza kuti akawononge banja la Ahabu.
8 Napasamak nga, idi ipatpatungpal ni Jehu ti panangpapatayna kadagiti amin a kaputotan ni Ahab a kas iti imbilin ti Dios, nasarakanna dagiti mangidadaulo iti Juda ken dagiti putot a lallaki ti kabsat a lalaki ni Ahazias nga agserserbi kenni Ahazias. Pinapatay ida ni Jehu.
Pamene Yehu ankalanga banja la Ahabu anapeza atsogoleri a ku Yuda ndiponso ana aamuna a abale ake a Ahaziya amene amatumikira Ahaziya, ndipo anawapha.
9 Binirok ni Jehu ni Ahazias, natiliwda isuna nga aglemlemmeng idiay Samaria, impanda isuna kenni Jehu, ket pinapatayda isuna. Ket intabonda isuna, ta kunada, “Putot isuna a lalaki ni Jehosafat, a nangipamaysa iti pusona kenni Yahweh.” Isu nga awanen iti pannakabalin ti balay ni Ahazias a mangituray iti pagarian.
Kenaka anapita kukafunafuna Ahaziya, ndipo anthu ake anagwira Ahaziya pamene amabisala mu Samariya. Anabwera naye kwa Yehu ndipo anaphedwa. Iwo anamuyika mʼmanda, pakuti anati, “Iyeyu anali mwana wa Yehosafati amene anafunafuna Yehova ndi mtima wake wonse.” Kotero panalibe wamphamvu mʼbanja la Ahaziya kuti nʼkukhala mfumu.
10 Ita, idi nakita ni Atalia nga ina ni Ahazias a natayen ti anakna, timmakder isuna ket pinatayna dagiti amin nga annak ti ari iti balay ti Juda.
Ataliya, amayi ake a Ahaziya, ataona kuti mwana wawo wafa, ananyamuka nakapha onse a banja laufumu la Yuda.
11 Ngem innala ni Jehosaba, a putot a babai ti ari, ni Joas, a putot a lalaki ni Ahazias, ket inyadayona isuna kadagiti annak ti ari a dandani mapapatay. Inkabilna isuna iti maysa a siled agraman ti mangay-aywan kenkuana. Isu nga inlemmeng isuna ni Jehoseba a putot a babai ni Ari Jehoram, nga asawa ni Jehoyada a padi (ta kabsat isuna a babai ni Ahazias) tapno saan a papatayen ni Atalia.
Koma Yehoseba, mwana wamkazi wa mfumu Yehoramu, anatenga Yowasi mwana wa Ahaziya, momuba ndi kumuchotsa pakati pa ana aamuna a mfumu amene amati aphedwe ndipo anamuyika iye ndi mlezi wake mʼchipinda chogona. Motero Yehoseba, mwana wamkazi wa mfumu Yehoramu, mkazi wa wansembe Yehoyada, yemwe anali mlongo wake wa Ahaziya anamubisa mwanayo kuti Ataliya asamuphe.
12 Kaduada isuna nga aglemlemmeng iti balay ti Dios iti innem a tawen, bayat iti panagturay ni Atalia iti daga.
Mwanayo anakhala mobisala pamodzi ndi iwo mu Nyumba ya Mulungu kwa zaka zisanu ndi chimodzi muulamuliro wa Ataliya.

< 2 Cronicas 22 >