< 1 Timoteo 2 >

1 Ngarud umuna iti amin, dawatek a dagiti kiddaw, dagiti kararag, dagiti pannangibabaet ken dagiti panagyaman ket maaramid koma para iti amin a tao,
Tsono choyamba ndikukupemphani kuti mupempherere anthu onse. Mapemphero anu akhale opemba, opempha, opempherera ena ndi oyamika.
2 para kadagiti ari ken kadagiti amin nga adda iti turay, tapno agbiagtayo koma a natalna ken naulimek iti amin a kinanadiosan ken kinatakneng.
Mupempherere mafumu ndi onse aulamuliro, kuti tikhale moyo wamtendere ndi bata, woopa Mulungu ndi oyera mtima.
3 Nasayaat ken makaay-ayo daytoy iti sangoanan ti Dios a mangisalakantayo.
Izi ndi zabwino ndipo zimakondweretsa Mulungu Mpulumutsi wathu,
4 Tarigagayna a ti amin a tao ket maisalakan ken maammoanda ti kinapudno.
amene amafuna kuti anthu onse apulumutsidwe ndipo kuti adziwe choonadi.
5 Ta adda maymaysa a Dios, ken adda maymaysa a mangibabaet para iti Dios ken ti tao, isu ti tao a ni Cristo Jesus.
Pakuti pali Mulungu mmodzi yekha ndi Mʼkhalapakati mmodzi yekha pakati pa Mulungu ndi anthu, munthu uja Khristu Yesu.
6 Intedna ti bagina kas subbot para kadagiti amin, a kas ti pammaneknek iti umno a tiempo.
Iyeyu anadzipereka kukhala dipo lowombolera anthu onse. Umenewu ndi umboni umene waperekedwa mu nthawi yake yoyenera.
7 Gapu iti daytoy a panggep, siak a mismo, ket nagbalin a mangaskasaba ken apostol. Ibagbagak ti kinapudno. Saanak nga agul-ulbod. Maysa-ak a manursuro kadagiti Hentil iti pammati ken kinapudno.
Nʼchifukwa chake anandisankha kukhala mlaliki ndiponso mtumwi wophunzitsa anthu a mitundu ina mawu achikhulupiriro choona. Sindikunama ayi, ndikunena zoona.
8 Ngarud, kayatko a dagiti lallaki iti tunggal disso ket agkararag ken agingato koma kadagiti nasantoan nga ima nga awanan panagpungtot ken panagdua-dua.
Choncho ndikufuna kuti paliponse popemphera, amuna azikweza manja awo kwa Mulungu mopanda mkwiyo kapena kukangana.
9 Kasta met, kayatko a dagiti babbai ket kawesanda dagiti bagbagida iti umno a kawes, nga addaan kinaemma ken panagteppel. Nasken a saan a nasallapid ti buokda, wenno maaddaan iti balitok, wenno dagiti perlas, wenno nangina a kawes.
Ndikufunanso kuti amayi azivala mwaulemu, modzilemekeza ndi moyenera. Adzikongoletse koma osati ndi tsitsi loluka mowonjeza muyeso kapena zokongoletsa zagolide kapena mikanda yamtengowapatali kapena ndi zovala zamtengowapatali.
10 Kayatko nga agkawesda iti maiyannatup kadagiti babbai a mangipakpakita iti kinanadiosan babaen iti nasayaat nga aramid.
Koma adzikongoletse ndi ntchito zabwino zoyenera mayi wopembedza Mulungu.
11 Ti babai ket masapul nga agsursuro a naulimek ken iti amin a panagtulnog.
Amayi azikhala chete pophunzitsidwa ndi mtima ogonjera kwathunthu.
12 Saanko a palubosan a mangisuro ti babai wenno iturayanna ti lalaki, ngem ketdi agbiag iti kinaulimek.
Ine sindikulola kuti amayi aziphunzitsa kapena kulamulira amuna; koma akhale chete.
13 Ta immun-una a naparsua ni Adan, kalpasan ket ni Eva.
Pakuti Adamu ndiye anayamba kupangidwa kenaka Hava.
14 Ken saan a naallilaw ni Adan, ngem ti babai ket naan-anay a naallilaw iti panagbasol.
Ndipo Adamu si amene ananyengedwa koma mkazi ndiye amene ananyengedwa nachimwa.
15 Nupay kasta, maisalakanto isuna babaen iti panangipasngayna kadagiti annak, no agtultuloyda iti pammati, iti ayat ken iti pannakadalus nga addaan iti nanakman a panagpanpanunot.
Ndipo mkazi adzapulumutsidwa pobereka mwana ngati apitiriza kukhala mʼchikhulupiriro, mʼchikondi ndi mʼkuyera mtima pamodzi ndi kudzichepetsa konse.

< 1 Timoteo 2 >