< Zsoltárok 8 >
1 Az éneklőmesternek a gittithre; Dávid zsoltára. Mi Urunk Istenünk, mily felséges a te neved az egész földön, a ki az egekre helyezted dicsőségedet.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa gititi. Salimo la Davide. Inu Yehova Ambuye athu, dzina lanu ndi la lamphamvudi pa dziko lonse lapansi! Inu mwakhazikitsa ulemerero wanu mʼmayiko onse akumwamba.
2 A csecsemők és csecsszopók szájával erősítetted meg hatalmadat a te ellenségeid miatt, hogy a gyűlölködőt és bosszúállót elnémítsd.
Kuchokera mʼkamwa mwa ana ndi makanda, Inu mwakhazikitsa mphamvu chifukwa cha adani anu, kukhazikitsa bata adani ndi anthu obwezera zoyipa.
3 Mikor látom egeidet, a te újjaidnak munkáját; a holdat és a csillagokat, a melyeket teremtettél:
Pamene ndilingalira za mayiko anu akumwamba, ntchito ya zala zanu, mwezi ndi nyenyezi, zimene mwaziyika pa malo ake,
4 Micsoda az ember – mondom – hogy megemlékezel róla? és az embernek fia, hogy gondod van reá?
munthu ndani kuti Inu mumamukumbukira, ndi mwana wa munthu kuti inu mumacheza naye?
5 Hiszen kevéssel tetted őt kisebbé az Istennél, és dicsőséggel és tisztességgel megkoronáztad őt!
Inu munamupanga kukhala wocheperapo kusiyana ndi zolengedwa zakumwamba ndipo mwamuveka ulemerero ndi ulemu.
6 Úrrá tetted őt kezeid munkáin, mindent lábai alá vetettél;
Inu munamuyika wolamulira ntchito ya manja anu; munayika zinthu zonse pansi pa mapazi ake;
7 Juhokat és mindenféle barmot, és még a mezőnek vadait is;
nkhosa, mbuzi ndi ngʼombe pamodzi ndi nyama zakuthengo,
8 Az ég madarait és a tenger halait, mindent, a mi a tenger ösvényein jár.
mbalame zamlengalenga ndi nsomba zamʼnyanja zonse zimene zimayenda pansi pa nyanja.
9 Mi Urunk Istenünk, mily felséges a te neved az egész földön!
Inu Yehova, Ambuye athu, dzina lanu ndi lamphamvudi pa dziko lonse lapansi!