< Hóseás 14 >

1 Térj meg Izraél, az Örökkévalóhoz, a te Istenedhez – mert elbotlottál bűnöd által.
Iwe Israeli bwerera kwa Yehova Mulungu wako. Machimo anu ndi amene akugwetsani!
2 Vigyetek magatokkal szavakat és térjetek meg az Örökkévalóhoz; szóljatok hozzá: egészen bocsásd meg a bűnt és fogadd el a jót: – hadd fizessünk tulkok helyett ajkainkkal.
Bweretsani zopempha zanu ndipo bwererani kwa Yehova. Munene kwa Iye kuti, “Tikhululukireni machimo athu onse ndi kutilandira mokoma mtima, kuti tithe kukuyamikani ndi mawu a pakamwa pathu.
3 Assúr nem segít minket, lóra nem ülünk, és nem mondjuk többé: istenünk! kezeink művének – te, kiben irgalmat talál az árva!
Asiriya sangatipulumutse; ife sitidzakwera pa akavalo ankhondo, sitidzanenanso kuti, ‘Milungu yathu’ kwa zimene manja athu omwe anazipanga, pakuti ndinu amene mumachitira chifundo ana amasiye.”
4 Meggyógyítom elpártolásukat, szeretem őket önkéntes szeretettel; mert elfordult tőle haragom.
Ine ndidzachiza kusakhulupirika kwawo ndipo ndidzawakonda mwaufulu pakuti ndaleka kuwakwiyira.
5 Mint a harmat úgy leszek Izraélnek, virulni fog mint a liliom; gyökeret verjen mint a Libánon.
Ndidzakhala ngati mame kwa Israeli Ndipo iye adzachita maluwa ngati kakombo. Adzazika mizu yake pansi ngati mkungudza wa ku Lebanoni;
6 Terjedjenek gallyai és olyan legyen a mint az olajfáé a dísze, illata pedig olyan, mint a Libánoné.
mphukira zake zidzakula. Kukongola kwake kudzakhala ngati mtengo wa olivi, kununkhira kwake ngati mkungudza wa ku Lebanoni.
7 Újra lesznek árnyékában ülők, termelnek gabonát és virulnak, mint a szőlőtő; híre olyan, mint a Libánon boráé.
Anthu adzakhalanso mu mthunzi wake. Iye adzakula bwino ngati tirigu. Adzachita maluwa ngati mphesa ndipo kutchuka kwake kudzakhala ngati vinyo wochokera ku Lebanoni.
8 Efraim: mi közöm többé a bálványokhoz? – Én meghallgattam és szemmel tartom; olyan vagyok mint a zöldellő cziprus, tőlem nyeretik gyümölcsöd!
Efereimu adzati, “Ndidzachita nawonso chiyani mafano? Ine ndidzamuyankha ndi kumusamalira. Ine ndili ngati mtengo wa payini wobiriwira; zipatso zako zimachokera kwa Ine.”
9 Ki oly bölcs, hogy megértse ezeket, értelmes, hogy megismerje? Mert egyenesek az Örökkévaló útjai, s az igazak járnak rajtuk, az elpártolók pedig megbotlanak rajtuk.
Ndani ali ndi nzeru? Adzazindikire zinthu izi. Ndani amene amamvetsa zinthu? Adzamvetse izi. Njira za Yehova ndi zolungama; anthu olungama amayenda mʼmenemo, koma anthu owukira amapunthwamo.

< Hóseás 14 >