< भजन संहिता 136 >
1 याहवेह का धन्यवाद करो, क्योंकि वे भले हैं,
Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino.
2 परम परमेश्वर के प्रति आभार अभिव्यक्त करो.
Yamikani Mulungu wa milungu.
3 उनके प्रति, जो प्रधानों के प्रधान हैं, आभार अभिव्यक्त करो:
Yamikani Ambuye wa ambuye,
4 उनके प्रति, जिनके अतिरिक्त अन्य कोई अद्भुत कार्य कर ही नहीं सकता,
Iye yekhayo amene amachita zodabwitsa zazikulu,
5 जिन्होंने अपनी सुबुद्धि से स्वर्ग का निर्माण किया,
Amene mwachidziwitso chake anapanga mayiko akumwamba,
6 जिन्होंने जल के ऊपर पृथ्वी का विस्तार कर दिया,
Amene anayala dziko lapansi pamwamba pa madzi,
7 जिन्होंने प्रखर प्रकाश पुंजों की रचना की,
Amene anapanga miyuni ikuluikulu,
8 दिन के प्रभुत्व के लिए सूर्य का,
Dzuwa lilamulire usana,
9 रात्रि के लिए चंद्रमा और तारों का;
Mwezi ndi nyenyezi zilamulire usiku,
10 उन्हीं के प्रति, जिन्होंने मिस्र देश के पहलौठों की हत्या की,
Amene anakantha ana woyamba kubadwa a Igupto,
11 और उनके मध्य से इस्राएल राष्ट्र को बाहर निकाल लिया,
Natulutsa Israeli pakati pawo,
12 सशक्त भुजा और ऊंची उठी हुई बांह के द्वारा;
Ndi dzanja lamphamvu ndi mkono wotambasuka,
13 उन्हीं के प्रति, जिन्होंने लाल सागर को विभक्त कर दिया था
Amene anagawa Nyanja Yofiira pakati,
14 और उसके मध्य की भूमि से इस्राएलियों को पार करवा दिया,
Nadutsitsa Israeli pakati pa nyanjayo,
15 किंतु फ़रोह और उसकी सेना को सागर ही में डुबो दिया;
Koma anakokolola Farao ndi ankhondo ake mʼNyanja Yofiira,
16 उन्हीं के प्रति, जिन्होंने अपनी प्रजा को बंजर भूमि से पार कराया;
Amene anatsogolera anthu ake mʼchipululu
17 जिन्होंने प्रख्यात राजाओं की हत्या की,
Amene anakantha mafumu akuluakulu,
18 जिन्होंने सशक्त राजाओं का वध कर दिया,
Napha mafumu amphamvu,
19 अमोरियों के राजा सीहोन का,
Siloni mfumu ya Aamori,
21 तथा उनकी भूमि निज भाग में दे दी,
Napereka dziko lawo ngati cholowa,
22 अपने सेवक इस्राएल को, निज भाग में दे दी,
Cholowa cha mtumiki wake Israeli;
23 उन्हीं के प्रति, जिन्होंने हमारी दुर्दशा में हमारी सुधि ली,
Amene anatikumbukira ife anthu opeputsidwa,
24 और हमें हमारे शत्रुओं से मुक्त किया,
Amene anatimasula kwa adani athu,
25 जो सब प्राणियों के आहार का प्रबंध करते हैं,
Amene amapereka chakudya kwa cholengedwa chilichonse,
26 स्वर्गिक परमेश्वर के प्रति आभार अभिव्यक्त करो,
Yamikani Mulungu wakumwamba,