< תהילים 82 >

מזמור לאסף אלהים נצב בעדת-אל בקרב אלהים ישפט 1
Salimo la Asafu. Mulungu akutsogolera msonkhano waukulu; Iye akuweruza pakati pa “milungu.”
עד-מתי תשפטו-עול ופני רשעים תשאו-סלה 2
“Mudzateteza osalungama mpaka liti, ndi kukondera anthu oyipa?
שפטו-דל ויתום עני ורש הצדיקו 3
Tetezani anthu ofowoka ndi amasiye; mukhazikitse ufulu wa anthu osauka ndi ozunzika.
פלטו-דל ואביון מיד רשעים הצילו 4
Landitsani anthu ofowoka ndi osowa; apulumutseni mʼdzanja la anthu oyipa.
לא ידעו ולא יבינו-- בחשכה יתהלכו ימוטו כל-מוסדי ארץ 5
“Iwo sadziwa kanthu, sazindikira kalikonse. Amayendayenda mu mdima; maziko onse a dziko lapansi agwedezeka.
אני-אמרתי אלהים אתם ובני עליון כלכם 6
“Ndinati, ‘Inu ndinu Mulungu, nonsenu ndinu ana a Wammwambamwamba.’
אכן כאדם תמותון וכאחד השרים תפלו 7
Koma mudzafa ngati anthu wamba; mudzagwa ngati wolamula wina aliyense.”
קומה אלהים שפטה הארץ כי-אתה תנחל בכל-הגוים 8
Dzukani Inu Mulungu, weruzani dziko lapansi, pakuti mayiko onse ndi cholowa chanu.

< תהילים 82 >