< תהילים 110 >

לדוד מזמור נאם יהוה לאדני--שב לימיני עד-אשית איביך הדם לרגליך 1
Salimo la Davide. Yehova akuwuza Mbuye wanga kuti, “Khala ku dzanja langa lamanja mpaka nditasandutsa adani ako kukhala chopondapo mapazi ako.”
מטה-עזך--ישלח יהוה מציון רדה בקרב איביך 2
Yehova adzakuza ndodo yamphamvu ya ufumu wako kuchokera mʼZiyoni; udzalamulira pakati pa adani ako.
עמך נדבת ביום חילך בהדרי-קדש מרחם משחר לך טל ילדתיך 3
Ankhondo ako adzakhala odzipereka pa tsiku lako la nkhondo. Atavala chiyero chaulemerero, kuchokera mʼmimba ya mʼbandakucha, udzalandira mame a unyamata wako.
נשבע יהוה ולא ינחם-- אתה-כהן לעולם על-דברתי מלכי-צדק 4
Yehova walumbira ndipo sadzasintha maganizo ake: “Ndiwe wansembe mpaka muyaya monga mwa unsembe wa Melikizedeki.”
אדני על-ימינך מחץ ביום-אפו מלכים 5
Ambuye ali kudzanja lako lamanja; Iye adzaponda mafumu pa tsiku la ukali wake.
ידין בגוים מלא גויות מחץ ראש על-ארץ רבה 6
Adzaweruza anthu a mitundu ina, adzadzaza dziko lapansi ndi mitembo ndipo adzaphwanya olamulira a pa dziko lonse lapansi.
מנחל בדרך ישתה על-כן ירים ראש 7
Iye adzamwa mu mtsinje wa mʼmbali mwa njira; choncho adzaweramutsa mutu wake.

< תהילים 110 >